Yeremiya
MUTU1
1MawuaYeremiyamwanawaHilikiyawaansembe ameneanalikuAnatotim’dzikolaBenjamini:
2MawuaYehovaanadzakwaiyem’masikuaYosiya+ mwanawaAmonimfumuyaYuda,m’chakacha13cha ulamulirowake
+3Linafikansom’masikuaYehoyakimu+mwanawa YosiyamfumuyaYuda,+mpakakumapetokwachakacha 11chaZedekiya+mwanawaYosiyamfumuyaYuda,+ mpakapameneYerusalemuanatengedwakupitaku ukapolom’mweziwachisanu.
4PamenepomauaYehovaanadzakwaine,kuti, 5Ndisanakulengem’mimbandinakudziwa;ndipo usanatulukem’mimbandinakupatulaiwe,ndipo ndinakuikaiwemneneriwaamitundu
6Pamenepondinati,Ha,AmbuyeYehova!tawonani, sindingathekuyankhula:pakutindinemwana.
7KomaYehovaanatikwaine,Usanenekuti,Ndine mwana;
8Usachitemanthandinkhopezawo,pakutiInendilindi iwekutindikulanditse,atiYehova
9PamenepoYehovaanatambasuladzanjalake,nakhudza pakamwapanga.NdipoYehovaanatikwaine,Taona, ndaikamauangamkamwamwako
10Taona,lerondakuikaiwewolamuliraamitundundi maufumu,kutiuzule,ndikupasula,ndikuwononga,ndi kugwetsa,kumanga,ndikubzala
11NdipomauaYehovaanadzakwaine,kuti,Yeremiya, uonaciani?Ndipondinati,Ndikuonandodoyamtengowa amondi
12PamenepoYehovaanatikwaine,Waonabwino; 13NdipomauaYehovaanadzakwainekachiwiri,kuti, Uonachiyani?Ndipondinati,Ndikuonamphikawotentha; ndinkhopeyaceinalozakumpoto.
14PamenepoYehovaanatikwaine,Choipachidzabuka kucokerakumpoto,paonseokhalam’dziko
15Pakutitaonani,ndidzaitanamafukoonseamaufumua kumpoto,atiYehova;+Iwoadzafika,+ndipoaliyense adzaikampandowakewachifumupachipatachazipataza Yerusalemu+ndimalingaakeozungulira+ndimizinda yonseyaYuda
+16Ndidzawauzazigamulo+zangapazoipazawozonse, +ameneanandisiya+ndikufukizansembekwamilungu ina+ndikulambirantchitozamanjaawo
17Cifukwacaceudzimangirem’chuunomwako,nuwuke, nunenenaozonsendikuuzaiwe; 18Pakutitaona,ndakusandutsalerokukhalamudzi wokhalandimipandayotchingidwa,mzatiwachitsulo,ndi makomaamkuwapadzikolonse,pamafumuaYuda,pa akalongaake,ndipaansembeake,ndipaanthuam’dziko 19Ndipoadzamenyanananu;komasadzakulakaiwe; pakutiInendilindiiwe,atiYehova,kutindikulanditse.
MUTU2
1NdipomauaYehovaanadzakwaine,kuti, 2Pitaukafuulem’makutuaYerusalemu,ndikuti,Atero Yehova;Ndikumbukilaiwe,cifundocaubwanawako,
cikondicamaukwatiako,pameneunanditsatam’cipululu, m’dzikolosabzalidwa
3IsrayelianaliwopatulikakwaYehova,ndizipatso zoyambazazokololazake;choipachidzawagwera,ati Yehova
4ImvanimawuaYehova,inuanyumbayaYakobo,ndi mabanjaonseanyumbayaIsrayeli;
5AteroYehova,Cholakwachanjichimenemakoloanu anapezamwaine,kutianandipitirakutali,natsatazachabe, nakhalaopandapake?
6Ndiposananenekuti,AlikutiYehova,ameneanatitulutsa m’dzikolaAigupto,ameneanatitsogoleram’chipululu, m’dzikolazipululundilamaenje,m’dzikolachilalandila mthunziwaimfa,m’dzikolosapitamomunthu,ndilopanda munthuwokhalamo?
7Ndipondinakulowetsanim’dzikolazipatsozambiri,kuti mudyezipatsozakendizokomazake;+Komapamene munalowa,munadetsadzikolanga,+ndipocholowa changamunachisandutsachonyansa
8Ansembesanati,AlikutiYehova?+Ogwirachilamulo sanandidziwe.Abusa+nawonsoanandilakwira+ndi aneneri+ananeneramwaBaala+ndikutsatirazinthu zopandaphindu.
9Cifukwacacendidzatsutsanansonanu,atiYehova,ndipo ndidzatsutsanandianaaanaanu
10PakutimuolokezisumbuzaKitimu,ndipomuwone;+ TumizanianthukuKedara,+ndipomuonengatizili choncho
11Kodimtunduwaanthuwasinthamilunguyawo,imene similungu?komaanthuangaasinthaulemererowawondi chosapindula
12Dzizizwani,inumiyambainu,ndiichi,ndikuchita manthandimanthaaakulu,khalaniabwinjandithu,ati Yehova
13Pakutianthuangaachitazoipaziwiri;andisiyaine kasupewamadziamoyo,nadzibowolerazitsime,zitsime zong'ambika,zosakhalamomadzi
14KodiIsrayelindikapolo?kodiiyendikapolo wobadwirakunyumba?waonongekabwanji?
15Mikangoinamtukulira,nipfuula,nipasuladzikolace; 16AnaaNofindiTahapanesianathyolansongayamutu wako
17Kodisimunadzichitirezimenezi,popezamunasiya YehovaMulunguwanu,pameneanakutsogoleranipanjira?
18TsopanoulindichiyanipanjirayakuIguputokuti ukamwemadziakuSihori?Kapenaulindichiyanipanjira yakuAsuri,kumwamadziam’nyanja?
+19Kuipakwako+kudzakudzudzula,+ndipokupanduka kwako+kudzakudzudzula
20Pakutikuyambirakalendinathyolagolilako,ndi kudatulazomangirazako;ndipounati,Sindidzalakwa; pakusokerapazitundazonsezazitali,ndipatsindepa mtengouliwonsewauwisindikuchitadama.
21Komainendinabzaliraiwemtengowampesa wolemekezeka,mbeuyabwinoyonse;
+22Ngakhalekutiwasambandisopo+n’kudzitengera sopowambiri,+komamphulupuluyakoyadziwika pamasopanga,’+wateroYehova,AmbuyeWamkulu Koposa.
23Unganenebwanjikuti,Sindinadetsedwa,sindinatsatire Abaala?penyanjirayakom’chigwa,dziwachimene unachita;
Yeremiya
24buruwakuthengowozolowerachipululu,amene amauziramphepopakufunakwake;panthawiyakendani angaubweze?onseakuufunasadzatopa;m’mweziwake adzampeza.
25Lekaphazilakolisachitensapato,ndipakhosipakopa ludzu;komaiweunati,Palibechiyembekezo;pakuti ndakondaalendo,ndipondidzawatsata
26Mongambalaichitidwamanyaziikapezedwa, momwemonyumbayaIsrayeliichitamanyazi;iwo, mafumuawo,akalongaawo,ansembeawo,ndianeneri awo,
27ndikunenakwamtengo,Iwendiweatatewanga;ndi kwamwala,InumwandibalaIne;pakuti ananditembenukira,sinkhopezao;
28Komailikutimilunguyako,imeneunadzipangira? adzuke,ngatiangathekukupulumutsam'nthawiyansautso yako;pakutimongamwakuwerengakwamidziyako, milunguyako,iweYuda
29Mudzatsutsanananebwanji?nonsemwalakwiraIne,ati Yehova
30Ndinakanthaanaanupachabe;sanalandirakulangidwa; lupangalanuladyaanenerianu,ngatimkangowowononga.
31Inumbadwo,onanimawuaYehovaKodindakhala chipululukwaIsraele?dzikolamdima?chifukwachakeati anthuanga,Ndifeambuye;sitidzabweransokwaInu?
32Kodinamwaliangaiwalezokongoletsazake,kapena mkwatibwimalayaake?komaanthuangaandiiwalaIne masikuosawerengeka.
33Ukonzanjinjirayakokufunafunacikondi?chifukwa chakeiwensowaphunzitsaoipanjirazako
34Ndiponsom’malayaakomupezedwamwaziwamoyo waaumphawiwosacimwa;
35Komaiweukuti,Popezandinewosacimwa,mkwiyo waceudzandicokera.Taona,ndidzatsutsananawe,popeza uti,Sindinacimwa
36Bwanjiukuyendayendakoterokutiusinthenjirayako? iwensoudzachitamanyazindiIgupto,mongaunachitira manyaziAsuri
37Inde,mudzaturukakwaiye,ndimanjaanupamutupanu;
MUTU3
1Akuti,Ngatimwamunaakacotsamkaziwace,nacoka kwaiye,nakakwatiwandimwamunawina,kodi adzabwereransokwaiye?dzikolimenelosilidzaipitsidwa ndithu?komawachitachigololondimabwenziambiri; komabwereranikwaine,atiYehova
2Kwezeramasoakokumisanje,nuwonekumene sunagonekoMunawakhaliram’njira,mongaMwarabia m’chipululu;ndipowaipitsadzikondizigololozakondi zoipazako
3Cifukwacacemvulayatha,ndipopanalibemvulaya masika;ndipounalindimphumiyahule,unakanakuchita manyazi
4Kodisudzandifuulirakuyambiralerolino,kuti,Atate wanga,ndiwebwenzilaubwanawanga?
5Kodiadzasungamkwiyowakempakakalekale?kodi adzausungakufikirachimaliziro?Taona,wanenandi kuchitazoipamongaungathe
6Yehovaanatinsokwainem’masikuamfumuYosiya, KodiwaonachimeneIsrayeliwobwereram’mbuyo
wachita?wakwerapamapirionseaatali,ndipatsindepa mitengoyaiwisiyonse,nachitadamakumeneko.
7Ndipondinatiatathakuchitazonsezi,Ubwererekwaine Komasanabwerere.Ndipomlongowakewachinyengo Yudaanaonazimenezo.
8Ndipondinaona,popezandinamcotsaIsrayeliwobwerera m’mbuyo,ndikumpatsakalatawacilekanirocifukwaca cigololoconse;komamlongowacewonyengaYuda sanaopa,komaanamukanacitacigololo
9Ndipokunachitikachifukwachakupepukakwauhule wake,kutianaipitsadziko,nachitachigololondimiyalandi mitengo
+10Ngakhalezilichoncho,m’balewakewachinyengo, Yuda,sanabwererekwainendimtimawakewonse,+ komamwachinyengo,”+wateroYehova
11NdipoYehovaanatikwaine,Israyeliwobwerera wadziyeserawolungamakoposaYudawonyenga
12Pitanulalikiremauawakumpoto,ndikuti,Bwerera, iweIsrayeliwobwerera,atiYehova;ndiposindidzagwetsa mkwiyowangapainu,pakutindinewachifundo,ati Yehova,ndiposindidzasungamkwiyompakakalekale 13Komavomerezanimphulupuluzako,kutiwalakwira YehovaMulunguwako,ndikupatukiranjirazakokwa alendopatsindepamitengoyaiwisiyonse,osamveramawu anga,atiYehova.
14Bwerani,inuanaobwerera,atiYehova;pakutiine ndakwatiwakwainu:ndipondidzakutenganiinummodzi wamudzi,ndiawiriabanja,ndipondidzakutengeraniinu kuZiyoni;
15Ndipondidzakupatsaniinuabusaapamtimapanga, ameneadzadyetsainundichidziwitsondiluntha.
16Ndipokudzachitikakuti,mukadzachulukandikucuruka m’dziko,m’masikuamenewo,”+wateroYehova, sadzanenansokuti,“LikasalapanganolaYehova,”+ silidzabweransom’maganizo,+ndipo sadzalikumbukiransondiposadzaulanga;ndipo sichidzachitidwanso.
17PanthawiyoadzatchaYerusalemumpandowachifumu waYehova;+ndimitunduyonseyaanthu idzasonkhanitsidwakumeneko,+kudzinalaYehova,ku Yerusalemu,+ndiposadzatsatiransokuumirirakwa mitimayawoyoipa
18M’masikuamenewonyumbayaYudaidzayenda pamodzindinyumbayaIsiraeli,+ndipoiwoadzabwera pamodzikuchokerakudzikolakumpotokupitakudziko limenendinaperekakwamakoloanukutilikhalecholowa chawo
19Komandinati,Ndidzakuikabwanjipakatipaana,ndi kukupatsadzikolokoma,cholowachokomachamakamua amitundu?ndipondinati,UdzanditchaIneAtate;ndipo sudzachokakwaine
+20Ndithudi,+mongammenemkaziwasiyamwamuna wakemonyenga,+inunsomwandichitirazachinyengo+ inunyumbayaIsiraeli,”+wateroYehova
+21Mawuanamvekam’malookwezeka,+kulira+ndi mapembedzero+aanaaIsiraeli,+chifukwaapotozanjira zawo+ndipoaiwalaYehovaMulunguwawo.
22Bwerani,anaobwererainu,ndipondidzachiritsa kubwererakwanuTaonani,tabwerakwaInu;pakutiInu ndinuYehovaMulunguwathu.
+23Zoonadi,chipulumutsochoyembekezekakuchokera kumapiri+ndim’phirilamapirin’chachabe;
24Pakutimanyaziadadyantchitoyamakoloathu kuyambiraubwanawathu;nkhosazawonding’ombezawo, anaawoaamunandiaakazi
25Tigonapansim’manyaziathu,manyaziathuatiphimba; pakutitachimwiraYehovaMulunguwathu,ifendimakolo athu,kuyambiraubwanawathukufikiralero,osamvera mauaYehovaMulunguwathu
MUTU4
1Ukabwerera,iweIsrayeli,atiYehova,bwererakwaIne; ndipoukacotsazonyansazakopamasopanga,sudzacoka 2Ndipoudzalumbira,kuti,PaliYehova,m’coonadi, m’ciweruzo,ndim’cilungamo;ndipomitundu idzadalitsidwamwaIye,nadzadzitamandiramwaiye
3PakutiYehovaaterokwaanthuaYudandiYerusalemu, Limanimathithianu,ndipomusabzalepakatipaminga 4DzichekenikwaYehova,ndikuchotsakhungulamitima yanu,inuamunaaYudandiokhalam’Yerusalemu; 5NenanimuYuda,lengezanimuYerusalemu;ndikunena kuti,Limbanilipengam’dziko;
6KwezanimbenderakuZiyoni,bwererani,musaime; pakutindidzatengerazoipazochokerakumpoto,ndi chiwonongekochachikulu
7Mkangowakweram’nkhalangoyake,ndipowowononga amitundualim’njira;watulukam’malomwace kudzasandutsadzikolakobwinja;ndimidziyanu idzapasuka,yopandawokhalamo.
8Chifukwachaichimuvalezigudulim’chuunomwanu, liranindikubuma;pakutimkwiyowaukaliwaYehova sunatichokere.
9Ndipopadzakhalatsikulimenelo,atiYehova,kutimtima wamfumuudzatayika,ndimitimayaakalonga;ndipo ansembeadzazizwa,ndianeneriadzazizwa.
10Pamenepondinati,Ha,AmbuyeYehova!ndithu, wanyengakwambirianthuawandiYerusalemu,ndikuti, Mudzakhalandimtendere;pamenelupangalifikiramoyo.
11PanthawiyoanthuawandiYerusalemuadzanenakuti, ‘Mphepoyowuma+yam’malookwezekam’chipululu yopitakwamwanawamkaziwaanthuanga,yosaulutsa kapenakuyeretsa
12Ngakhalemphepoyamkunthoyochokeram’malo amenewoidzafikakwaine; 13Taonani,adzakwerangatimitambo,ndimagaretaake adzakhalangatikamvulumvulu;Tsokakwaife!pakuti tafunkhidwa.
14OYerusalemu,sambitsamtimawakokucokerazoipa, kutiupulumuke.Maganizoakoopandapakeadzakhala mwaiwekufikiraliti?
+15PakutimawuakulengezakuchokerakuDani+ndipo akulengezatsoka+kuchokerakumapiriaEfuraimu
16Nenanikwaamitundu;taonani,lengezaniza Yerusalemu,kutialondaacokerakudzikolakutali, nafuuliramidziyaYuda
17Mongaalondaam’mundaauzungulira;pakuti wandipandukira,atiYehova
18Njirazanundizochitazanuzakuchitiraniizi;ichindi choipachako,chifukwandichowawa,chifukwachimafika pamtimapako
19M'mimbamwanga,m'mimbamwanga!Ndiwawa mumtimamwanga;mtimawangauchitaphokosomwaine;
Sindingathekukhalachete,chifukwawamva,moyowanga, kulirakwalipenga,kulirakwankhondo.
20Chiwonongekopachiwonongekochikufuula;pakuti dzikolonselapasuka;mahemaangaafunkhidwa modzidzimutsa,ndinsaruzangam'kamphindi.
21Kodindidzaonambenderakufikiraliti,ndikumva kulirakwalipenga?
22Pakutianthuangandiopusa,sanandidziwa;aliana opulukira,ndiopandanzeru;
23Ndinapenyadzikolapansi,ndipo,taonani,linalilopanda kanthu,lopandakanthu;ndikumwamba,ndipokunalibe kuwala
24Ndinaonamapiri,ndipotaonani,ananjenjemera,ndi zitundazonsezinagwedezeka
25Ndinapenya,taonani,panalibemunthu,ndimbalame zonsezam’mlengalengazinathawa;
26Ndinaona,ndipotaonani,maloobalazipatsoanali chipululu,ndimidziyakeyonseyapasukapamasopa Yehova,ndimkwiyowakewoopsa.
27PakutiateroYehova,Dzikolonselidzakhalabwinja; komasindidzathetsa
28Chifukwachaichidzikolapansilidzalira,ndithambola kumwambalidzadetsedwa;
29Mzindawonseudzathawachifukwachaphokosola okwerapamahatchindioponyauta;adzalowam’nkhalango, nakweram’matanthwe;
30Ndipoukafunkhidwa,udzachitachiyani?Ungakhale udzivekakapezi,ungakhaleudzikometseranazo zokometserazagolidi,ungakhalewang'ambankhopeyako ndizojambula,udzikongoletsapachabe;okondedwaako adzakupeputsa,nadzafunamoyowako.
31Pakutindamvamawungatiamkaziwobala,ndi zowawangatizamkaziwobalamwanawakewoyamba, mawuamwanawamkaziwaZiyoni,ameneakulira,amene akutambasulamanjaake,kuti,Tsokainetsopano!pakuti moyowangawalemandiamapha
MUTU5
1Thamanganiukundiukom’makwalalaaYerusalemu, taonanitsopano,dziwani,ndikufunafunam’makwalalaace, ngatimudzapezamunthu,ngatialipowinawocitaciweruzo, wakufunacoonadi;ndipondidzachikhululukira.
2Ndipongakhaleadzati,Yehovaalindimoyo;Ndithu, alumbiramonama
3InuYehova,kodimasoanualipachoonadi? mudawakantha,komasanadandaule;mudawatha,koma akanakudzudzulidwa;aumitsankhopezaokoposa thanthwe;akanakubwerera
4Chifukwachakendinati,Zoonadi,awandiaumphawi;ali opusa,pakutisadziwanjirayaYehova,kapenaciweruzoca Mulunguwao.
5Ndidzafikakwaakulu,ndikunenanawo;pakutiadziwa njirayaYehova,ndiciweruzocaMulunguwao; 6Cifukwacacemkangowakuthengoudzawapha,ndi mmbuluwamadzuloudzawaononga,nyalugwe adzalonderamidziyao;yensewakuturukam’menemo adzakhadzulidwa;
7Ndidzakukhululukirabwanjipaichi?anaakoandisiya Ine,nalumbirapayosakhalamilungu;nditawadyetsa mokhuta,anacitacigololo,nasonkhanamaguluankhondo m'nyumbazaakaziacigololo
8Analingatiakavalookhutam’maŵa:Yenseanafuulira mkaziwamnansiwake.
9Kodisindidzawalangachifukwachaizi?atiYehova; ndipomoyowangasudzabwezeracilangomtunduwotere uwu?
10Kweranipamalingaace,nimuononge;koma musamalizekonse:chotsanimalingaace;pakutisiza Yehova.
+11PakutinyumbayaIsiraelindinyumbayaYuda zandichitirazachinyengokwambiri,’+wateroYehova
12AnatsutsaYehova,ndikuti,Siiye;kapenachoipa sichidzatigwera;ndipositidzawonalupangakapenanjala; 13Ndipoaneneriadzakhalamphepo,ndipomulibemawu mwaiwo:choterozidzawachitikira
14CifukwacaceateroYehova,Mulunguwamakamu, Popezamwanenamauawa,taonani,ndidzayesamauanga m’kamwamwakomongamoto,ndianthuawankhuni, ndipoudzawanyeketsa
15Taonani,ndidzakutengeranimtunduwakutali,inua nyumbayaIsrayeli,atiYehova;ndiwomtundu wamphamvu,mtunduwakale,mtunduumenechinenero chawosimuchidziwa,kapenakumvachimeneiwoamanena. 16Phodolawolilingatimandaotseguka,onsewondianthu amphamvu
17Ndipoadzadyazokololazanu,ndichakudyachanu chimeneanaanuamunandiakaziadzadya;adzadya nkhosazanunding’ombezanu;adzadyamipesayanundi mikuyuyanu;adzasaukandilupangamidziyanu yamalinga,imenemunaikhulupirira
18Komabem’masikuamenewo,’+wateroYehova, ‘Sindidzakutheranindithu.
19Ndipopadzakhala,pamenemudzati,Chifukwaninji YehovaMulunguwathuwatichitiraifezonsezi?pamenepo uzitikwaiwo,MongamomwemunandisiyaIne,ndi kutumikiramilunguyachilendom’dzikolanu,momwemo mudzatumikiraalendom’dzikolaeni
20Nenaniizim’nyumbayaYakobo,ndikuzilengeza m’Yuda,kuti,
21Tamveranitsono,anthuopusainu,ndiopandanzeru; amenealinawomaso,komaosapenya;amenealindi makutu,komaosamva;
22SimundiopaInekodi?atiYehova:Kodi simudzanjenjemerapamasopanga,amenendinaika mchengaukhalemalekezeroanyanja,ndilamulolosatha, kutisungathekuwadutsa;Ngakhaleatabangula,koma sangathekuwoloka?
23Komaanthuawaalindimtimawopandukandi wopanduka;apanduka,napita.
24Ndiposanenam’mitimamwawo,Tiyenitsonotiope YehovaMulunguwathu,ameneamavumbitsiramvula, mvulayoyambandiyamasika,panyengoyake;
25Zolakwazanuzapatutsazinthuizi,ndipomachimoanu akukanizainuzabwino
26Pakutipakatipaanthuangapalianthuoipa;atchera msampha,agwiraanthu
27Mongakholalidzalandimbalame,momwemonso nyumbazaozadzalandicinyengo;
28Iwoanenepa,anyezimira,inde,amapitirirantchitoza oipa;ndipoufuluwaumphawisaweruza
29Kodisindidzawalangachifukwachaizi?atiYehova; moyowangasudzabwezeracilangomtunduwotere?
30Chodabwitsandichowopsyachachitikam’dziko;
31Aneneriakuloseramonama,ndipoansembe amalamuliramwaiwo.ndipoanthuangaakondakuti zikhalechomwecho:ndipomudzachitachiyanipamapeto pake?
MUTU6
1InuanaaBenjamini,sonkhanitsanikuthawapakatipa Yerusalemu,ndikulizalipengakuTekoa,nimuyike chizindikirochamotom'Beti-hakeremu;pakutichoipa chatulukirakumpoto,ndichiwonongekochachikulu
2NdafaniziramwanawamkaziwaZiyonindimkazi wokongolandiwosalimba.
3Abusandizowetazaoadzafikakwaiye;adzamanga mahemaaomomzungulira;iwoadzadyerayensem’malo mwake.
4Konzekeraninkhondoyomenyananaye;ukani,tikwere usanaTsokakwaife!pakutiusanawapita,pakutimithunzi yamadzuloyatambasuka.
5Nyamukani,tipiteusiku,ndipotiwonongenyumbazake zachifumu
+6PakutiYehovawamakamuwanenakuti,‘Gwetsani mitengo+ndikumangachiundapaYerusalemuali nsautsoyonsepakatipace
7Mongakasupeaturutsamadziace,momwemoaturutsa zoipazace;chiwawandikufunkhazamvekamwaiye; pamasopangapalizowawandimabala
8Ulangizidwe,Yerusalemu,ungachokerekwaiwe;kuti ndingakusandutsebwinja,dzikolopandaanthu
9Yehovawamakamuatero,Iwoadzakunkhandithuotsala aIsrayelingatimpesa;
10Ndidzalankhulandiyani,ndikuchenjeza,kutiamve? taonani,makutuaondiosadulidwa,ndiposangathe kumvera;sakondweranazo.
11CifukwacacendadzalandiukaliwaYehova;Ndatopa ndikuugwira:ndidzautsanulirapaanaakunja,ndipa msonkhanowaanyamatapamodzi:pakutimwamunandi mkaziadzatengedwa,nkhalambapamodzindiiyewokhuta masiku
12Nyumbazawozidzasandukazaanthuena,mindayawo ndiakaziawopamodzi,+pakutindidzatambasuladzanja langapaanthuokhalam’dzikolo,”+wateroYehova
13Pakutikuyambirawamng’onokufikirawamkuluwa iwoonseachitachisiriro;ndikuyambirakwamneneri kufikirakwawansembe,onseachitamonyenga
14Achiritsansobalalamwanawamkaziwaanthuanga pang’ono,ndikuti,Mtendere,mtendere;pamenepalibe mtendere.
15Kodianachitamanyazipameneanachitachonyansa?iai, sanachitemanyazikonse,kapenakuchitamanyazi; chifukwachakeadzagwapakatipaiwoakugwa;panthawi imenendidzawalangaiwoadzagwetsedwa,atiYehova.
16AteroYehova,Imanim’njira,nimuwone,funsaniza mayendedweakale,kutinjirayabwinoilikuti,ndikuyenda m’menemo,ndipomudzapezampumulowamiyoyoyanu Komaadati,Sitidzayendamo 17Ndinakuikiranialonda,ndikuti,Mveranikulirakwa lipenga;Komaadati,Sitimvera 18Chifukwachakeimvani,inuamitundu,ndipodziwani, inukhamu,chimenechilipakatipawo.
19Tamvera,iwedzikolapansi,taona,ndidzatengeracoipa paanthuawa,cipatsocamaganizoao,cifukwasanamvera mauanga,kapenacilamulocanga,komaanacikana
20ZofukizazakuSebazindifikirabwanji,ndinzimbewa kudzikolakutali?nsembezanuzopsereza sizindivomerezeka,kapenansembezanusizindikoma
21CifukwacaceateroYehova,Taonani,ndidzaikiraanthu awazopunthwitsa,ndipoatatendianaadzawagwera pamodzi;mnansindibwenzilakeatayika
22Yehovaatero,Taonani,anthuakudzakuchokeraku dzikolakumpoto,ndipomtunduwaukuluudzaukitsidwa kuchokerakumalekezeroadzikolapansi
23Adzagwirautandimkondo;ndiankhanza,opanda chifundo;mawuawoalimkokomongatinyanja;+Iwo akukwerapamahatchi,+ndikufolangatianthuomenyana ndiiwe,+iwemwanawamkaziwaZiyoni.
24Tamvambiriyace,manjaathualefuka;
25Musaturukirekumunda,kapenakuyendam’njira;pakuti lupangalamdanindimanthaaliponsepo.
26Iwemwanawamkaziwaanthuanga,udzimangire chigudulim’chuunomwako,+ndikubvimvinizika m’phulusa;
27Ndakuikaukhalensanjandilingapakatipaanthuanga, kutiudziwendikuyesanjirayao
28Onsewondiopandukaankhanza,akuyendandimiseche: alimkuwandichitsulo;onsewondiowononga
29Mivumvuyapsa,mtovuwanyeketsandimoto;woyenga asungunukapachabe;pakutioipasazulidwa.
30Anthuadzawatchasilivawotayidwa,pakutiYehova wawakana
MUTU7
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova, kuti,
2ImanipachipatachanyumbayaYehova,nulalikire pamenepomawuawa,ndikuti,ImvanimawuaYehova, inunonseAyudaaYuda,amenemulowapazipataizi kudzalambiraYehova
3AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli, Konzaninjirazanundimachitidweanu,ndipo ndidzakukhalitsanim’maloano
4Musakhulupiriremawuonama,akuti,KachisiwaYehova, KachisiwaYehova,KachisiwaYehova,awandiwo 5Pakutimukakonzandithunjirazanundizochitazanu; mukaweruzandithupakatipamunthundimnansiwake; 6Mukapandakuponderezamlendo,mwanawamasiye,ndi mkaziwamasiye,osakhetsamwaziwosalakwapamaloano, osatsatamilunguina,kukupweteketsani;
7Pamenepondidzakukhalitsanim’maloano,m’dziko limenendinapatsamakoloanukunthawizanthawi
8Taonani,mukhulupiriramawuonama,osapindulakanthu.
+9Kodimudzaba,+kupha,+kuchitachigololo, kulumbiramonama,+kufukizansembezofukizakwa Baala,+ndikutsatiramilunguinaimenesimuidziwa?
10ndipobweranimudzaimepamasopangam’nyumbaiyi, imeneimatchedwadzinalanga,ndikuti,Tapulumutsidwa kuchitazonyansazonsezi?
11Kodinyumbaiyi,yochedwadzinalanga,yasanduka phangalaachifwambapamasopanu?Taonani,inenso ndachiwona,atiYehova
12KomapitanitsopanokumaloangaameneanalikuSilo, +kumenendinaikadzinalangapoyamba,+ndipomuone zimenendinachitakumenekochifukwachakuipakwa anthuangaAisiraeli.
13Ndipotsopano,popezamunacitanchitozonsezi,ati Yehova,ndipondinalankhulananu,kuukamamawandi kulankhula,komasimunamva;ndipondinakuitanani,koma simunayankha;
14Chifukwachakendidzachitiranyumbaiyi,yochedwa ndidzinalanga,imenemukhulupirira,ndimaloamene ndinakupatsaniinundimakoloanu,mongandinachitira Silo
15Ndipondidzakuchotsanipamasopanga,monga ndinatayaabaleanuonse,mbewuyonseyaEfraimu
16Chifukwachakeiweusapempherereanthuawa, usawakwezeremfuukapenapemphero,kapena kundipembedzeraine,pakutisindidzamveraiwe
17Kodisukuonazimeneakuchitam’mizindayaYudandi m’misewuyaYerusalemu?
18Anaakutolankhuni,+ndipoatateamasonkhamoto,+ ndipoakaziakukandaufa+kutiaphikiremfumukazi yakumwamba+mikate,+ndikuthiransembezachakumwa +kwamilunguina,+kutiandikwiyitse
19Kodiandikwiyitsa?atiYehova;kodisadziputaokhandi manyazipankhopezao?
20CifukwacaceateroAmbuyeYehova;Taonani,mkwiyo wangandiukaliwangazidzathiridwapamaloano,pa anthu,ndipanyama,ndipamitengoyakuthengo,ndipa zipatsozanthaka;ndipoudzayaka,komasudzazimitsidwa 21AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli;Ikani nsembezanuzopserezapansembezanu,ndikudyanyama. 22Pakutisindinalankhulendimakoloanu,kapena kuwauzazansembezopsereza,kapenansembe,tsikulija ndinawatulutsam’dzikolaAigupto;
23Komandinawauzacinthuici,ndikuti,Mveranimau anga,ndipondidzakhalaMulunguwanu,ndiinu mudzakhalaanthuanga;
24Komasanamvera,kapenakutcherakhutu,koma anayendam’upondikuumirakwamtimawaowoipa, nabwereram’mbuyo,osatikutsogolo.
+25Kuyambiratsikulimenemakoloanuanatuluka m’dzikolaIguputompakalero,+ndatumizakwainu atumikiangaonseaneneri,+tsikunditsikundikamadzuka m’mawandikuwatumiza
26Komasanandimveraine,kapenakutcherakhutu,koma anaumitsakhosilawo;
27Cifukwacaceuzinenanaomauawaonse;koma sadzamveraiwe;udzawaitananso;komasadzakuyankha.
28Komauzitikwaiwo,Umenewundimtunduwosamvera mauaYehovaMulunguwao,kapenakulandirakulangidwa; 29Metatsitsilako,Yerusalemu,ulitaye,nuimbemaliro pamisanje;pakutiYehovawakanandikuusiyambadwowa mkwiyowake
30PakutianaaYudaachitazoipapamasopanga,ati Yehova;
+31IwoanamangansomalookwezekaakuTofeti+ amenealim’chigwachamwanawaHinomu,+kutiatenthe anaawoaamunandiaakazipamotochimene sindinawalamulira,osalowamumtimamwanga
32Chifukwachake,taonani,masikuakudza,atiYehova, amenesudzatchedwansoTofeti,kapenachigwachamwana waHinomu,komachigwachakupha;
33Ndipomitemboyaanthuawaidzakhalachakudyacha mbalamezam’mlengalenga,ndichazirombozapadziko; ndipopalibewakuziingitsa
34Pamenepondidzaletsam’mizindayaYuda,ndi m’misewuyaYerusalemu,mawuachisangalalo,ndimawu akukondwa,mawuamkwatindimkwatibwi,pakutidziko lidzakhalabwinja
MUTU8
1Panthawiyo,atiYehova,adzatulutsamafupaamafumua Yuda,ndimafupaaakalongaake,ndimafupaaansembe, ndimafupaaaneneri,ndimafupaaokhalam'Yerusalemu m'mandaao;
2Ndipoadzawafunyululapamasopadzuwa,ndimwezi, ndikhamulonselakumwamba,ameneiwoanakonda,ndi ameneanawatumikira,ndiameneanatsatira,amene anafunafuna,ndiameneanalambira:iwo sadzasonkhanitsidwa,kapenakuikidwa;adzakhalandowe padzikolapansi
+3Ndipootsalaonseam’banjaloipaliadzasankhaimfa kuposamoyo+osatimoyo,+ameneatsalam’malomonse kumenendinawathamangitsira,”+wateroYehovawa makamu
4Ndipouzinenanao,AteroYehova;Kodiadzagwaosauka? kodiadzapatuka,osabwerera?
5Nangan’cifukwacianianthuawaakuYerusalemu abwereram’mbuyondikubwelelakosatha?agwira chinyengo,akanizakubwerera
6Ndinamverandikumva,komasanalankhulazolungama; yenseanatembenukiranjirayake,mongakavalo athamangirakunkhondo
7Inde,dokowem’mwambaadziwanyengozakezoikika; ndikamba,ndikamba,ndinamzeze,zisunganthawi yakufikakwao;komaanthuangasadziwachiweruzocha Yehova
8Mukutibwanji,Ndifeanzeru,ndichilamulochaYehova chilindiife?Taonani,adalipangapachabe;cholemberacha alembichilichabe
9Anzeruachitamanyazi,achitamantha,nagwidwa; taonani,akanamawuaYehova;ndipom'menemomuli nzeruyotani?
10Cifukwacacendidzaperekaakaziaokwaena,ndi mindayaokwaiwoadzalandira;pakutiyensekuyambira wamng’onokufikirawamkuruaperekamwadyera, kuyambiramnenerikufikirakwawansembeonseacita monyenga
11Pakutiacizakuvulazakwamwanawamkaziwaanthu angapang’ono,ndikuti,Mtendere,mtendere;pamene palibemtendere
12Kodianachitamanyazipameneanachitachonyansa?iai, sanachitemanyazikonse,kapenakuchitamanyazi; chifukwachakeadzagwapakatipaiwoakugwa;panthawi yakuwalangaiwoadzagwetsedwa,atiYehova
13Ndidzawathandithu,atiYehova:sipadzakhalamphesa pampesa,kapenankhuyupamkuyu,ndipomasamba adzafota;ndipozimenendawapatsazidzawapitirira. 14N’chifukwachiyanitikhalachete?sonkhanani,tilowe m’midziyamalinga,ndipotikhalechetem’menemo;pakuti YehovaMulunguwathuwatikhalitsachete,watipatsa madziandulukutitimwe,chifukwatachimwiraYehova
15Tinayembekezeramtendere,komapalibechabwino chinadza;ndinthawiyamoyo,ndipotaonanimavuto! +16Kupumakwaakavaloakekunamvekakuchokeraku Dani+ndipodzikolonselinanjenjemerachifukwacha kulirakwaanthuakeamphamvu.pakutiafika,nadyadziko, ndizonsezirim’mwemo;mzinda,ndiiwookhalamo 17Pakuti,taonani,ndidzatumizapakatipainunjoka, zimbalamba,zimenesizidzaloŵa,ndipozidzakulumaniinu, atiYehova
18Pamenendidzitonthozamtimandichisoni,mtima wangaunakomokamwaine
19Taonanimauamfuuwamwanawamkaziwaanthu angacifukwacaiwookhalakudzikolakutali,Kodi YehovasalimuZiyoni?simfumuyakemwaiyekodi? Anandikwiyitsabwanjindimafanoawoosemedwa,ndi zachabechabezachilendo?
20Zokololazapita,dzinjalatha,ndipoifesitinapulumuke 21Chifukwachakupwetekedwakwamwanawamkaziwa anthuangandapwetekedwa;Ndinewakuda;kudabwa kwandigwira
22Kodimulibemvungutim’Giliyadi?palibesing'anga pamenepo?Nangamwanawamkaziwaanthuanga sanachirabwanji?
MUTU9
1Ha!mutuwangaukadakhalamadzi,ndimasoanga kasupewamisozi,kutindilireusanandiusikuchifukwa chaophedwaamwanawamkaziwaanthuanga!
2Ha!ndikadakhalandipogonam'chipululu;kutindisiye anthuanga,ndikuchokakwaiwo!pakutionsendiwo acigololo,khamulaanthuonyenga
3Ndipoakungamalilimeawongatiutawawokunama; pakutiacokerakucoipandikucitacoipa,ndiposadziwaIne, atiYehova
4Yensechenjeranindimnansiwake,musakhulupirire mbalealiyense;
5Ndipoiwoadzanyengayensemnansiwake,ndipo sadzanenazoona;
6Kukhalakwanukulipakatipachinyengo;mwachinyengo akanakundidziwa,”+wateroYehova
7CifukwacaceateroYehovawamakamu,Taonani, ndidzawasungunula,ndikuwayesa;pakutindidzachita bwanjikwamwanawamkaziwaanthuanga?
8Lilimelaolilingatimuviwolasa;lilankhulachinyengo: winaalankhulamwamtenderendimnansiwakendi pakamwapake,komamumtimaamalolera
9Kodisindiyenerakuwalangachifukwachazimenezi?ati Yehova;moyowangasudzabwezeracilangomtundu wotere?
10Pakutimapirindidzaliriramisozindikuliramofuula, ndikuliramoliramokhalam’chipululu,chifukwa atenthedwa,koterokutipalibeangadutsemo;kapena munthusangathekumvamawuang'ombe;mbalameza m’mlengalengandinyamazonsezathawa;iwoapita
11NdipondidzasandutsaYerusalemumiyulu,phangala ankhandwe;ndipondidzasandutsamidziyaYudabwinja, lopandawokhalamo
12Ndaniwanzeru,kutiazindikireichi?ndipondaniamene m'kamwamwaYehovamwalankhulanaye,kutianene,kuti dzikoliwonongekendikutenthedwangatichipululu,kuti palibeameneadutsamo?
Yeremiya
+13Yehovawanenakuti:“Chifukwachakutianasiya chilamulo+changachimenendinachiikapamasopawo,+ ndiposanamveremawuanga+osayendamo
+14Komaatsatirakuumirirakwamitimayawo+ndi kutsatiraAbaala+amenemakoloawoanawaphunzitsa.
15CifukwacaceateroYehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli;Taonani,ndidzadyetsaiwo,ndiwoanthuawa, chitsambachowawa,ndikuwapatsamadziandulukuti amwe
16Ndidzabalalitsansopakatipaamitundu,ameneiwo kapenamakoloawosanawadziwe;
17AteroYehovawamakamu,Lingaliraniinu,nimuitane akazioliramaliro,kutiadze;ndipoitanitsaniakazianzeru, kutiadze;
18Ndipoafulumire,natilireifemaliro,kutimasoathu agwemisozi,ndizikopezathuzitulutsemadzi.
+19PakutimawuakuliraamvekakuchokerakuZiyoni+ kuti:“Ha!tachitamanyazikwambiri,chifukwatasiya dziko,chifukwanyumbazathuzatichotsa.
+20Komaakaziinu,imvanimawuaYehova,+ndipo makutuanualandiremawuam’kamwamwake,+ndipo muphunzitseanaanuaakazikulira,+ndipoaliyense aphunzitsemnansiwakekulira
21Pakutiimfayakweram’mazeneraathu,yalowa m’nyumbazathuzachifumu,kuphaanaakunja,ndi anyamatam’makwalala
22Nena,AteroYehova,Mitemboyaanthuidzagwangati ndowem’munda,ndingatidzanjalamanjalawotuta,ndipo palibewakuzisonkhanitsa
23Yehovawanenakuti:“Wanzeruasadzitamandire chifukwachanzeruzake,wamphamvuasadzitamandendi mphamvuzake,+wolemeraasadzitamandirechifukwacha chumachake
24Komaiyewodzitamandiraadzitamandiremwaichi,kuti amandizindikirandikundidziwaine,kutiinendineYehova amenendichitakukomamtimakosatha,chiweruzondi chilungamo,padzikolapansi; 25Taonani,masikuakudza,atiYehova,pamene ndidzalangaonseodulidwapamodzindiosadulidwa; +26Iguputo,+Yuda,+Edomu,+anaaAmoni,+ Mowabu,+ndionseokhalam’makonaam’chipululu,+ pakutimitunduyonseyindiyosadulidwa,+ndiponyumba yonseyaIsiraelindiyosadulidwa+mumtima.
MUTU10
1ImvanimauameneYehovaanenakwainu,inunyumba yaIsrayeli;
2AteroYehova,Musaphunzirenjirayaamitundu, musaopezizindikirozakumwamba;pakutiamitunduachita manthandiiwo
3Pakutimiyamboyaanthundiyopandapake:pakuti munthuamadulamtengom’nkhalango,ntchitoyamanjaa mmisirindinkhwangwa
4Amaukongoletsandisilivandigolidi;aukhomeretsandi misomalindinyundo,kutiusagwedezeke
5Zilizoongokangatimtengowakanjedza,koma osalankhula;ziyenerakunyamulidwa,chifukwasizipita musawaopa;pakutisangathekuchitachoipa,ndiponso mulibemwaiwokuchitachabwino.
6PopezapalibewinawongaInu,Yehova;ndinuwamkulu, ndipodzinalanundilalikulundimphamvu
7NdaniamenesakuopaniInu,Mfumuyaamitundu?pakuti kuyenerakwainu;popezamwaanzeruonseaamitundu, ndim’maufumuawoonse,palibewinawongaInu
8Komaonsealiopusandiopusa:mtengondiwo chiphunzitsochachabe.
9SilivawoyalidwakukhalamapaleanatengedwakuTarisi, ndigolidiwakuUfazi,nchitoyammisiri,ndiyamanjaa wosula;zobvalazaondizozabuluundizofiirira;
10KomaYehovandiyeMulunguwoona,ndiyeMulungu wamoyo,ndimfumuyosatha;
+11Muziwauzakuti,‘Milunguimenesinapange kumwambandidzikolapansi,+ndiyoidzawonongeka padzikolapansindipansipathambo.
12Iyeanalengadzikolapansindimphamvuyake, anakhazikitsadzikolapansindinzeruzake,ndipoanayala kumwambandikuzindikirakwake.
13Pamenealankhula,paliunyinjiwamadzim’mwamba, ndipoakwezeranthunzikumalekezeroadzikolapansi; alengamphezindimvula,naturutsamphepom’zosungira zace
14Munthualiyensealiwopusam’chidziwitsochake; 15Iwoalichabe,ndintchitoyamphulupulu;
16GawolaYakobosilingafananenazo,pakutiiyendiye analengazonse;ndipoIsrayelindiyendodoyacholowa chake:DzinalakendiYehovawamakamu.
17Sonkhanitsakatunduwakom’dziko,iwewokhala m’linga
18Yehovawanenakuti,‘Taonani,ndidzaponyerakunja anthuokhalam’dzikolinokamodzikokha,+ndipo ndidzawasautsa+kutiawapeze
19Tsokakwainechifukwachakupwetekedwakwanga! chilondachangachilichowawa:komandinati,Zowawaizi ndithu,ndipondiyenerakupiriranazo
20Chihemachangachapasuka,ndizingwezangazonse zaduka;anaangaandituruka,ndipopalibe;
21Pakutiabusaasandukaopandanzeru,ndipo sanafunefuneYehova;
22Taonani,mkokomowachiphokosochafika,ndi phokosolalikululotulukam’dzikolakumpoto,kusandutsa midziyaYudabwinja,phangalazinjoka.
23Yehova,ndidziwakutinjirayamunthusilimwaiye mwini;sikulikwamunthuwoyendakulongosolamapazi ake.
24Yehova,mundilangize,komandichiweruzo;osatimu mkwiyowanu,kutimungandiwonongeine
25ThiraniukaliwanupaamitunduosadziwaInu,ndipa mabanjaosaitanapadzinalanu;
MUTU11
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova, kuti, 2Imvaniinumawuapanganoili,ndikunenakwaamunaa Yuda,ndikwaokhalamuYerusalemu; 3Unenenao,AteroYehovaMulunguwaIsrayeli; Wotembereredwamunthuwosamveramawuapanganoili; 4chimenendinalamuliramakoloanutsikulija ndinawaturutsam’dzikolaAigupto,m’ng’anjoyachitsulo, ndikuti,Mveranimawuanga,ndikuwachitamongamwa zonsendikuuzaniinu; 5kutindikwaniritselumbirolimenendinalumbiriramakolo anu,kuwapatsadzikoloyendamkakandiuchingati
Yeremiya
mmenezililileroPamenepondinayankha,ndikuti, Zikhalechomwecho,Yehova.
6PamenepoYehovaanatikwaine,Lalikiramawuawa onsem’midziyaYuda,ndim’misewuyaYerusalemu,ndi kuti,Imvanimauapanganoili,ndikuwachita.
+7Pakutindinadzudzulamwamphamvumakoloanu+pa tsikulimenendinawatulutsam’dzikolaIguputompakalero, +ndilawiram’mamawandikuwadzudzula+kuti, ‘Mveranimawuanga
+8Komasanamvere+kapenakutcherakhutu+lawo,+ komaanayendaaliyensem’kuumirirakwamtimawake woipakomasanawachita
9NdipoYehovaanatikwaine,Chiwembuchapezekamwa anthuaYuda,ndimwaokhalam’Yerusalemu
10Iwoabwererakuzolakwazamakoloawo,amene anakanakumvamawuanga;+Iwoanatsatiramilunguina +ndikuitumikira:+nyumbayaIsiraelindinyumbaya Yudazaphwanyapangano+limenendinapanganandi makoloawo.
11CifukwacaceateroYehova,Taonani,ndidzawatengera coipa,cimenesadzathakuthawa;ndipoangakhale akandilirira,sindidzawamvera.
12PamenepomidziyaYudandiokhalam’Yerusalemu adzanka,nafuulirakwamilunguimeneakuifukiza;
13Pakutimongamwakuwerengakwamidziyako,iwe Yuda,milunguyako;ndipomongamwakuchulukakwa misewuyaYerusalemumudaukirakomaguwaamanyazi, maguwaansembeofukiziraBaala.
14Cifukwacaceusapempherereanthuawa,kapena kuwaikiramfuukapenapemphero;
15Kodiwokondedwawangaadzachitachiyanim'nyumba mwanga,popezawachitazonyansandianthuambiri,ndipo thupilopatulikalachokakwaiwe?ukachitazoipa, ukondwera.
16Yehovaanakutchadzinalako,Mtengowaazitona wauwisi,wokongolandiwazipatsozokoma; +17Yehovawamakamu,+ameneanakubzalani+wanena zoipazokhudzainuyo,+chifukwachazoipazimene nyumbayaIsiraelindinyumbayaYudaanachita pondikwiyitsa+pofukiziraBaala.
18NdipoYehovawandidziwitsa,ndipondidziwa; 19Komainendinalingatimwanawankhosakapena ng’ombeyopitakukaphedwa;ndiposindinkadziwakuti anandipangirachiwembu,ndikuti,Tiwonongemtengo pamodzindizipatsozake,ndipotimusadzem’dzikola amoyo,kutidzinalakelisakumbukikenso.
20Koma,Yehovawamakamu,amenemumaweruza molungama,amenemumayesaimpsondimtima,ndiloleni ndionekubwezerachilangochanupaiwo;
+21ChoteroYehovawanenazaanthuakuAnatotiamene akufunafunamoyowako+kuti,‘Usaloserem’dzinala Yehova,+kutiungafendidzanjalathu.
22CifukwacaceateroYehovawamakamu,Taonani, ndidzalangaiwo;anaaoaamunandiaakaziadzafandi njala;
23Ndiposipadzakhalawotsalamwaiwo,pakuti ndidzatengerazoipapaanthuakuAnatoti,m’chakacha kuwalanga
MUTU12
1InuYehovandinuwolungama,potsutsanananu;koma ndilankhulendiinuzamaweruzoanu;Njirayaoipa ipindulanji?Odalaachitachiwembuchifukwaninji?
2Munawabzala,inde,anazikamizu,aphuka,inde,abala zipatso;
3KomaInu,Yehova,mukundidziwa:Mwandiona, nimuyesamtimawangakwaInu;
4Dzikolidzalirakufikiraliti,ndizitsambazam’munda uliwonsezifota,chifukwachakuipakwaokhalamo? zilombozatha,ndimbalame;popezaanati,Iyesadzaona citsirizirocathu.
5Ngatiwathamangandioyendapansi,nakutopetsaiwe, udzalimbanabwanjindiakavalo?ndipongati adakutopetsanim’dzikolamtenderem’mene munalikhulupirira,nangamudzachitabwanjim’mabwinja aYordano?
6Pakutingakhaleabaleakondiam’nyumbayaatatewako anakuchitiraiwechiwembu;indeaitanakhamulaanthu pambuyopako;usawakhulupirire,angakhalealankhula nawemauokoma.
7Ndasiyanyumbayanga,ndasiyacholowachanga; Ndaperekawokondedwawamoyowangam’manjamwa adaniake.
8Cholowachangachilikwainengatimkangowa m’nkhalango;Chifuuliramonditsutsa:chifukwachake ndadananacho.
9Cholowachangachilikwainengatimbalame yamathothomathotho,mbalamezomuzungulira mozungulira.idzani,sonkhanitsanizilombozonseza kuthengo,idzadyani
10Abusaambiriaonongamundawangawamphesa, aponderezagawolanga;
11Iwoausandutsabwinja,ndipopokhalabwinjaandilira maliro;dzikolonselasandukabwinja,chifukwapalibe munthuwosamalira.
12Ofunkhaafikiramisanjeyonsem’cipululu;
13Afesatirigu,komaadzatutaminga;adzipwetekaokha, komaosapindulakanthu;
14AteroYehovazaanansiangaonseoipa,ameneakhudza cholowachimenendapatsaanthuangaIsraele;Taonani, ndidzawakwatulam’dzikolawo,ndikuzulanyumbaya Yudapakatipao
15Ndipopadzakhala,nditawazula,ndidzabwerera,ndi kuwachitirachifundo,ndikuwabwezera,yensekucholowa chake,ndiyensekudzikolake
16Ndipopadzakhala,akadzaphunziramwakhamanjiraza anthuanga,kulumbiram’dzinalanga,Yehovaalimoyo; mongaanaphunzitsaanthuangakulumbirapaBaala; pamenepoadzamangidwapakatipaanthuanga
17Komaakapandakumvera,ndidzazulamtunduumenewo ndikuuwononga,”+wateroYehova
MUTU13
1AteroYehovakwaine,Pita,udzitengerelambawabafuta, nudzimangem’chuunomwako,osauikam’madzi
2Pamenepondinatengalambamongamwamawua Yehova,ndikuumangam’chiunomwanga.
3NdipomauaYehovaanadzakwainekachiwiri,kuti,
4Tengalambaumeneunagula,umeneulim’chiuno mwako,nuwuke,nupitekuFirate,nuubisem’phangala thanthwe
5ChoterondinapitandikukaubisakuFirate,monga mmeneYehovaanandilamulira.
6Patapitamasikuambiri,Yehovaanandiuzakuti: “Nyamuka,pitakuFirate,ukatengelambaamene ndinakuuzakutiukabisekumeneko.
7PamenepondinamukakuFirate,ndikukumba,ndi kutengalambam’malom’menendinaubisa;
8PamenepomauaYehovaanadzakwaine,kuti, +9Yehovawanenakuti,‘Moterendidzawonongakunyada kwaYuda+ndikunyadakwakukulukwaYerusalemu.
10Anthuoipaawa,ameneakanakumvamawuanga,+ ameneakuyendamukuumirirakwamitimayawo+ndi kutsatiramilunguina+ndikuitumikirandikuigwadira,+ adzakhalangatilambauyuwosathandiza
11Pakutimongalambaamamatiram’chuunomwa mwamuna,momwemonsondamamatirakwainenyumba yonseyaIsrayelindinyumbayonseyaYuda,’watero Yehova;kutiakhalekwaInekwaanthu,ndidzina,ndi matamando,ndiulemerero:komasanamvera.
12Cifukwacaceuzinenanaomauawa;AteroYehova MulunguwaIsrayeli,Botololililonselidzadzazidwandi vinyo;
+13Ukawauzekuti,‘Yehovawanenakuti,‘Taonani, ndidzaledzeretsaanthuonseokhalam’dzikolino,mafumu okhalapampandowachifumuwaDavide,+ansembe, aneneri,+ndionseokhalamuYerusalemu 14Ndipondidzawaphwanyawinandimnzake,atatendi anapamodzi,atiYehova;
15Imvani,tcheranikhutu;musadzikuza;pakutiYehova wanena
16LemekezaniYehovaMulunguwanu,asanadzetse mdima,ndimapazianuasanagwepamapiriamdima,ndipo, pamenemuyembekezerakuunika,iyeasandutsemthunzi waimfa,ndikuuyesamdimawandiweyani.
17Komamukapandakumvera,moyowangaudzalira m’maloobisikachifukwachakunyadakwanu;ndipodiso langalidzalirakwambiri,ndikukhetsamisozi,chifukwa zowetazaYehovazatengedwandende
18Nenanikwamfumundikwamfumukazi,Dzichepetseni, khalanipansi;pakutimaukuluanuadzatsika,koronawa ulemererowanu
19Mizindayakumweraidzatsekedwa,palibewoitsegula; Yudaadzatengedwandendewonse,adzatengedwandende. 20Kwezanimasoanu,muoneiwoakuchokerakumpoto; 21Udzanenachiyaniakakulanga?pakutimwawaphunzitsa iwoakhaleakazembe,ndiakuluanu; 22Ndipoukanenam’mtimamwako,Izizandigwera chifukwaninji?Chifukwachakuchulukakwamphulupulu zakozobvalazakozabvundukuka,zidendenezako zabvulidwa
23KodiMkusiangasinthekhungulake,kapenanyalugwe mawangaake?pamenepoinunsomuthakuchitazabwino, amenemuzolowerakuchitazoyipa
24Chifukwachakendidzawabalalitsangatichiputu chowolokandimphepoyam’chipululu
25Ichindigawolako,gawolamiyesoyakoyochokera kwaine,atiYehova;popezawandiiwalaIne,ndi kukhulupirirazonama
26Cifukwacacendidzavundukulamkanjowakopankhope pako,kutimanyaziakoaonekere.
27Ndaonazigololozako,ndikulirakwako,chigololocha chigololochako,ndizonyansazakopazitundazakuthengo. Tsokakwaiwe,Yerusalemu!sudzayeretsedwakodi? lidzakhalaliti?
MUTU14
1MauaYehovaameneanadzakwaYeremiyaponenaza cilala
2Yudaakulira,ndipozipatazakezalefuka;ndizakuda pansi;ndipokulirakwaYerusalemukwakwera.
3Ndipoakuluaoatumizaang’onoaokumadzi;anabwerera zotengerazaozopandakanthu;iwoanachitamanyazindi manyazi,naphimbamituyawo.
4Popezanthakayang’ambika,popezapanalibemvulapa dzikolapansi,olimaanachitamanyazi,naphimbamitu yawo.
5Inde,nswalayaberekansokuthengo,niyisiya,popeza kulibemsipu
6Ndipombidzi+zinaimapamalookwezeka,+ndipo zinauluzamphepongatizinjokamasoawoanakomoka, chifukwapanalibeudzu
7Yehova,ngakhalemphulupuluzathuzitichitiraumboni, chitanichifukwachadzinalanu;takuchimwirani
8Inuchiyembekezo+chaIsiraeli,+Mpulumutsiwake+ m’nthawiyansautso,+n’chifukwachiyanimukhalangati mlendom’dzikolo,+ngatimlendowopatukakutiagone usikuumodziwokha?
9Mukhalabwanjingatimunthuwodabwa,ngatimunthu wamphamvuwosakhozakupulumutsa?komainu,Yehova, mulipakatipathu,ndipoifetachedwandidzinalanu; musatisiye.
10AteroYehovakwaanthuawa,Momwemoanakonda kuyendayenda,sanaumitsamapaziao;tsopano adzakumbukiramphulupuluzao,nadzalangazolakwazao.
11PamenepoYehovaanatikwaine,Usapempherereanthu awakuwachitiraubwino
12Pameneasalakudya,sindidzamvakulirakwawo;+ Poperekansembezopsereza+ndinsembeyaufa,+ sindidzawalandira,+komandidzawathandilupanga,+ njala,+ndimliri.
13Pamenepondinati,Ha,AmbuyeYehova!taonani, anenerianenanao,simudzaonalupanga,kapenanjala; komandidzakupatsanimtenderewotsimikizirikapamalo pano
14PamenepoYehovaanatikwaine,Anenerianenera monamam’dzinalanga;sindinawatuma,sindinawalamulira, sindinanenanao;
+15ChoteroYehovawanenazaaneneriameneakulosera m’dzinalanga,+amenesindinawatume,+komaakunena kuti,‘Lupangandinjalasizidzakhalapom’dzikolino Aneneriawoadzathedwandilupangandinjala
16Ndipoanthuameneakuloseraadzatayidwam’misewu yaYerusalemuchifukwachanjalandilupanga;ndipo sadzakhalandiwakuwaika,iwo,akaziawo,kapenaana awoaamuna,kapenaanaawoaakazi:pakuti ndidzatsanulirazoipazawopaiwo
17Cifukwacaceuzinenanaomauawa;Masoanga agwetsemisoziusikundiusana,asaleke;
Yeremiya
18Ndikatulukakumunda,taonaniophedwandilupanga! ndipondikalowam’mudzi,taonani,akudwalandinjala; indemnenerindiwansembeayendayendam’dzikolimene sakulidziwa.
19KodimwakanaYudakotheratu?Kodimoyowako wanyansidwandiZiyoni?Mwatikanthabwanji,ndipo palibewotichiritsa?tinayembekezeramtendere,koma palibechabwino;ndinthawiyamachiritso,ndipotaonani masautso!
20Tikuvomerezakuipakwathu,Yehova,ndimphulupulu yamakoloathu;
21Musatidetseife,chifukwachadzinalanu,musanyoze mpandowachifumuwaulemererowanu;kumbukirani, musaphwanyepanganolanundiife
22Kodipalienamwazachabechabezaamitunduamene angagwetsemvula?Kapenakumwambakungagwetsa mvula?sindinukodi,YehovaMulunguwathu?chifukwa chaketidzayembekezeraInu:chifukwamudapangazonsezi
MUTU15
1NdipoYehovaanatikwaine,NgakhaleMosendi Samueliakaimapamasopanga,mtimawangasukanakhala paanthuawa;
2Ndipopadzakhala,akadzatikwaiwe,Tipitekuti? pamenepouzitikwaiwo,AteroYehova;Omwealiaimfa, kuimfa;ndiakuyeneralupanga,kulupanga;ndipozanjala, zanjala;ndiamenealiam'ndendekundende.
3Ndipondidzawaikiramitunduinayi,’wateroYehova: lupangalakupha,ndiagaluothyola,ndimbalameza m’mlengalenga,ndizilombozapadziko,kutizidyendi kuwononga
4Ndidzawachititsakukhalachinthuchochititsamantha m’maufumuonseapadzikolapansichifukwachaManase mwanawaHezekiyamfumuyaYuda,chifukwacha zimeneanachitakuYerusalemu
5Pakutindaniadzakuchitirachifundo,Yerusalemuiwe? Kapenaadzakulirandani?Kapenaadzapatukandani kudzafunsamulibwanji?
6Mwandisiya,atiYehova,wabwereram’mbuyo;ndatopa ndikulapa
7Ndipondidzawauluzandichouluzirapazipatazadziko; Ndidzawalandaana,ndidzaonongaanthuanga,popeza sanabwererekulekanjirazao
8Akaziawoamasiyeandichulukirakuposamchengawa kunyanja:Ndawatengerawofunkhamasanamasanandi mayiwaanyamata
9Wobalaasanundiawirialefuka;Dzuwalakelapita kukadaliusana:wachitamanyazindikuthedwanzeru; ndipootsalaawondidzaperekalupangapamasopaadani awo,atiYehova
10Tsokaine,mayiwanga,kutiwandibalainemunthu wandewundimunthuwokanganandidzikolonselapansi! sindinabwereketsakatapira,kapenaanthusandibwereka ndikatapira;komaaliyensewaiwoanditembereraine
11Yehovaanati,Zoonadikudzakhalabwinondiotsalaako; Ndithu,ndidzampembedzeramdaniwakopanthawiya zoipandim’nthawiyamasautso
12Kodichitsulochidzaphwanyachitsulochakumpotondi chitsulo?
13Chumachakondichumachakondidzaziperekakuti zifunkhidwepopandamtengowake,ndichifukwacha machimoakoonsem’malireakoonse
14Ndipondidzakupitikitsapamodzindiadaniakom’dziko limenesulidziwa,pakutiwayakamotomumkwiyowanga, umeneudzayakapainu
15InuYehova,mudziwa:mundikumbukile,nimuyendere, nimubwezerecilangokwaondisautsa;musandichotseine m’kulezamtimakwanu;
16Mawuanuanapezeka,ndipondinawadya;ndipomawu anuanalikwainechisangalalondichisangalalochamtima wanga:pakutindatchedwandidzinalanu,Yehova Mulunguwamakamu.
17Sindinakhalam’msonkhanowaonyoza,kapena kukondwera;Ndinakhalandekhachifukwachadzanjalanu: pakutimwadzazaukaliwanga.
18N’cifukwacianiululuwangaukhalilakosalekeza,+ndi balalangalosapola,+limenelikukanakuchiritsidwa?kodi mudzakhalakwaInemongawabodza,ndingatimadzi akutha?
19CifukwacaceateroYehova,Ukabwerera, ndidzakubweza,ndipoudzaimapamasopanga;komaiwe usabwererekwaiwo
20Ndipondidzakusandutsalingalamkuwalampandawa anthuawa;ndipoadzamenyanandiiwe,komasadzakulaka; pakutiInendilindiiwekutindikupulumutsendi kukulanditsa,atiYehova
21Ndidzakupulumutsam’manjamwaoipa,+ndipo ndidzakuombolam’manjamwaanthuoopsa
MUTU16
1NdipomauaYehovaanandidzeranso,kuti, 2Usadzitengeremkazi,usakhalendianaamunakapena akazipano
+3PakutiYehovawanenazaanaaamunandiaakazi obadwam’maloano,+amayiawoameneanawabereka,+ ndizamakoloawoameneanawaberekeram’dzikolino,+4 kuti:
4Adzafandiimfazowawa;sadzalira;kapenasadzaikidwa; komaadzakhalangatindowepankhopepadzikolapansi: ndipoadzathedwandilupanga,ndinjala;ndimitembo yawoidzakhalachakudyachambalamezam’mlengalenga, ndichazirombozapadziko
5PakutiYehovawanenakuti:“Usalowem’nyumbaya maliro,+usapitekukawaliramaliro+kapenakuwalirira maliro,+pakutindachotsamtenderewangapaanthuawa, +kukomamtimakosathandichifundo+kwaanthuawa,” +wateroYehova
6Akulundiang’onoadzafam’dzikomuno;
7Anthusadzawang’ambachifukwachakulirakwawo,kuti awatonthozechifukwachaakufa;kapenaanthu sadzawapatsachikhochotonthozamtimachawokutiamwe chifukwachaatatewawokapenaamayiawo
8Iwensousalowem’nyumbayamadyerero,kukhalapansi ndikudyandikumwa
9PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Taonani,ndidzaletsam’malomunopamasopanu,ndi m’masikuanu,liwulachisangalalo,liwulachisangalalo, liwulamkwati,ndimawuamkwatibwi.
10Ndipopadzakhala,pameneudzauzaanthuawamawu onsewa,ndipoiwoadzatikwaiwe,ChifukwaninjiYehova
Yeremiya waneneraifechoipachachikuluichi?kapenamphulupulu yathundiyotani?+kapenatchimolathun’lotanilimene tamchimwiraYehovaMulunguwathu?
11Pamenepouzitikwaiwo,Chifukwamakoloanu anandisiya,atiYehova,natsatamilunguina,naitumikira, ndikuigwadira,ndikundisiyaIne,osasungachilamulo changa;
12Ndipoinumwachitazoipakoposamakoloanu;pakuti, taonani,muyendayensemongamwakuumirirakwamtima wakewoipa,kutiangandimvereIne;
13Cifukwacacendidzakutulutsanim’dzikolino,ndi kukulowetsanim’dzikolimenesimukulidziwa,inukapena makoloanu;pamenepomuzitumikiramilunguinausana ndiusiku;kumenesindidzakukomeranimtima
14Cifukwacace,taonani,masikuakudza,atiYehova, amenesadzanenanso,PaliYehova,ameneanaturutsaanaa Israyelim’dzikolaAigupto;
15Koma,PaliYehova,ameneanakwezaanaaIsrayeli kucokerakudzikolakumpoto,ndim’maikoonsekumene anawaingitsirako,ndipondidzawabwezerakudzikolao limenendinapatsamakoloao
16Taonani,ndidzaitanaasodziambiri,atiYehova,ndipo iwoadzawapha;ndipopambuyopakendidzaitanaasaka nyamaambiri,ndipoadzazisakam’phirilililonse,ndi m’zitundazonse,ndim’maenjeamatanthwe.
17Pakutimasoangaalipanjirazaozonse;
18Ndipopoyambandidzabwezeramphulupuluyaondi tchimolawokawiri;popezaanaipitsadzikolanga,nadzaza cholowachangandimitemboyazonyansazaondi zonyansazao
19Yehova,mphamvuyanga,lingalanga,pothawirapo pangatsikulamasautso,amitunduadzadzakwaInu kuchokerakumalekezeroadzikolapansi,nadzati,Zoonadi makoloathuanalandiramabodza,zachabe,ndizinthu zopandaphindu
20Kodimunthuangadzipangiremilungu,komasimilungu?
21Chifukwachake,taonani,ndidzawadziwitsanthawiiyi, ndidzawadziwitsadzanjalangandimphamvuyanga;ndipo adzadziwakutidzinalangandineYehova
MUTU17
1TchimolaYudalalembedwandicholemberachachitsulo, ndinsongayadiamondi;
+2Pameneanaawoamakumbukiramaguwaawoansembe +ndimizatiyawoyopatulika+pafupindimitengoyaiwisi pamapiriaatali
3Iwephirilangalam’munda,ndidzaperekacumacakondi cumacakozonsekufunkhidwe,ndimisanjeyakocifukwa cakucimwa,m’malireakoonse
4Ndipoinunokha,mudzalekacholowachanuchimene ndinakupatsani;ndipondidzakutumikiraniadanianu m’dzikolimenesimulidziwa;
5AteroYehova;Wotembereredwamunthuamene akhulupiriramunthu,ameneapangathupilamunthudzanja lake,amenemtimawakeuchokakwaYehova
6Pakutiadzakhalangatichitsambacham’chipululu,ndipo sadzawonapakudzazabwino;komaadzakhalam’malo oumam’cipululu,m’dzikolamcherelosakhalamoanthu
7WodalandimunthuameneakhulupiriraYehova,amene chiyembekezochakendiYehova
8Pakutiadzakhalangatimtengowobzalidwam’mphepete mwamadzi,wotambasuliramizuyakekumtsinje,wosaona kutenthakumabwera,komatsambalakelidzakhalalaliwisi; ndiposudzasamalam’chakachachilala,kapenakuleka kubalazipatso.
9Mtimandiwowonyengakoposa,ndiwosachiritsika: ndaniangaudziwe?
10IneYehovandisanthulamtima,ndiyesaimpso,kuti ndipatsemunthuyensemongamwanjirazace,ndimonga zipatsozanchitozace
11Mongankhwaliikhaliramazira,osawaswa;koteroiye ameneapezachuma,osatimwachilungamo,adzazisiya pakatipamasikuake,ndipopamapetopakeadzakhala chitsiru
12Maloamaloathuopatulikandimpandowachifumu wautaliwaulemererokuyambirapachiyambi.
13InuYehova,chiyembekezochaIsiraeli,onseamene akusiyaniadzachitamanyazi,+ndipoiwoameneachoka kwaineadzalembedwam’dziko,+chifukwachakuti anasiyaYehova,+kasupewamadziamoyo
14Ndichiritseni,Yehova,ndipondidzachiritsidwa; ndipulumutseni,ndipondidzapulumutsidwa:pakuti ulemererowangandinu
15Taonani,akutikwaine,MauaYehovaalikuti?libwere tsopano.
16Komaine,sindinafulumirekukhalambusakukutsatani; udziwa:choturukam'milomoyangachinalipamasopako
17Musakhalewondiwopsaine:Inundinuchiyembekezo changatsikulatsoka
18Achitemanyaziiwoameneakundizunza,komaine ndisachitemanyazi:iwoaopsedwe,komainendisachite mantha;
19Yehovaanatikwaine;Mukani,nimuimepacipataca anaaanthu,m’menealowamomafumuaYuda,ndi poturukanalo,ndim’zipatazonsezaYerusalemu; +20Ukawauzekuti,‘ImvanimawuaYehovainumafumu aYuda,inuAyudaonse,ndiinunonseokhalamu Yerusalemu,amenemumalowapazipataizi
21AteroYehova;Chenjerani,musanyamulekatundutsiku lasabata,kapenakulowanawopazipatazaYerusalemu; 22Musaturutseakatundum’nyumbazanupatsikula sabata,kapenakugwirantchitoiriyonse,komamuzipatula tsikulasabata,mongandinalamuliramakoloanu.
23Komasanamvera,kapenakutcherakhutu,koma anaumitsakhosilawo,kutiangamve,kapenakulandira mwambo.
24Ndipokudzakhala,mukandimveraine,atiYehova, osalowetsakatundupazipatazamudziunopatsikula sabata,komakuyeretsatsikulasabata,osagwirantchito iliyonse;
25Pamenepopadzalowapazipatazamudziuwumafumu ndiakalongaokhalapampandowachifumuwaDavide, okwerapamagaletandipaakavalo,iwo,ndiakalongaawo, amunaaYuda,ndiokhalam’Yerusalemu;
26Ndipoiwoadzachokeram’mizindayaYuda,ndi m’maloozunguliraYerusalemu,ndikudzikolaBenjamini, ndikuchigwa,ndikumapiri,ndikumwera,nadzandi nsembezopsereza,ndizophera,ndinsembezaufa,ndi zofukiza,ndikudzanazonsembezoyamikakunyumbaya Yehova.
27Komangatisimudzandimverainekuyeretsatsikula sabata,ndikusasenzakatundu,ndikulowapazipataza
Yeremiya
Yerusalemupatsikulasabata;pamenepondidzasonkha motopazipatazace,ndipoudzanyeketsanyumbazacifumu zaYerusalemu,ndiposudzazimitsidwa
MUTU18
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova, kuti,
2Nyamuka,tsikirakunyumbayawoumbambiya,ndipo kumenekondidzakudziwitsamawuanga
3Pamenepondinatsikirakunyumbayawoumbambiya, ndipo,taonani,wakugwirantchitopamawilo
4Chiwiyachimeneanaumbandidongochinawonongeka m’manjamwawoumbambiya,ndipoanachipanganso mbiyaina,+mongammenewoumbayoanakonderakuti achipange.
5PamenepomauaYehovaanadzakwaine,kuti, 6InunyumbayaIsrayeli,kodisindingathekuchitandiinu mongawoumbauyu?ateroYehova.Taonani,monga dongolirim’dzanjalawoumba,momwemomulim’dzanja langa,inunyumbayaIsrayeli
7Nthawiyomweyondidzanenazamtundu,ndiufumu, kuuzula,kuugwetsa,ndikuuononga;
8Mtunduumenendaunenerawoukatembenukakusiya zoipazawo,ndidzalekazoipazimenendinaganizakuti ndiwachitire
9Ndiponthawiyomweyondidzanenazamtunduwaanthu, ndizaufumu,kuumangandikuuoka;
10Chikachitachoipapamasopanga,osamveramawuanga, ndidzalekachabwinochimenendinatindidzachichitira
11TsopanolankhulandiamunaaYudandiokhalamu Yerusalemu,kuti,AteroYehova;Taonani,ndikupangirani inucoipa,ndipangirainuciwembu;
12Ndipoiwoanati,Palibechiyembekezo; 13CifukwacaceateroYehova;Funsanitsopanomwa amitundu,ndaniwamvazotere?
14KodimunthuadzasiyachipalechofewachakuLebano chochokeram’thanthwelakuthengo?Kapenamadzi oziziraoyendaakuchokerakwinaadzalekeka?
15Popezaanthuangaandiiwala,+afukizirazachabechabe +zofukiza,+ndipoawapunthwitsa+m’njirazawopanjira zakale,+kutiayendem’njira,m’njirayosakonzedwanso
16Kusandutsadzikolaobwinja,ndichotsonyetsakosatha; aliyensewodutsapoadzadabwa,ndikupukusamutuwake
17Ndidzabalalitsapamasopaadaningatimphepoya kum'mawa;Ndidzawaonetsamsana,osatinkhope,tsikula tsokalawo
18Pamenepoanati,Tiyeni,tikonzeremaerepaYeremiya; pakutichilamulosichidzatayikakwawansembe,kapena uphungukwawanzeru,kapenamawukwamneneriTiyeni timumenyanendililime,ndipotisamveremawuake aliwonse.
19Ndimvereni,Yehova,ndikumveramawuaiwo akutsutsananane
20Kodizoipazidzabwezedwam’malomwazabwino? pakutianakumbadzenjemoyowangaKumbukiranikuti ndinaimapamasopanukuwanenerazabwino,ndi kuwachotseraukaliwanu
21Cifukwacaceperekanianaaokunjala,ndikuwathira mwaziwaondimphamvuyalupanga;ndipoakaziao aphedweana,nakhaleamasiye;ndipoamunaawoaphedwe; anyamataaoaphedwendilupangakunkhondo
22Kulirakumvekem’nyumbazawo,pamene muwabweretserakhamumwadzidzidzi; 23KomainuYehova,mudziwauphunguwaowonse wondipangirainekundipha;muwachitirechoteropanthawi yamkwiyowanu.
MUTU19
1AteroYehova,Muka,nutengensupayawoumba, nutengeakuluaanthu,ndiakuluaansembe; 2NdipotulukakuchigwachamwanawaHinomu, chimenechiripakhomolachipatachakum’mawa, nulalikirekumenekomawuamenendidzakuuza; +3Unenekuti,‘ImvanimawuaYehovainumafumua YudandiinuokhalamuYerusalemuAteroYehovawa makamu,MulunguwaIsrayeli;taonani,ndidzatengera coipapamaloano,cimenealiyensewakumvamakutuake adzanjenjemera
+4Chifukwaanandisiya+ndikuchititsamaloanokukhala achilendo+ndikufukizaponsembezautsi+kwamilungu ina,+imeneiwokapenamakoloawokapenamafumua Yudasanaidziwe,+ndipomaloanoadzazandimagazia anthuosalakwa
+5IwoamangansomalookwezekaaBaala+kutiatenthe anaawoaamuna+pamotokutiakhalensembezopsereza zaBaala,+zimenesindinawalamule,kapenakuzinena, zimenesindinaziganizire
6Chifukwachake,taonani,masikuakudza,atiYehova, pamenemaloanosadzatchedwansoTofeti,kapenaChigwa chamwanawaHinomu,komaChigwachakupha
7NdipondidzathetsauphunguwaYudandiwa Yerusalemum’malomuno;+Ndidzawagwetsandilupanga pamasopaadaniawo+ndim’manjamwaanthuamene akufunafunamoyowawo,+ndipomitemboyawo ndidzaiperekakutiikhalechakudyachambalameza m’mlengalengandizilombozapadziko
8Ndipondidzasandutsamudziunobwinja,ndi chotsonyetsa;aliyensewodutsapoadzadabwandikuchita mluzichifukwachamiliriyakeyonse
9Ndipondidzawadyanyamayaanaawoaamunandiana awoaakazi,ndipoaliyenseadzadyanyamayamnzake m’malootchingidwandiadaniawondiameneakufuna moyowawoadzawasautsa.
10Pamenepouthyolebotolopamasopaamunaamene akupitanawe;
11Ndipouwauzekuti,AteroYehovawamakamu; Momwemondidzathyolaanthuawandimudziuwu,monga munthuathyolambiyayawoumba,yosatha kukonzedwanso;
12Ndidzachitiramaloanondianthuokhalamo,+ndipo ndidzasandutsamzindauwungatiTofeti
13NdiponyumbazaYerusalemu,ndinyumbazamafumu aYuda,zidzadetsedwangatimaloaTofeti,+chifukwacha nyumbazonsezimenepamadengaakeanafukizirapo nsembezautsi+kwakhamulonselakumwamba+ndi kuthiransembezachakumwakwamilunguina
14PamenepoYeremiyaanachokerakuTofeti,kumene Yehovaanamtumakulosera;naimam’bwalolanyumbaya Yehova;natikwaanthuonse,
15AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Taonani,ndidzatengeramudziuwu,ndimidziyakeyonse
Yeremiya zoipazonsendinaunenera,popezaanaumitsamakosiao, kutiangamvemauanga.
MUTU20
1NdipoPasurimwanawaImeriwansembe,ndiye kazembewamkulum'nyumbayaYehova,anamvakuti Yeremiyaakuloserazinthuizi.
2PamenepoPasurianakanthamneneriYeremiya,+ndi kum’tsekeram’matangadza+ameneanalipaChipata ChapamwambachaBenjamini,+chimenechinalipafupi ndinyumbayaYehova
3Ndipokunalim’mawamwake,kutiPasurianatulutsa Yeremiyam’matangadzaPamenepoYeremiyaanatikwa iye,YehovasanakutchadzinalakoPasuri,koma Magormisabibu.
4PakutiateroYehova,Taonani,ndidzakuyesaiwe chowopsakwaiwewekha,ndikwamabwenziakoonse; ndipoadzagwandilupangalaadaniao,ndimasoako adzaona;ndipondidzaperekaYudayensem’dzanjala mfumuyakuBabulo,ndipoiyeadzawatengerandendeku Babulo,ndikuwaphandilupanga.
5Ndidzaperekansomphamvuzonsezamzindauno,ndi zolemetsazakezonse,ndizinthuzakezonsezamtengo wapatali,ndichumachonsechamafumuaYuda, ndidzaperekam’manjamwaadaniawo,amene adzawafunkha,ndikuwalanda,n’kupitanawokuBabulo 6Ndipoiwe,Pasuri,ndionseokhalam’nyumbamwako mudzankakundende;ndipomudzafikakuBabulo, n’kukaferakomweko,ndikuikidwakomweko,iwendi mabwenziakoonse,ameneunawaneneramonama.
7Yehova,mwandinyengaine,ndipondinanyengedwa;
8Pakutipamenendinalankhula,ndinapfuula,ndinapfuula ciwawandikufunkha;+chifukwamawuaYehova anasandukachitonzokwaine+ndichoseketsatsikundi tsiku
9Pamenepondinati,Sindidzamtchulaiye,sindidzanenanso m’dzinalake;Komamauacem’mtimamwangaanalingati motowotenthawotsekedwam’mafupaanga;
10Pakutindinamvamatonzoaambiri,manthaponsepo; Nenani,atero,ndipotidzanenaAnzangaonse akuyang'anirakugwakwanga,ndikuti,Kapena angakopeke,ndipotidzamlaka,ndipotidzabwezeracilango paiye
11KomaYehovaalindiinengatiwamphamvuwoopsa; pakutisadzachitamwanzeru:chitonzochawochosatha sichidzaiwalika
12Koma,Yehovawamakamu,amenemumayesa olungama,ndiwakuonaimpsondimtima,ndilolenindione kubwezerakwanupaiwo;pakutindakutseguliranimlandu wanga
13ImbiraniYehova,lemekezaniYehova; 14Litembereredwetsikulimenendinabadwa:Lidalitsike tsikulimeneamayiangaanandibalira
15Atembereredwemunthuameneanatengeramaukwa atatewanga,kuti,Wakubadwiranimwanawamwamuna; kumusangalatsakwambiri.
+16MunthuameneyoakhalengatimizindaimeneYehova anapasula,+osalapa,+ndipoamvekuliram’mawandi kufuulamasana;
17Popezasanandiphainem’mimba;kapenakutimai wangaakadakhalamandaanga,ndimimbayaceikhalendi inenthawizonse
18N’chifukwachiyanindinatulukam’mimbakutindione ntchitoyovutitsandichisoni,kutimasikuangaathendi manyazi?
MUTU21
1MauameneanadzakwaYeremiyaocokerakwaYehova, pamenemfumuZedekiyaanatumizakwaiyePasurimwana waMelikiya,ndiZefaniyamwanawaMaaseyawansembe, kuti,
2UtifunsirekwaYehova;pakutiNebukadirezaramfumu yaBabuloacitankhondonafe;kapenakutiYehova adzatichitiramongamwazodabwizazakezonse,kuti akwerekuticokera
3PamenepoYeremiyaanawauzakuti:“MukauzeZedekiya kuti:
4AteroYehovaMulunguwaIsrayeli;Taonani, ndidzabwezazidazankhondozirim'manjamwanu,zimene mumenyananazondimfumuyakuBabulo,ndiAkasidi, ameneakuzinganikunjakwamalinga,ndipo ndidzawasonkhanitsapakatipamudziuno
5Ndipoinendidzamenyanananundidzanjalotambasuka, ndimkonowamphamvu,ndimkwiyo,ndiukali,ndiukali waukulu
6Ndipondidzakanthaokhalam’mudziuno,anthundi nyama:adzafandimliriwaukulu
7Ndipopambuyopake,atiYehova,ndidzapereka ZedekiyamfumuyaYuda,ndiatumikiake,ndianthu,ndi otsalam’mudziunokumliri,kulupanga,ndikunjala, m’dzanjalaNebukadirezaramfumuyakuBabulo,ndi m’dzanjalaadaniao,ndim’dzanjalaiwoakufunamoyo wao;ndipoiyeadzawaphandilupanga;sadzawalekerera, kapenakuwachitirachifundo,kapenakuwachitirachifundo 8Ndipokwaanthuawauziti,AteroYehova;Taonani, ndaikapamasopanunjirayamoyo,ndinjirayaimfa
9Wokhalamumzindaunoadzafandilupanga,+njala,+ ndimliri,+komaiyeameneatulukandikukanthakwa Akasidiameneakuzungulirainu,adzakhalandimoyo,+ ndipomoyowakeudzakhalawofunkha
10Pakutinkhopeyangayalunjikapamudziunokuuchitira choipa,osatichabwino,atiYehova;udzaperekedwa m’dzanjalamfumuyakuBabulo,ndipoidzautenthandi moto.
11NdipoponenazanyumbayamfumuyaYuda,uti, ImvanimauaYehova;
12OnyumbayaDavide,ateroYehova;Chitanichiweruzo m'mamawa,ndikupulumutsawofunkhidwam'dzanjala wopondereza,kutiukaliwangaungatulukengatimoto,ndi kutenthaosauzima,chifukwachakuipakwazochitazanu.
13Taona,nditsutsananawe,iwewokhalam’chigwa,ndi thanthwelam’chigwa,”wateroYehova;ameneati, Adzatsikirandanikudzamenyananafe?Kapenaadzalowa ndanim'nyumbazathu?
14Komandidzakulanganimongamwazipatsoza machitidweanu,atiYehova;
1AteroYehova;TsikirakunyumbayamfumuyaYuda, nunenekumenekomauawa; +2Unenekuti,‘ImvanimawuaYehova,+inumfumuya Yuda,amenemwakhalapampandowachifumuwaDavide, inuyo,atumikianundianthuanuameneamalowapazipata izi.
3AteroYehova;Citaniciweruzondicilungamo, nimulanditsewofunkhidwam'dzanjalawotsendereza; 4Pakutimukachitaichindithu,pazipatazanyumbaiyi adzalowamafumuokhalapampandowachifumuwa Davide,okwerapamagaletandipaakavalo,iye,ndi atumikiake,ndianthuake
5Komamukapandakumveramawuawa,ndilumbirapaine ndekha,atiYehova,kutinyumbaiyiidzakhalabwinja.
6PakutiYehovawanenakwanyumbayamfumuyaYuda; IwendiweGiliyadikwaine,mutuwaLebanoni:koma ndithundidzakusandutsachipululu,ndimidziyopanda anthu
7Ndidzakukonzeraniowononga,aliyensendizidazake; 8Ndipoamitunduambiriadzadutsapafupindimudziuwu, nadzatiyensekwamnansiwake,Yehovawachitiranji choterondimzindawaukuluuwu?
9Pamenepoadzayankhakuti,Chifukwaanasiyapangano laYehovaMulunguwawo,nalambiramilunguyina,ndi kuitumikira
10Musamlirirewakufayo,kapenakumchitiracisoni;
11PakutiYehovawanenazaSalumu+mwanawaYosiya mfumuyaYuda,ameneanalowaufumum’malomwa Yosiyabamboake,+ameneanatulukam’malomuno. sadzabwereransokomweko;
12Komaiyeadzaferakumalokumeneanamtengerako ndende,ndiposadzaonansodzikoili.
13Tsokakwaiyeameneamanganyumbayakendi chosalungama,ndizipindazakemopandachilungamo; ameneatumikiramnansiwakewopandamalipiro,ndi wosamperekakuntchitoyake;
14Uyowakuti,Ndidzadzimangirainenyumbayaikulundi zipindazazikulu,ndipoadzadzichekeramazenera;ndipo amayalapondimkungudza,napakidwautotowofiira 15Kodiudzalamulira,popezaudzitsekerezapamikungudza? Kodiatatewakosanadyendikumwa,ndikuchita chiweruzondichilungamo,ndipopamenepo zidamukomera?
16Iyeanaweruzamlanduwaaumphawindiwosauka; pamenepokudakhalabwinondiiye;ateroYehova 17Komamasoakondimtimawakosizilikomapa umbombowako,ndikukhetsamwaziwosalakwa,ndi kupondereza,ndichiwawakutiuchite
18ChifukwachakeYehovawanenazaYehoyakimu mwanawaYosiyamfumuyaYuda;Sadzamliraiye,kuti, Ha,mbalewanga!kapena,Mlongo!iwosadzamliraiye, kuti,Ha!kapena,Ha,ulemererowake!
+19Iyeadzaikidwam’mandangatimmenebuluwake anakwiriridwira,ndipoadzakokedwandikuponyedwa kunjakwazipatazaYerusalemu.
20KwerakuLebanoni,ukalire;kwezamawuako m’Basana,nulireulim’makhwalala;pakutimabwenziako onseaonongeka.
21Ndinalankhulandiiwem’kukhalabwinokwako;koma unati,Sindidzamva.Awandiwomachitidweako kuyambiraubwanawako,kutisunamveramauanga 22Mphepoidzadyaabusaakoonse,ndimabwenziako adzankakundende;
23Iwewokhalam’Lebano,ameneukumangachisanja chakom’mikungudza,udzakondwerachotaninanga pamenezowawazakufikira,zowawangatizamkazi wobala!
24PaliIne,atiYehova,ngakhaleKoniyamwanawa YehoyakimumfumuyaYudaakakhalachosindikizira padzanjalangalamanja,ndikakuchotsako;
+25Ndidzakuperekanim’manjamwaanthuamene akufunamoyowanu+ndim’manjamwaanthuamene mukuwaopa,+m’manjamwaNebukadirezaramfumuya Babulo+ndim’manjamwaAkasidi.
26Ndipondidzakuponyerakunjaiwe,ndiamakoamene anakubala,kunkakudzikolina,kumeneinu simunabadwira;ndipomudzaferakomweko.
27Komakudzikolimeneafunakubwererako, sadzabwererako
28KodimunthuuyuKoniyandifanoloswekalonyozeka? Iyendiyechotengerachosakondweretsa?Chifukwachiyani atayidwakunja,iyendimbumbayake,naponyedwa kudzikolimeneiwosalidziwa?
29Iwedzikolapansi,dzikolapansi,dzikolapansi,imva mawuaYehova
30Yehovawanenakuti,‘Lembanikutimunthuuyualibe ana,+munthuamenesadzachitabwinom’masikuake,+ pakutipalibealiyensewam’mbewuzake+amene adzachitezinthumwanzeru,+wokhalapampando wachifumuwaDavide+ndikulamuliransoYuda
MUTU23
1Tsokakwaabusaameneawonongandikubalalitsa nkhosazapabusapanga!ateroYehova.
2CifukwacaceateroYehovaMulunguwaIsrayeli motsutsanandiabusaakudyetsaanthuanga;Mwamwaza nkhosazanga,ndikuziingitsa,osazifikira;
3Ndipondidzasonkhanitsaotsalaankhosazangam’maiko onsekumenendinaziingitsirako,ndipondidzazibwezanso kumakolaawo;ndipoadzabalanachuluka.
4Ndidzaziikiraabusaameneadzazidyetsa,ndipo sizidzaopanso,kapenakuchitamantha,ndiposizidzasowa,” +wateroYehova.
5Taonani,masikuadza,atiYehova,pamene ndidzamuukitsiraDavideNthambiyolungama,ndipo Mfumuidzalamulirandikuchitazinthumwanzeru,ndipo idzachitachilungamondichilungamopadzikolapansi
6M’masikuaceYudaadzapulumutsidwa,ndipoIsrayeli adzakhalamwabata;
7Chifukwachake,taonani,masikuakudza,atiYehova, amenesadzanenanso,PaliYehova,ameneanatulutsaanaa Israyelim’dzikolaAigupto;
8Koma,PaliYehova,ameneanakwezandikutsogolera mbeuyanyumbayaIsrayelikucokerakudzikolakumpoto, ndim’maikoonsekumenendinawapitikitsirako;ndipo adzakhalam’dzikolao
9Mtimawangawaswekam’katimwangachifukwacha aneneri;mafupaangaonseagwedezeka;Inendiringati munthuwoledzera,ndiponsongatimunthuamene
Yeremiya
wagonjetsedwandivinyo,chifukwachaYehova,ndi chifukwachamawuakeoyera.
10Pakutidzikoladzalandiachigololo;pakutichifukwa chakulumbiradzikolikulira;malookomaam’cipululu aphwa,ndinjirayaonjoipa,ndimphamvuyaosi yolungama
11Pakutimnenerindiwansembeonseaipitsa;+inde, m’nyumbamwangandapezamokuipakwawo,”+watero Yehova
12Cifukwacacenjirayaoidzakhalakwaiwongatinjira zotereramumdima;adzakankhidwandikugwam’menemo; pakutindidzawatengeracoipa,cakacakuwalanga,’watero Yehova.
13NdipondaonazopusamwaaneneriakuSamariya; ananeneramwaBaala,nasokeretsaanthuangaAisrayeli
14NdaonansomwaaneneriakuYerusalemuchinthu chonyansa:achitachigololo,nayendam’mabodza; 15CifukwacaceateroYehovawamakamuzaaneneriwo; Taonani,ndidzawadyetsachivumulo,ndikuwamwetsa madziandulu;
16Yehovawamakamuatero,Musamveremawuaaneneri ameneakuloserakwainu;
17Anenabekwaiwoakundipeputsa,Yehovawanena, Mudzakhalandimtendere;ndipoamatikwayense wakuyendam’kuunikakwamtimawakewaiyeyekha, Choipasichidzakugwerani
18PakutindaniwaimamuuphunguwaYehova, nazindikirandikumvamawuake?ndaniadasungamawu ake,namva?
19Taonani,kamvuluvuluwaYehovawatulukamwaukali, ngakhalemphepoyamkunthoyoopsa;
20MkwiyowaYehovasudzabwerera,kufikiraatachita, ndikufikiraatachitazolingalirazamtimawake;
21Sindinatumizaaneneriawa,komaadathamanga;
22Komaakadaimamuuphunguwanga,ndikumveketsa anthuangamawuanga,akanawatembenuzakulekanjira zawozoipa,ndizoipazamachitidweawo.
23KodiinendineMulunguwapafupi,atiYehova,osati Mulunguwakutali?
24Kodialipoameneangabisalem’maloobisikakutiine ndisamuone?ateroYehovaKodisindidzazakumwamba ndidzikolapansi?ateroYehova
25Ndamvazimeneaneneriakunena,akuloseramonama m’dzinalanga,kuti,ndalota,ndalota
26Kodizimenezizidzakhalamumtimamwaaneneri ameneakuloseramonamampakaliti?inde,alianeneri achinyengochamitimayawo;
+27Iwoakuganizakutiadzaiwalitsaanthuanga+dzina langandimalotoawoameneamauzaaliyensekwamnzake, +mongammenemakoloawoanaiwaladzinalanga chifukwachaBaala
28Mneneriamenealinalolotoaneneloto;ndipoiye amenealinawomawuanga,alankhulemawuanga mokhulupirikaKodimankhusundichiyanikwatirigu? ateroYehova
29Kodimawuangasalingatimoto?ateroYehova;ndi monganyundoyothyolathanthwe?
30Chifukwachake,taonani,nditsutsanandianeneri,ati Yehova,ameneamabamawuanga,yensekwamnansi wake.
31Taonani,nditsutsanandianeneri,atiYehova,amene amalankhulamalilimeawo,nati,Atero
32Taonani,nditsutsanandiiwoakuneneramalotoonama, ndikuwafotokozera,ndikulakwitsaanthuangandi mabodzaawo,ndikupeputsakwawo;komasindinawatuma, kapenakuwauza;cifukwacacesadzapindulaanthuawa konse,atiYehova.
33Ndipoanthuawa,kapenamneneri,kapenawansembe, akakufunsa,kuti,KatunduwaYehovanchiyani?ndipo udzatikwaiwo,Katunduwanji?+Inensondidzakusiyani,” +wateroYehova
34Komamneneri,ndiwansembe,ndianthu,ameneadzati, KatunduwaYehova,ndidzalangamunthuyondinyumba yake
35Muziteroyensekwamnansiwake,ndiyensekwambale wake,Yehovawayankhakutichiyani?ndipoYehova wanenachiyani?
36KatunduwaYehovamusadzatchulenso,pakutimawua munthualiyenseadzakhalakatunduwake;pakuti mwapotozamauaMulunguwamoyo,Yehovawamakamu, Mulunguwathu.
37Ukaterokwamneneriyo,Yehovawakuyankhachiyani? ndipoYehovawanenachiyani?
38Komapopezamukuti,KatunduwaYehova;chifukwa chakeateroYehova;Pakutimukunenamauawa,Katundu waYehova;
39Cifukwacace,taonani,Ine,Inetu,ndidzakuiwalaniinu ndithu,ndipondidzakusiyaniinu,ndimudziumene ndinakupatsaniinundimakoloanu,ndikukutayanipamaso panga;
40Ndidzabweretsapainuchitonzochosatha,ndimanyazi osatha,amenesadzaiwalika
MUTU24
1Yehovaanandionetsa,ndipo,taonani,madenguawiria nkhuyuanaikidwakukachisiwaYehova,atatenga NebukadirezaramfumuyakuBabulom’ndendeYekoniya mwanawaYehoyakimumfumuyaYuda,ndiakalongaa Yuda,ndiamisiriamatabwandiosulakuYerusalemu, napitanawokuBabulo
2Mtangawinaunalindinkhuyuzabwinondithu,ngati nkhuyuzoyambakupsa;
3NdipoYehovaanatikwaine,Uonaciani,Yeremiya? Ndipondinati,Nkhuyu;nkhuyuzabwino,zabwinondithu; ndipozoipa,zoipandithu,zosadyedwa,nzoipakwambiri 4MawuaYehovaanadzansokwaine,kuti,
5AteroYehova,MulunguwaIsrayeli;Mongankhuyu zabwinoizi,momwemondidzavomerezaiwootengedwa ndendeaYuda,amenendinawatulutsam’malomuno kumkakudzikolaAkasidi,kuwachitiraubwino
6Pakutindidzayang’anapaiwokuwachitirazabwino, ndipondidzawabwezerakudzikolino;ndipo ndidzawabzala,osawazula.
7NdidzawapatsamtimawodziwakutiinendineYehova,+ ndipoiwoadzakhalaanthuanga,+ndipoinendidzakhala Mulunguwawo,+pakutiadzabwererakwainendimtima wawowonse
8Ndipomongankhuyuzoipa,zosadyedwa,zirizoipa; ndithu,ateroYehova,MomwemondidzapatsaZedekiya mfumuyaYuda,ndiakalongaake,ndiotsalaa Yerusalemu,otsalam’dzikolino,ndiiwookhalam’dziko laAigupto;
9Ndipondidzawaperekaakhalechinthuchoopsetsa m’maufumuonseadzikolapansi,chitonzo,ndimwambi, ndichitonzo,ndichitemberero,kulikonsekumene ndidzawaingitsira.
10Ndipondidzawatumiziralupanga,njala,ndimliri, kufikiraatatham’dzikolimenendinapatsaiwondimakolo ao
MUTU25
1MauameneanadzakwaYeremiyaponenazaanthuonse aYudam’chakachachinayichaYehoyakimumwanawa YosiyamfumuyaYuda,ndichochakachoyambacha NebukadirezaramfumuyaBabulo;
2YeremiyamnenerianauzaanthuonseaYuda,ndionse okhalamuYerusalemu,kuti:
3Kuyambiram’chakachakhumindichitatu+chaYosiya +mwanawaAmoni,mfumuyaYuda,+mpakalero, ndichochakachamakumiawirindizitatu,+mawua Yehovaanandidzera+ndipondinalankhulandiinu,+ kudzukam’mamawandikulankhulakomasimunamvera 4NdipoYehovawatumizakwainuatumikiakeonse aneneri,kuukamamawandikuwatumiza;koma simunamvera,kapenakutcherakhutulanukutimumve
+5Iwoanati:“Bwereranitsopanoaliyensekusiyanjira yakeyoipa+ndikuipakwazochitazanu+ndipomukhale m’dzikolimeneYehovaanakupatsaniinundimakoloanu mpakakalekale.
6Ndipomusatsatemilunguinandikuitumikira,ndi kuigwadira,ndikusautsamkwiyowangandintchitoza manjaanu;ndiposindidzakuchitiranichoipa.
7Komasimunandimvera,atiYehova;kutimundikwiyitse ndintchitozamanjaanu,kudzipwetekanokha
8CifukwacaceateroYehovawamakamu;popeza simunamvamauanga;
9Taonani,ndidzatumizandikutengamabanjaonsea kumpoto,atiYehova,ndiNebukadirezaramfumuyaku Babulo,mtumikiwanga,ndipondidzawatengerapadziko lino,ndiokhalamo,ndiamitunduonseozungulira,ndi kuwaonongakonse,ndikuwasandutsachodabwitsa,ndi chotsonyetsa,ndimabwinjakosatha
10Ndipondidzachotsakwaiwomawuachisangalalo,ndi mawuakukondwera,mawuamkwati,ndimawua mkwatibwi,mawuamphero,ndikuwalakwanyali
11Ndipodzikolonselilidzakhalabwinja,ndichodabwitsa; ndipomitunduiyiidzatumikiramfumuyakuBabulozaka makumiasanundiawiri
12Ndipokudzachitikazaka70zikadzatha,ndidzalanga mfumuyaBabulondimtunduumenewo,’wateroYehova, chifukwachamphulupuluyawo,+ndidzikolaAkasidi,+ ndipondidzalisandutsamabwinjampakakalekale
13Ndipondidzatengeradzikolimenelomawuangaonse amenendalankhulamotsutsananalo,zonsezolembedwa m’bukuili,zimeneYeremiyawaneneramitunduyonse
14Pakutimitunduyambirindimafumuaakulu adzatumikiraiwookha,ndipondidzawabwezeramonga mwantchitozawo,ndimongamwantchitozamanjaawo. 15PakutiateroYehovaMulunguwaIsrayelikwaine; Tengachikhochavinyochaukaliichim’dzanjalanga, numwetsekomitunduyonseimenendikutumizako.
16Ndipoiwoadzamwa,ndikunjenjemera,ndikuchita misala,chifukwachalupangalimenendidzatumizapakati pawo
17Pamenepondinatengachikhom’dzanjalaYehova,ndi kumwetsamitunduyonseyaanthu,imeneYehova ananditumako;
18kuYerusalemu,+mizindayaYuda,mafumuake,+ akalongaake,+kutiawapangebwinja,+chodabwitsa, cholozetsamluzi,+nditembereromongalero; 19FaraomfumuyaAigupto,ndiatumikiake,ndiakalonga ake,ndianthuakeonse; 20ndianthuosakanizaonse,ndimafumuonseadzikola Uzi,ndimafumuonseadzikolaAfilisti,ndiAsikeloni,ndi Aza,ndiEkroni,ndiotsalaaAsidodi; 21Edomu,ndiMoabu,ndianaaAmoni, 22ndimafumuonseakuTuro,ndimafumuonseaZidoni, ndimafumuam’zisumbuzakutsidyalanyanja; 23Dedani,ndiTema,ndiBuzi,ndionseokhala m’mangondyaakutali; 24ndimafumuonseaArabiya,ndimafumuonseaanthu osakanikiranaokhalam’chipululu;
25ndimafumuonseaZimiri,ndimafumuonseaElamu, ndimafumuonseaAmedi;
26Mafumuonseakumpoto,akutalindiapafupi,winandi mnzake,ndimaufumuonseadzikolapansi,okhalapadziko lapansi,ndipomfumuyaSesakiidzamwapambuyopawo 27Chonchouwauzekuti,‘Yehovawamakamu,Mulungu waIsiraeliwanena.Imwaniinu,ndikuledzera,ndi kulavula,ndikugwa,osadzukanso,chifukwachalupanga limenendidzatumizapakatipanu
28Ndipokudzali,akakanakutengachikhom’dzanjalako kutiamwe,uzitikwaiwo,AteroYehovawamakamu; mudzamwandithu
29Pakutitaonani,ndayambakutengerazoipapamudzi wochedwadzinalanga;Simudzasalangidwa,pakuti ndidzaitaniraanthuonseokhalapadzikolapansilupanga, atiYehovawamakamu.
30Cifukwacaceunenereiwomauonsewa,ndikunenanao, Yehovaadzabangulaalikumwamba,nadzamveketsamau akealim’maloakeopatulika;adzabangulamolimba pokhalapace;Iyeadzapfuula,mongaakupondamphesa, adzapfuuliraonseokhalapadzikolapansi
31Phokosolidzafikakumalekezeroadzikolapansi;pakuti Yehovaalindimlandundiamitundu,adzatsutsanandi anthuonse;+Oipaadzawaperekakulupanga,”+watero Yehova.
+32Yehovawamakamuwanenakuti,‘Taonani,choipa chidzatulukakuchokerakumtundukupitakumtunduwina, +ndipomphepoyamkuntho+idzawukakuchokera kumalekezeroadzikolapansi
33NdipoophedwaaYehovaadzakhalatsikulimenelo kuchokerakumalekezeroadzikolapansikufikira malekezeroenaadzikolapansi;adzakhalandowepanthaka 34Liraniabusainu,nimulire;+16mumadzibvinika m’phulusa,+inuolamuliraagululankhosa;ndipo mudzagwangatichotengerachokoma
35Ndipoabusaadzasowapothawira,kapenakuthawa akuruazoweta
36Mauakulirakwaabusa,ndikulirakwaakuluazoweta, adzamveka;pakutiYehovawaonongapobusapao.
37Malookhalaamtendereadzawonongedwachifukwacha mkwiyowoyakamotowaYehova
38Wasiyachobisalirachakengatimkango;pakutidziko lawolakhalabwinjachifukwachaukaliwawopondereza, ndichifukwachamkwiyowakewoopsa
MUTU26
1KuchiyambikwaufumuwaYehoyakimumwanawa YosiyamfumuyaYudakunadzamauawaochokerakwa Yehova,ndikuti,
2AteroYehova;Uimem’bwalolanyumbayaYehova, nunenendimidziyonseyaYuda,imeneikudza kudzalambiram’nyumbayaYehova,mauonseamene ndikukuuzauwanene;musachepetsemawu:
3Ngatiadzamvera,nadzatembenuka,yensekulekanjira yakeyoipa,kutindilekechoipachimenendiganiza kuwachitirachifukwachakuipakwamachitidweawo.
4Ndipouwauzekuti,AteroYehova;Mukapandakumvera Ine,kuyendam’chilamulochangachimenendaikapamaso panu;
5kumveramawuaatumikiangaaneneri,amene ndinawatumizakwainu,kudzukamamawandikuwatuma, komainusimunamvera;
6PamenepondidzayesanyumbaiyingatiSilo,ndipo ndidzayesamudziuwuchitembererokwamitunduyonse yadzikolapansi.
7Chonchoansembe,anenerindianthuonseanamva Yeremiyaakulankhulamawuamenewam’nyumbaya Yehova.
8Ndipokunali,Yeremiyaatathakunenazonsezimene Yehovaadamuuzakutianenekwaanthuonse,ansembe, ndianeneri,ndianthuonseanamgwira,ndikuti,Udzafa ndithu
9N’chifukwachiyaniunaneneram’dzinalaYehovakuti, ‘NyumbaiyiidzakhalangatiSilo,+ndipomzindauwu udzakhalabwinjalopandamunthuwokhalamo?+Anthu onseanasonkhanakutiathanendiYeremiyam’nyumbaya Yehova.
10PameneakalongaaYudaanamvazimenezi,anakwera kuchokerakunyumbayamfumukupitakunyumbaya Yehova,+ndipoanakhalapansipakhomolachipata chatsopanochanyumbayaYehova
11Pamenepoansembendianeneriananenandiakalonga ndianthuonse,ndikuti,Munthuuyuayenerakufa;pakuti waneneramudziuwu,mongamudamvandimakutuanu
12PamenepoYeremiyaanauzaakalongaonsendianthu onsekuti:“Yehovaananditumainekuneneranyumbaiyi ndimzindauwumawuonseamenemwamva
13Choterotsopanokonzaninjirazanundizochitazanu,+ ndikumveramawuaYehovaMulunguwanu;ndipo Yehovaadzalekachoipachimenewanenerainu
14Komaine,taonani,ndilim’dzanjalanu;
15Komadziwanindithu,kutimukandipha, mudzadzitengeramwaziwosalakwapainu,ndipamudzi uwu,ndipaokhalamo;
16Pamenepoakalongandianthuonseananenakwa ansembendianeneri;+Munthuuyusayenerakufa,+ chifukwawalankhulanafem’dzinalaYehovaMulungu wathu
17Pamenepoananyamukaenamwaakuluam’dziko, nanenandikhamulonselaanthu,kuti; +18MikawakuMoreti+analoseram’masikuaHezekiya mfumuyaYuda,+ndipoanauzaanthuonseakuYudakuti:
“Yehovawamakamuwanenakuti:“Yehovawamakamu wati:Ziyoniadzalimidwangatimunda,ndiYerusalemu adzakhalamiunda,ndiphirilanyumbangatimisanjeya nkhalango.
19KodiHezekiyamfumuyaYudandiAyudaonse anamupha?+KodiiyesanaopeYehova+ndi kuchondereraYehova,+ndipoYehovaanasintha maganizoakepazoipazimeneanawauza?Momwemo tingadzibweretserechoipachachikulupamiyoyoyathu +20Panalinsomunthuwinaameneanalikunenera m’dzinalaYehova,+UriyamwanawaSemayawaku Kiriyati-yearimu,+ameneananenerazamzindaunondi dzikolinomogwirizanandimawuonseaYeremiya.
+21MfumuYehoyakimu+ndiamunaakeonse amphamvu+ndiakalongaonseatamvamawuake,+ mfumuinafunakumupha.
22NdiyenomfumuYehoyakimuinatumizaanthuku Iguputo,Elinatani,mwanawaAkibori,ndiamunaenaku Iguputo.
23KenakoanatulutsaUriyakuIguputondikupitanaye kwamfumuYehoyakimuameneanamuphandilupanga, naponyamtembowakem’mandaaanthuwamba.
24KomadzanjalaAhikamumwanawaSafanilinalindi Yeremiya,kutiasamperekem’manjamwaanthukuti amuphe.
MUTU27
1KuchiyambikwaufumuwaYehoyakimumwanawa Yosiya,mfumuyaYuda,kunadzamauawakwaYeremiya ocokerakwaYehova,kuti, 2AteroYehovakwaine;udzipangirezomangirandi magoli,nuwaikepakhosipako;
3NdipoutumizekwamfumuyaEdomu,ndimfumuya Mowabu,ndimfumuyaanaaAmoni,ndimfumuyaTuro, ndimfumuyaSidoni,mwadzanjalaamithengaamene anabwerakuYerusalemukwaZedekiyamfumuyaYuda; 4Ndipouwauzekutiakauzeambuyeawo,AteroYehova wamakamu,MulunguwaIsrayeli;Muziterokwaambuye anu;
5Inendapangadzikolapansi,munthundichilombozili padziko,ndimphamvuyangayayikulundimkonowanga wotambasula,ndipondaziperekakwaiwoamene ndidafuna
6Tsopanondaperekamaikoonsewam’manjamwa NebukadinezaramfumuyaBabulo,+mtumikiwanga;ndi nyamazakuthengondampatsansozimtumikire
7Ndipomitunduyonseidzamtumikiraiye,ndimwana wakewamwamuna,ndimdzukuluwake,kufikiraikafika nthawiyadzikolake;
8Ndipokudzali,kutimtundundiufumuumene sudzatumikiraNebukadinezarayemweyomfumuyaku Babulo,wosaikakhosilaom’golilamfumuyakuBabulo, mtunduumenewondidzaulangandilupanga,ndinjala,ndi mliri,kufikiranditawathandidzanjalake,atiYehova +9“Choteromusamvereanenerianu,+obwebwetaanu, olota+anu,obwebwetaanu,+obwebwetaanu,+amene akunenandiinukuti,‘SimudzatumikiramfumuyaBabulo 10Pakutiakuneneranizonama,kutiakutengerenikutalindi dzikolanu;ndikutindikuingitseni,ndipo mudzawonongeka
11Komaamitunduameneadzaikakhosilawopansipagoli lamfumuyakuBabulo,ndikuitumikira,ndidzawalekaiwo akhalem’dzikolao,atiYehova;ndipoadzalima, nadzakhalam’mwemo.
12NdinalankhulansondiZedekiyamfumuyaYudamonga mwamawuawaonse,kuti,Lolanimakosianumugolila mfumuyakuBabulo,ndikumtumikiraiyendianthuake, kutimukhalendimoyo.
13Mudzaferanji,inundianthuanu,ndilupanga,ndinjala, ndimliri,mongaYehovawanenazamtunduumene sudzatumikiramfumuyaBabulo?
+14“Choteromusamveremawuaaneneri+amene akunenakwainukuti,‘Simudzatumikiramfumuya Babulo,’+pakutiakuloserazonamakwainu
15Pakutisindinawatuma,atiYehova,komaanenera monamam’dzinalanga;kutindikupitikitseniinu,ndikuti muwonongeke,inu,ndianeneriameneanenerakwainu
16Ndinalankhulansondiansembendianthuonseawa,kuti, AteroYehova;Musamveremawuaanenerianuamene akuloserakwainu,kuti,Taonani,ziwiyazanyumbaya YehovazidzabwezedwakuBabuloposachedwapa; 17Musawamvereiwo;tumikiranimfumuyakuBabulo, nimukhalendimoyo:mudziuwuupasukabwanji?
+18Komangatialianeneri+ndipomawuaYehovaali nawo,+apembedzere+Yehovawamakamu,+kutiziwiya zotsalam’nyumbayaYehova,+m’nyumbayamfumuya Yuda,+ndikuYerusalemu,zisapitekuBabulo
+19Yehovawamakamuwanenakutiponenazazipilala, nyanja,mabeseni,+ndiziwiyazotsalamumzindauno
+20ChimeneNebukadinezaramfumuyaBabulo sanachitenge+pameneanatengerandendeYekoniya+ mwanawaYehoyakimumfumuyaYudakuYerusalemu n’kupitanayekuBabulo,+pamodzindianthuonse olemekezekaaYudandiYerusalemu;
+21Inde,Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeli wanenakuti,‘Ponenazaziwiyazimenezatsalam’nyumba yaYehova,m’nyumbayamfumuyaYudandiku Yerusalemu
22AdzatengedwakunkakuBabulo,+ndipoadzakhala kumenekompakatsikulimenendidzawazonda,”+watero Yehovapamenepondidzawakweza,ndikuwabwezera kumalokuno
MUTU28
1Ndipokunali,cakacomweco,ciyambicaufumuwa ZedekiyamfumuyaYuda,cakacinai,ndimweziwacisanu, HananiyamwanawaAzurimneneri,wakuGibeoni, analankhulananem’nyumbayaYehova,pamasopa ansembendianthuonse,ndikuti, 2Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeliwanenakuti, ‘NdathyolagolilamfumuyaBabulo.
+3M’zakaziwirizathunthu+ndidzabweretsansokumalo anoziwiyazonsezam’nyumbayaYehova,zimene NebukadinezaramfumuyaBabuloanazichotsapamaloano n’kupitanazokuBabulo
+4NdidzabweretsansokumaloanoYekoniya+mwanawa YehoyakimumfumuyaYuda,+pamodzindiandendeonse aYudaameneanapitakuBabulo,+wateroYehova, chifukwandidzathyolagolilamfumuyaBabulo.
5PamenepomneneriYeremiyaanauzamneneriHananiya pamasopaansembendipamasopaanthuonseamene anaimiriram’nyumbayaYehova
6NdipomneneriYeremiyaanati,Amen,Yehovaacite comweco;
7Komaimvatsopanomauawandinenam’makutuako,ndi m’makutuaanthuonse;
+8Aneneriameneanakhalapoinendisanakhaleinendi iweusanakhalepokalekaleloanaloserazamaikoambiri,+ maufumuaakulu,zankhondo,+zoipa,+ndimliri
9Mneneriameneakuloserazamtendere,mawua mneneriyoakadzakwaniritsidwa,mneneriyoadzadziwika kutiYehovaanamutumadi.
10PamenepomneneriHananiyaanachotsagolipakhosila mneneriYeremiya,nalithyola
11NdipoHananiyaananenapamasopaanthuonse,kuti, AteroYehova;Momwemondidzathyolagolila NebukadinezaramfumuyaBabulopakhosilaamitundu onsem’zakaziwirizathunthu.NdipomneneriYeremiya anamuka
12PamenepomawuaYehovaanadzakwaYeremiya mneneri,Hananiyamneneriatathyolagolipakhosila mneneriYeremiya,kuti:
13PitaukauzeHananiya,kuti,AteroYehova;Wathyola magoliamtengo;komaudzawapangiramagoliachitsulo.
14PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Ndaikagolilachitsulopakhosilaamitunduonsewa,kuti atumikireNebukadinezaramfumuyakuBabulo;ndipo zidzamtumikiraiye:ndipondapatsaiyensonyama zakuthengo
15PamenepomneneriYeremiyaanauzamneneriHananiya kuti:“TamveraHananiya!Yehovasanakutuma;komaInu mukhulupirirazonamaanthuawa
16CifukwacaceateroYehova;Taonani,ndidzakuchotsani pankhopepadzikolapansi;
17ChoteromneneriHananiyaanamwalirachaka chomwechom’mweziwa7.
MUTU29
1TsopanoawandimawuakalataimeneYeremiya mnenerianatumizakuchokerakuYerusalemukwaakulu otsalaameneanatengedwandende,ndikwaansembe,ndi aneneri,ndikwaanthuonseameneNebukadinezara anawatengandendekuYerusalemukumkanawoku Babulo;
2(PamenepoYekoniyamfumu,ndimfumukazi,ndinduna, akalongaaYudandiYerusalemu,ndiamisiriamatabwa, ndiosula,anachokakuYerusalemu;)
3MwadzanjalaElasamwanawaSafani,ndiGemariya mwanawaHilikiya,ameneZedekiyamfumuyaYuda anawatumizakuBabulokwaNebukadinezaramfumuya Babulo
4AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli,kwa onseotengedwandende,amenendinawatengeraku BabilonikucokerakuYerusalemu;
5Mumangenyumbandikukhalamo;Limaniminda,idyani zipatsozake;
6Tenganiakazi,nimubalaanaamunandiakazi; muwatengereanaanuamunaakazi,ndianaanuakazikwa amuna,kutiadzabalaanaamunandiakazi;kutimuchuluke kumeneko,osacepa
7Ndipofunanimtenderewamudziumenendakutengerani akapolo,nimuupemphererekwaYehova; 8PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Anenerianundialaulianuokhalapakatipanu asakunyengeni,kapenakumveramalotoanuamenemulota.
9Pakutianenerakwainuzonamam’dzinalanga; sindinawatuma,atiYehova
10PakutiateroYehova,Zitathazaka70kuBabulo, ndidzakufikirani,ndikukwaniritsamauangaabwinokwa inu,kukubwezanikumalokuno
11Pakutindidziwamalingiriroamenendilingiririrainu,ati Yehova,maganizoamtendere,osatiachoipa,kuti ndikupatseniinuchiyembekezerochakumapeto.
12Pamenepomudzandiitana,ndipomudzankandi kupempherakwaIne,ndipondidzakumverani
13NdipomudzandifunaIne,ndikundipeza,pamene mudzandifunandimtimawanuwonse
14Ndipondidzapezedwandiinu,atiYehova;ndipo ndidzakubwezeranikumalokumenendinakutengerani ndende
15Pakutimwati,Yehovawatiutsiraifeanenerim’Babulo;
16DziwanikutiYehovawanenazamfumuyakukhala pampandowachifumuwaDavide,ndizaanthuonseokhala mumzindauno,ndizaabaleanuamenesanatulukenanuku ukapolo;
17AteroYehovawamakamu;Taonani,ndidzawatumizira lupanga,ndinjala,ndimliri,ndipondidzawayesankhuyu zonyansa,zosadyedwa,ndizoipandithu.
18Ndipondidzawalondalondandilupanga,ndinjala,ndi mliri,ndipondidzawaperekaakhalechinthuchoopsezedwa kumaufumuonseadzikolapansi,akhaletemberero,ndi chodabwitsa,ndichotonzedwa,ndichitonzo,mwa amitunduonsekumenendinawapirikitsirako;
19Chifukwasanamveremawuanga,+wateroYehova, amenendinawatumizirakudzeramwaatumikiangaaneneri, +ndikamadzukam’mawandikuwatumakoma simunamvera,atiYehova.
+20ChoteroimvanimawuaYehova,+inunonseamene munatengedwaukapolo,+amenendinawatumizaku BabulokuchokerakuYerusalemu.
+21Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeliwanena kuti:“Ahabu+mwanawaKolayandiZedekiyamwanawa Maaseyaameneakuloserazonamam’dzinalanga.Taonani, ndidzawaperekam'dzanjalaNebukadirezaramfumuyaku Babulo;ndipoiyeadzawaphapamasopanu;
+22AndendeonseaYudaamenealikuBabulo adzatembererapaiwo,+kuti,‘Yehovaakuchitengati Zedekiya+ndiAhabu,+amenemfumuyaBabulo inaotchapamoto
+23+23Chifukwachakutiachitazachiwembu+mu Isiraeli+ndipoachitachigololo+ndiakaziaanansiawo, +ndikulankhulamawuonamam’dzinalanga,+amene sindinawalamulirengakhaleinendikudziwa,ndipondine mboni,atiYehova
24UkateronsokwaSemayawakuNehelamu,kuti, +25Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeliwanena kuti,‘Popezaunatumizamakalata+m’dzinalakokwa anthuonseokhalakuYerusalemu,+kwaZefaniya+ mwanawaMaaseyawansembe,+ndikwaansembeonse, +kuti:
26Yehovawakusankhanikukhalawansembem’malomwa Yehoyadawansembe,+kutimukhaleakapitawo+
m’nyumbayaYehova,+kwamunthualiyensewamisala,+ ameneamadzipangakukhalamneneri,+kutium’tsekere m’ndende+ndim’matangadza
27Tsopanon’chifukwachiyanisimunadzudzuleYeremiya wakuAnatoti+ameneakudzipangakukhalamnenerikwa inu?
28CifukwacaceanatitumiziraifekuBabulo,ndikuti, Undendeutali;Limaniminda,ndikudyazipatsozake.
29NdipoZefaniyawansembeanaŵerengakalataiyi m’makutuaYeremiyamneneri
30PamenepomauaYehovaanadzakwaYeremiya,kuti, 31Utumizekwaonseamenealim’ndende+kuti,‘Yehova wanenazaSemayawakuNehelamu.+ChifukwaSemaya +wanenerakwainu,+ndiposindinamutumize,+ndipo anakuchititsanikukhulupirirazonama
32CifukwacaceateroYehova;Taonani,ndidzalanga SemayawakuNehelami,ndimbeuyace;ndiposadzaona zabwinozimenendidzachitiraanthuanga,atiYehova; chifukwawanenazopandukiraYehova.
MUTU30
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova, kuti,
2AteroYehovaMulunguwaIsrayeli,kuti,Lembam’buku mauonseamenendalankhulanawe
3Pakutitaonani,masikuadza,atiYehova,pamene ndidzabwezansoundendewaanthuangaIsrayelindiYuda, atiYehova,ndipondidzawabwezakudzikolimene ndinapatsamakoloao,ndipoadzalilandira
4AwandimawuameneYehovaananenazaIsiraelindi Yuda
5PakutiateroYehova;Tamvamawuakunjenjemera, mantha,osatimtendere.
6Funsanitsopano,muonengatimwamunaalindipakati?
Ndipenyeranjimwamunaaliyensealindimanjam’chuuno mwake,ngatimkaziwobala,ndinkhopezonsezasanduka zotumbululuka?
7Tsoka!pakutitsikulondilalikuru,koterokutipalibelina lofanananalo;ndiyonthawiyamasautsoaYakobo;koma adzapulumutsidwam’menemo
8Pakutipadzakhalatsikulimenelo,atiYehovawa makamu,ndidzathyolagolilakekulichotsapakhosipako, ndikudulazomangirazako,ndipoalendo sadzamtumikiranso;
9KomaadzatumikiraYehovaMulunguwawo,ndiDavide mfumuyawo,amenendidzawaukitsira
10Chifukwachakeusaope,mtumikiwangaYakobo,ati Yehova;usaope,iweIsrayeli;pakuti,taona, ndidzakupulumutsakucokerakutali,ndimbeuzakoku dzikolandendezao;ndipoYakoboadzabwera,nadzakhala mumpumulo,ndikukhalachete,palibewomuopsa.
11PakutiInendilindiiwe,atiYehova,kuti ndikupulumutseiwe;
12PakutiYehovawanenakuti,‘Mkwingwirimawakondi wosachiritsika,+ndipobalalakon’lopwetekakwambiri
13Palibewonenezamlanduwako,kutiumangidwe;ulibe mankhwalaochiritsa
14Okondedwaakoonseakuiwala;sakufunaInu;pakuti ndakulasandibalalamdani,ndikulangakwawankhanza, cifukwacakucurukakwamphulupuluzako;chifukwa machimoakoadachuluka
15Uliriranjicifukwacakuzunzikakwako?chisonichako ndichosachiritsika,chifukwachakuchulukakwa mphulupuluzako;
16Chifukwachakeonseakudyaiweadzadyedwa;ndi adaniakoonse,onseaiwo,adzankakundende;ndipoiwo ameneakufunkhaadzafunkhidwa,ndionseakufunkha ndidzawaperekaakhalecofunkha
17Pakutindidzakubwezerathanzi,+ndipo ndidzakuchiritsazilondazako,”+wateroYehovapopeza anakutchaiweWopirikitsidwa,nati,UyundiZiyoni, amenepalibemunthuakuufuna
18AteroYehova;Taonani,ndidzabwezansoundendewa mahemaaYakobo,ndipondidzacitiracifundomokhalamo iye;ndimudziudzamangidwapamuluwace,ndinyumba yacifumuidzakhalamongamwamakonzedweace 19Ndipomwaiwomudzatulukachiyamikondimawua iwoakusekerera;+Ndidzawalemekeza+ndiposadzakhala ochepa
20Anaawonsoadzakhalamongakale,ndimsonkhano wawoudzakhazikikapamasopanga,ndipondidzalanga onseameneakuwatsendereza
21Ndipoolemekezekaaoadzakhalamwaiwookha,ndi kazembewaoadzaturukapakatipao;ndipo ndidzamyandikira,nadzayandikirakwaine;ateroYehova 22Ndipomudzakhalaanthuanga,ndipoInendidzakhala Mulunguwanu
23Taonani,kamvuluvuluwaYehovaatulukandiukali, ngatikamvuluvuluwokhalitsa;
24MkwiyowaukaliwaYehovasudzabwerera,kufikira atachita,mpakaatachitazolingalirazamtimawake;
MUTU31
1Nthawiyomweyo,atiYehova,InendidzakhalaMulungu wamabanjaonseaIsrayeli,ndipoiwoadzakhalaanthu anga
2Yehovawanenakuti:“Anthuameneanatsalandilupanga anapezachisomom’chipululungakhaleIsrayeli,pamene ndinapitakukamkhazikamtimapansi
3Yehovawandionekerakalekale,nati,Inde,ndakukonda iwendicikondicosatha;
4Ndipondidzakumanganso,ndipoudzamangidwa,iwe namwaliwaIsrayeli;
5UdzabzalansompesapamapiriaSamariya;
6PakutilidzafikatsikulimenealondapamapiriaEfraimu adzafuula,kuti,Nyamukani,tikwerekuZiyonikwa YehovaMulunguwathu
7PakutiateroYehova;ImbiraniYakobomokondwera, fuulanimwaakuluaamitundu;lengezani,lemekezani,ndi kuti,Yehova,pulumutsanianthuanu,otsalaaIsrayeli
8Taonani,ndidzawatengaiwokuchokerakudzikola kumpoto,ndipondidzawasonkhanitsaiwokuchokeraku malekezeroadzikolapansi,pamodzindiiwoakhungundi otsimphina,mkaziwapakatindiwobalamwanapamodzi; khamulalikululidzabwererakomweko
9Adzafikandikulira,ndipondidzawatsogolerandi mapembedzero;ndidzawayendetsapamitsinjeyamadzi m’njirayolunjika,m’menemosadzapunthwa;pakutiine ndineatatewaIsrayeli,ndiEfraimundiyemwanawanga woyamba.
10ImvanimawuaYehova,inuamitundu,nimuwalalikire m’zisumbuzakutali,ndikuti,AmeneanabalalitsaIsrayeli
adzamsonkhanitsa,nadzamsunga,mongambusaasamalira gululake.
11PakutiYehovaanaombolaYakobo,namuombola m’dzanjalaiyeameneanamposaiyemphamvu.
12Chifukwachakeadzadzanadzayimbam’phirilalitalila Ziyoni,+nadzathamangirapamodzikuubwinowaYehova, +tirigu,+vinyo,+mafuta,+anaankhosanding’ombe+ ndipomoyowawoudzakhalangatimundawothiriramadzi. ndiposadzamvachisonikonse
13Pameneponamwaliadzasangalalandikuvina,anyamata ndiokalambapamodzi;
14Ndipondidzakhutitsamoyowaansembendimafuta, ndipoanthuangaadzakhutandiubwinowanga,atiYehova.
15AteroYehova;MauanamvekakuRama,kulirandi kulirakowawa;Rakeleakuliraanaakeanakana kutonthozedwachifukwachaanaake,chifukwapalibe.
16AteroYehova;Lekamauakokulira,ndimasoakoku misozi;ndipoiwoadzabweransokuchokerakudzikola adani.
17Ndipochilipochiyembekezopamapetoako,atiYehova, kutianaakoadzabwererakumalireao
18NdamvaEfuraimuakudzigugudapachifuwachotere; Mwandilanga,ndipondalangidwa,ngating’ombeyaikazi yosakonzekeragoli;pakutiInundinuYehovaMulungu wanga.
19Zoonadi,nditatembenuka,ndinalapa;ndipo nditalangizidwa,ndinamenyapantchafuyanga:Ndinachita manyazi,inde,ngakhalemanyazi,popezandinanyamula chitonzochaubwanawanga
20KodiEfuraimundimwanawangawokondedwa?ali mwanawokoma?pakutikuyambirapamenendinalankhula motsutsananaye,ndikumbukirabendithu;+Ndithu ndidzam’chitirachifundo,”+wateroYehova
21Dziikirenizipilala,dzipangirenimiundaitaliitali, lozetsanimtimawanukukhwalala,njiramudayendamo; 22Udzayendayendakufikiraliti,iwemwanawamkazi wopanduka?pakutiYehovawalengachinthuchatsopano padzikolapansi,kutimkaziadzazingamwamuna
23AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Adzanenamauawam'dzikolaYudandim'midziyace, pamenendidzabwezansoundendewao;Yehova akudalitseni,pokhalamolungama,ndiphirilopatulika; 24NdipomuYuda,ndim’midziyaceyonsemudzakhala alimi,ndioturukandizoŵeta
25Pakutindakhutitsamtimawolefuka,ndipondadzaza moyowachisoniuliwonse.
26Pamenepondinadzuka,ndipondinapenya;ndipotulo langalinalilokomakwaine.
27Taonani,masikuakudza,atiYehova,pamene ndidzafesambeuzaanthundizanyamam’nyumbaya IsrayelindinyumbayaYuda
28Ndipokudzachitikakuti,mongandinawayang’anira, kuzula,ndikugumula,ndikugwetsa,ndikuononga,ndi kusautsa;momwemondidzawayang’anira,kumanga,ndi kubzala,atiYehova
29M’masikuamenewosadzanenansokuti,Atateanadya mphesazosacha,ndipomanoaanawoanayayamira.
30Komaaliyenseadzafachifukwachamphulupuluyake: munthualiyenseakadyamphesazosacha,manoake adzayayamira.
31Taonani,masikuadza,atiYehova,pamene ndidzapanganapanganolatsopanondinyumbayaIsrayeli, ndinyumbayaYuda;
32Osatimongamwapanganondinapanganandimakolo ao,tsikulijandinawagwirapadzanjakuwaturutsam’dziko laAigupto;limeneanaswapanganolanga,ngakhalendinali mwamunawao,atiYehova;
33Komailindipanganolimenendidzapanganandi nyumbayaIsrayeli;Atathamasikuamenewo,atiYehova, ndidzaikacilamulocangam'mtimamwao,ndipo ndidzacilembam'mitimayao;ndipondidzakhalaMulungu wao,ndiiwoadzakhalaanthuanga
34Ndiposadzaphunzitsansoyensemnansiwake,ndiyense mbalewake,kuti,DziwaYehova;pakutiiwoonse adzandidziwa,kuyambirawamng’onokufikirawamkulu waiwo,atiYehova;
35AteroYehova,ameneapatsadzuwakutilikhale lounikirausana,ndimalamuloamwezindinyenyezikuti zikhalezounikirausiku,ameneamagawanitsanyanjakuti mafundeakeagwedezeke;Yehovawamakamundilodzina lake;
36Maweruzoawaakachokapamasopanga,atiYehova, ndiyekutimbewuyaIsrayelinayonsoidzalekakukhala mtundupamasopangampakakalekale
37AteroYehova;Ngatikumwambakungayesedwe,ndi kufufuzidwamazikoadzikopansi,inensondidzataya mbewuyonseyaIsrayelichifukwachazonseanazichita,ati Yehova.
38Taonani,masikuakudza,atiYehova,pamenemzindawo udzamangidwiraYehovakuyambirapansanjayaHananeli kufikirakuchipatachapangodya.
39Ndipochingwechoyezerachochidzatulukiranso kutsogolokwakepaphirilaGarebu,n’kuzungulirampaka kuGowa.
40Chigwachonsechamitembo,+phulusa,+ndiminda yonsempakamtsinjewaKidironi,+mpakakungodyaya ChipatachaKavalo,+kum’mawa,+pazikhalazopatulika kwaYehovasichidzazulidwa,kapenakupasulidwaku nthawizonse
MUTU32
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova cakacakhumicaZedekiyamfumuyaYuda,ndichocaka cakhumindicitatucaNebukadirezara
2PamenepogululankhondolamfumuyaBabulolinazinga Yerusalemu,+ndipomneneriYeremiyaanatsekeredwa m’bwalolandende+limenelinalim’nyumbayamfumuya Yuda
3ZedekiyamfumuyaYudaanaliatamutsekera,+kuti: “N’chifukwachiyaniukuloserakuti,‘Yehovawanenakuti, ‘Taonani,ndiperekamzindauwum’manjamwamfumuya Babulo,ndipoidzaulanda
4ZedekiyamfumuyaYudasadzapulumukam’manjamwa Akasidi,+komandithuadzaperekedwam’manjamwa mfumuyaBabulo,+ndipoadzalankhulanayepakamwa ndipakamwa,+ndipomasoakeadzaonamasoake. +5IyeadzatengeraZedekiyakuBabulo,+ndipo adzakhalakumenekokufikiranditam’chezera,+watero Yehova.
6NdipoYeremiyaanati,MauaYehovaanadzakwaine, kuti,
7Taonani,HanamelimwanawaSalumumlongowako adzadzakwaiwe,ndikuti,Ugulemundawangauliku Anatoti,pakutiulindiufuluwakuombolakuugula
8PamenepoHanamelimwanawamlongowangaanadza kwainem’bwalolandende,mongamwamauaYehova, natikwaine,Uguletumundawanga,umeneulikuAnatoti, m’dzikolaBenjamini;dzigulirewekhaPamenepo ndinadziwakutiawandimauaYehova.
9NdipondinagulamundawaHanamelimwanawamlongo wangawakuAnatoti,ndikumuyeserandalama,masekeli khumindiasanundiawiriasiliva
10Ndipondinalembachikalatacho,ndikuchisindikiza, ndiitanamboni,ndikamuyezandalamamumiyeso.
11Choterondinatengachikalatachoguliracho, chosindikizidwachizindikirochomogwirizanandi chilamulo+ndimwambo,+ndichotsegulacho.
12NdipoumboniwakugulandinauperekakwaBaruki mwanawaNeriya,mwanawaMaaseya,pamasopa Hanamelimwanawamlongowanga,ndipamasopamboni zolemberam’bukulazogulira,pamasopaAyudaonse okhalam’bwalolakaidi
13NdipondinauzaBarukipamasopao,ndikuti, 14AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Tenganimaumboniawa,umboniuwuwakugula,zonse zomwezasindikizidwa,ndiumboniuwuumeneuli wotseguka;ndikuziikam’chotengerachadothi,kuti zikhalemasikuambiri
15PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Nyumbandimindandimindayampesaidzalandidwanso m’dzikomuno
16NditaperekachikalatachogulirakwaBarukimwanawa Neriya,ndinapempherakwaYehova,ndikuti, 17OAmbuyeYehova!taonani,mudalengakumwambandi dzikolapansindimphamvuyanuyaikulu,ndimkonowanu wotambasuka;
18Mumachitirazikwizikwi,ndikubwezeramphulupulu zaatatem’chifuwachaanaawopambuyopao:Wamkulu, MulunguWamphamvu,Yehovawamakamu,ndilodzina lake;
19Wamkulumuuphungu,ndiwamphamvum’ntchito, pakutimasoanualiotsegukiranjirazonsezaanaaanthu, kutimupatseyensemongamwanjirazake,ndimonga zipatsozantchitozake;
20amenemunaikazizindikirondizozizwam’dzikola Aiguptokufikiralerolino,ndim’Israyeli,ndimwaanthu ena;ndipomunadzipangiradzina,mongalerolino;
21NdipomunaturutsaanthuanuAisrayelim’dzikola Aiguptondizizindikiro,ndizodabwitsa,ndidzanja lamphamvu,ndimkonowotambasuka,ndizoopsazazikulu; 22ndipomunawapatsadzikoili,limenemunalumbirira makoloawokuwapatsa,dzikomoyendamkakandiuchi ngatimadzi;
23Ndipoadalowa,naulandira;komasanamveramauanu, kapenakutsatacilamulocanu;sanachitekanthukalikonse mwazonsemudawalamulirakuchita:chifukwachake mwawatengerachoipaichichonse;
24Taonani,zitundazafikakumzindakuulanda;+ Mzindawuwaperekedwam’manjamwaAkasidiamene akumenyananawochifukwachalupanga,+njala,+mliri, +ndipozimenemwanenazachitika.ndipo,taona,ucipenya.
25InuYehovaAmbuyeWamkuluKoposa,mwandiuza kuti,‘Udziguliremundandindalama,ndipoutengemboni. pakutimzindawowaperekedwam’manjamwaAkasidi 26PamenepomauaYehovaanadzakwaYeremiya,kuti, 27Taonani,InendineYehova,Mulunguwaanthuonse; 28CifukwacaceateroYehova;Taonani,ndidzapereka mudziuwum’manjamwaAkasidi,ndim’dzanjala NebukadirezaramfumuyakuBabulo,ndipoiye adzaulanda;
29NdipoAkasidi,ameneakumenyanandimzindauwu, adzabwerandikuyatsamotopamzindauwu,ndikuutentha pamodzindinyumbazimenepamwambapamatsindwi awoanaperekansembezautsikwaBaala,+ndikuthira nsembezachakumwakwamilunguina,+kutiandikwiyitse +30PakutianaaIsiraelindianaaYudaakhalaakuchita zoipazokhazokhapamasopangakuyambirapaubwana wawo,+pakutianaaIsiraeliangondiputandintchitoya manjaawo,”+wateroYehova
31Pakutimudziuwuwakhalawoutsamkwiyowangandi ukaliwangakuyambiratsikulijaanaumangampakalero; kutindiuchotsepamasopanga,
+32Chifukwachazoipazonse+zaanaaIsiraeli+ndiza anaaYuda,+zimeneanachitapofunakundikwiyitsa,+ iwowo,mafumuawo,+akalongaawo,ansembeawo, aneneriawo,anthuakuYudandiokhalamuYerusalemu.
33Ndipoananditembenuziramsana,sinkhope; 34Komaanaikazonyansazaom’nyumbayochedwadzina langa,kuidetsa.
35AnamangansomalookwezekaaBaala+m’chigwacha mwanawaHinomu+kutiaziwotchaanaawoaamunandi aakazipamoto+kwaMoleki.chimenesindinawalamulira, kapenasichinandilowam'mtimamwanga,kutiachite chonyansaichi,kuchimwitsaYuda
+36ChoterotsopanoYehovaMulunguwaIsiraeliwanena kuti,‘Ponenazamzindauwu,umeneinumukuti, Udzaperekedwam’manjamwamfumuyaBabulondi lupanga,njala,ndimliri.
37Taonani,ndidzawasonkhanitsam’maikoonsekumene ndinawaingitsiramumkwiyowanga,ndiukaliwanga,ndi ukaliwaukulu;ndipondidzawabwezansokumaloano,ndi kuwakhalitsamwabata;
38Ndipoiwoadzakhalaanthuanga,ndipoInendidzakhala Mulunguwawo;
39Ndipondidzawapatsamtimaumodzindinjiraimodzi, kutiandiwopekosatha,kutiiwondianaawoapambuyo pawoapindule;
40Ndipondidzapangananaopanganolosatha,kuti sindidzawapatuka,ndikuwachitirazabwino;koma ndidzaikakuopakwangam’mitimayao,kutiasandicoke
41Inde,ndidzakondweranawokuwachitirazabwino, ndipondidzawabzalandithum’dzikomunondimtima wangawonsendimoyowangawonse.
42PakutiateroYehova;Mongandatengeracoipaiciconse paanthuawa,momwemondidzawatengerazabwinozonse ndinawalonjeza
43Ndipomindaidzagulidwam’dzikolino,limenemukuti, Ndibwinja,lopandamunthukapenanyama;waperekedwa m’manjamwaAkasidi
44Anthuadzagulamindandindalama,nadzalemba zikalata,nadzazisindikiza,nadzatengambonim’dzikola Benjamini,ndim’maloozunguliraYerusalemu,ndi m’midziyaYuda,ndim’midziyakumapiri,ndim’midzi
yakucigwa,ndim’midziyakumwera;pakutindidzabweza undendewao,atiYehova.
MUTU33
1NdipomauaYehovaanadzakwaYeremiyanthawi yaciwiri,iyeakaliwotsekeredwam'bwalolakaidi,kuti, 2AteroYehovaameneanachipanga,Yehovaamene anachipanga,kutialikhazikitse;dzinalakendiYehova; 3Undiitane,ndipondidzakuyankha,ndipo ndidzakusonyezazinthuzazikulundizamphamvu,zimene suzidziwa
+4PakutiYehovaMulunguwaIsiraeliwanenakuti, ‘Zonenazanyumbazamzindauno+ndizanyumbaza mafumuaYuda+zogwetsedwandizitundandilupanga +5IwoakubwerakudzamenyanandiAkasidi,+koma adzawadzazandimitemboyaanthu+amenendinawapha mumkwiyowanga+ndiukaliwanga,+ndiponso chifukwachazoipazonsezimenendabisankhopeyanga mumzindauno
6Taonani,ndidzaupatsathanzindikuciritsa,ndipo ndidzaciritsaiwo,ndikuwavumbulutsirakucurukakwa mtenderendicoonadi
7NdipondidzabwezaundendewaYudandiwaIsrayeli, ndikuwamangamongapoyambapaja.
8Ndidzawayeretsakumphulupuluzawozonsezimene wandichimwiranazo;+Ndidzakhululukiramphulupulu zawozonsezimenewandichimwiranazo+ndi kundilakwiranazo
9Ndipolidzakhalakwainedzinalachisangalalo, chitamandondiulemupamasopaamitunduonseadziko lapansi,ameneadzamvazabwinozonsendidzawachitira; 10AteroYehova;Padzamvekansom’maloano,ameneinu mukutipadzakhalabwinjalopandamunthundinyama, ngakhalem’mizindayaYuda,ndim’misewuya Yerusalemu,imeneilibwinja,yopandamunthu, yokhalamo,yopandanyama;
11Mauacimwemwe,ndimauacimwemwe,maua mkwati,ndimauamkwatibwi,mauaiwoameneadzati, TamandaniYehovawamakamu,pakutiYehovandiye wabwino;pakuticifundocacecikhalakosatha;Pakuti ndidzabwezaundendewam'dzikomongapoyambapaja, atiYehova.
12AteroYehovawamakamu;Ndiponsom’malomuno, amenealibwinja,opandamunthundinyama,ndi m’mizindayakeyonse,mudzakhalamokhalaabusa akugonetsazoŵetazawo
13M’mizindayakumapiri,+m’mizindayakuchigwa,+ m’mizindayakumwera,+m’dzikolaBenjamini,+ m’maloozunguliraYerusalemu+ndim’mizindayaYuda, +zowetazidzadutsansom’manjamwaiyeamene akuwauza,+wateroYehova.
14Taonani,masikuakudza,atiYehova,pamene ndidzakwaniritsamauabwinoamenendalankhulakwa nyumbayaIsrayelindinyumbayaYuda 15M’masikuamenewo,ndipanthawiimeneyo,+ ndidzameretsaMphukirayachilungamokwaDavide.ndipo iyeadzachitachiweruzondichilungamom’dziko 16M’masikuamenewoYudaadzapulumutsidwa,+ndipo Yerusalemuadzakhalamosatekeseka,+ndipodzinalimene adzatchedwanalondiili,Yehovandiyechilungamochathu
17PakutiateroYehova;Davidesadzasowamunthu wokhalapampandowachifumuwanyumbayaIsraele; +18AnsembeAlevisadzasowamunthupamasopanga woperekansembezopsereza+ndikupserezansembe zambewu+ndikuperekansembenthawizonse.
19NdipomauaYehovaanadzakwaYeremiya,kuti, 20AteroYehova;+Ngatimungathekuswapanganolanga lausana+ndipanganolangalausiku,+kutipasakhale usanandiusikupanthawiyake;
21PamenepopanganolangandiDavidemtumikiwanga likhozakuthyoledwa,kutiasakhalendimwana wamwamunawolamulirapampandowakewachifumu;ndi Aleviansembe,atumikianga.
+22Mongakhamulakumwambasilingathekuŵerengeka, +ngakhalemchengawakunyanjaungayesedwe,+ momwemondidzachulukitsambewu+yaDavidemtumiki wanga,+ndiAleviameneakunditumikira
23NdipomauaYehovaanadzakwaYeremiya,kuti, 24Kodisimukuonachimeneanthuawaanena,kuti, MabanjaawiriameneYehovaanawasankha,wawataya? moteroanapeputsaanthuanga,kutiasakhalensomtundu pamasopao.
25AteroYehova;Ngatipanganolangasilikhalandiusana ndiusiku,ndipongatisindinakhazikitsemalamulo akumwambandidzikolapansi; 26PamenepondidzatayambewuyaYakobo,ndiDavide mtumikiwanga,kutisindidzatengawinawambeuzake akhalewolamulirambewuyaAbrahamu,Isake,ndi Yakobo;
MUTU34
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova, pameneNebukadinezaramfumuyakuBabulo,ndigulu lacelonse,ndimaufumuonseadzikolapansim’ulamuliro wace,ndianthuonse,anamenyanandiYerusalemu,ndi midziyaceyonse,kuti,
2AteroYehova,MulunguwaIsrayeli;Pitaukanenendi ZedekiyamfumuyaYuda,numuuzekuti,AteroYehova; Taonani,ndidzaperekamudziuwum’dzanjalamfumuya kuBabulo,ndipoidzautenthandimoto;
3Ndipoiwesudzapulumukam’dzanjalake,koma udzagwidwandithu,ndikuperekedwam’dzanjalake;ndipo masoakoadzaonamasoamfumuyakuBabulo,ndipoiye adzalankhulanawepakamwandipakamwa,ndipoudzapita kuBabulo.
4KomaiweZedekiyamfumuyaYuda,imvamawua Yehova;AteroYehovazaiwe,Sudzafandilupanga; 5Komaiweudzafamumtendere;ndipoadzakuliriraniinu, ndikuti,Ha!pakutindanenamau,atiYehova
6PamenepomneneriYeremiyaanauzaZedekiyamfumu yaYudamawuonsewakuYerusalemu.
+7PamenegululankhondolamfumuyaBabulo linamenyanandiYerusalemu+ndimizindayonseyaYuda imeneinatsala,+Lakisi+ndiAzeka,+pakutimizinda yokhalandimipandayolimbakwambiriimeneyiinatsala m’mizindayaYuda.
8AwandimauameneYehovaanadzakwaYeremiya, mfumuZedekiyaitapanganapanganondianthuonse okhalakuYerusalemu,kutiawalalikireufulu; 9kutiyensealolekapolowakewamwamuna,ndiyense alolemdzakaziwake,MhebrikapenaMhebri,amukemfulu;
kutiasatumikiremmodziwaiwo,ndiyeMyudambale wake.
10Tsopanoakalongaonsendianthuonseameneanachita panganoanamvakutialiyensealolekapolowake wamwamunandimdzakaziwakeapitemfulu,kuti asatumikirensoaliyensewaiwo,anamverandikuwalola kupita
11Komapambuyopakeanatembenuka,nabwezaakapolo ndiadzakazi,ameneadawamasula,nawagwiritsantchito akapolondiadzakazi
12ChonchomawuaYehovaanadzakwaYeremiya kuchokerakwaYehova,kuti:
13AteroYehova,MulunguwaIsrayeli;Ndinapangana panganondimakoloanutsikulijandinawaturutsam’dziko laAigupto,m’nyumbayaakapolo,ndikuti;
14Pakuthazakazisanundiziŵirimuzilolayensembale wakeMhebri,ameneanagulitsidwakwainu;ndipo akadzakutumikiranizakazisanundichimodzi,umlole amukekwainuwaufulu;komamakoloanusanandimvera Ine,sanatcherakhutu
15Ndipoinumunatembenukatsopano,ndikuchita zoongokapamasopanga,mwakulalikiraufulu,yensekwa mnansiwake;ndipomunapanganapanganopamasopanga m’nyumbayochedwadzinalanga;
16Komamunatembenukandikuipitsadzinalanga,ndi kubwezayensekapolowace,ndiyensemdzakaziwace, amenemunammasulamwakufunakwao,nimuwagonjetsa, akhaleakapoloanundiadzakazianu.
17CifukwacaceateroYehova;Simunandimveraine, kulalikiraufulu,yensekwambalewake,ndiyensekwa mnansiwake;ndipondidzakusandutsachinthuchoopsetsa m’maufumuonseadzikolapansi
18Ndidzaperekaamunaameneanaphwanyapanganolanga, amenesanachitemawuapanganolimeneanapangana pamasopanga,pameneanadulamwanawang’ombepakati, ndikudutsapakatipaziwalozake
19AkalongaaYuda,akalongaaYerusalemu,nduna,ndi ansembe,ndianthuonseam’dziko,ameneanadutsapakati pambalizamwanawang’ombe;
+20Ndidzawaperekam’manjamwaadaniawo+ndi m’manjamwaanthuameneakufunamoyowawo,+ndipo mitemboyawoidzakhalachakudyachambalameza m’mlengalengandizilombozapadzikolapansi.
+21NdidzaperekaZedekiya+mfumuyaYudandi akalongaakem’manjamwaadaniawo,+m’manjamwa anthuameneakufunamoyowawo,+ndim’manjamwa gululankhondolamfumuyaBabulo,+limenelikuchokera kwainu.
22Taonani,ndidzalamulira,atiYehova,ndikuwabwezera kumzindauwu;+Iwoadzamenyananawondikuulandandi kuutenthandimoto
MUTU35
1MauameneanadzakwaYeremiyakucokerakwaYehova masikuaYehoyakimumwanawaYosiyamfumuyaYuda, kuti,
2PitakunyumbayaArekabu,lankhulanawo,nulowe nawom'nyumbayaYehova,m'chipindachina,nuwapatse vinyoamwe.
3PamenepondinatengaYaazaniyamwanawaYeremiya, mwanawaHabaziniya,ndiabaleake,ndianaakeonse,ndi nyumbayonseyaArekabu;
4Kenakondinawalowetsam’nyumbayaYehova+ m’chipindachaanaaHanani+mwanawaIgidaliya+ munthuwaMulunguwoona,+chimenechinalipafupindi chipindachaakalonga+chimenechinalipamwambapa chipindachaMaaseya+mwanawaSalumu,+ woyang’anirapakhomo
5NdipondinaikapamasopaanaanyumbayaArekabu mitsukoyodzalandivinyo,ndizikho,ndikunenanao, Imwanivinyo
6Komaiwoanati,Sitimwavinyo,pakutiYehonadabu+ mwanawaRekabuatatewathuanatilamulakuti, ‘Musamamwevinyo,inukapenaanaanumpakakalekale 7musamangenyumba,kapenakufesambewu,kapena kubzalamphesa,kapenakukhalanayo;kutimukhale masikuambirim’dzikolimenemulialendo +8ChoterotamveramawuaYehonadabu+mwanawa Rekabuatatewathupazonsezimenewatilamulakuti tisamwevinyomasikuathuonse,+ife,akaziathu,anaathu aamunandianaathuaakazi; 9kapenakutimanganyumbazokhalamo:tiribeminda yamphesa,kapenaminda,kapenambewu; 10Komaifetakhalam’mahema,ndikumvera,ndikuchita mongamwazonseYehonadabuatatewathuanatilamulira 11Komakunachitika,pameneNebukadirezaramfumuya Babuloanakweram’dzikolo,tinati,Tiyeni,tipiteku YerusalemuchifukwachankhondoyaAkasidi,ndikuopa ankhondoaAsiriya;
12PamenepomauaYehovaanadzakwaYeremiya,kuti, 13AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli;Pita ukauzeanthuaYudandiokhalam'Yerusalemukuti,Kodi simudzalandiramalangizokumveramawuanga?atero Yehova
14MawuaYehonadabu+mwanawaRekabu,+amene analamulaanaakekutiasamwevinyo,+akwaniritsidwa. pakutimpakaleroiwosamamwakanthu,komaamvera lamulolaatatewao;komasimunandimveraIne
15Ndinatumizansokwainuatumikiangaonseaneneri, kuukamamawandikuwatuma,ndikuti,Bwereranitu, yensekunjirayakeyoipa,nimukonzemachitidweanu, osatsatamilunguyinakuitumikira;ndipomudzakhala m’dzikolimenendakupatsaniinundimakoloanu;koma simunatcherakhutulanu,kapenakundimveraIne
16PakutianaaYehonadabumwanawaRekabuasunga lamulolaatatewao,limeneanawalamulira;komaanthu awasanandimveraIne;
17CifukwacaceateroYehova,Mulunguwamakamu, MulunguwaIsrayeli;Taonani,ndidzatengerapaYudandi onseokhalam'Yerusalemuzoipazonsendinazineneraiwo; ndipondinawaitana,komasanayankhe.
18Yeremiyaanauzaam’nyumbayaArekabukuti: “Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeliwanenakuti:+ ChifukwamunamveralamulolaYehonadabuatatewanu,+ ndikusungamalamuloakeonse,+ndikuchitamongamwa zonseanakulamulirani.
19CifukwacaceateroYehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli;YehonadabumwanawaRekabusadzasowa munthuwoimapamasopanganthawizonse.
MUTU36
1Ndipokunali,cakacacinaicaYehoyakimumwanawa YosiyamfumuyaYuda,mauawaanadzakwaYeremiya kucokerakwaYehova,kuti, 2Tengampukutuwabukhu,nulembem’menemomawu onseamenendanenakwaiweotsutsaIsrayeli,ndiYuda, ndiamitunduonse,kuyambiratsikulimenendinalankhula nawe,kuyambiramasikuaYosiya,kufikiralerolino 3KapenanyumbayaYudaidzamvazoipazonsezimene nditindiwachitire;kutiabwerereyensekulekanjirayace yoipa;kutindikhululukiremphulupuluzaondikucimwa kwao.
4PamenepoYeremiyaanaitanaBarukimwanawaNeriya, ndipoBarukianalembapampukutumawuonseaYehova ameneYehovaanamuuza,kuchokeramkamwamwa Yeremiya
5NdipoYeremiyaanalamuliraBaruki,kuti,Ine ndatsekedwa;Sindingathekulowam’nyumbayaYehova. 6Cifukwacacepitaiwe,nuwerengem’mpukutuumene unalembam’kamwamwanga,mauaYehovam’makutua anthum’nyumbayaYehovapatsikulakusalakudya; +7Mwinamapembedzeroawoadzafikapamasopa Yehova,+ndipoaliyenseadzabwererakusiyanjirayake yoipa,+pakutimkwiyondiukaliumeneYehovawanenera anthuawandiwaukulu
8NdipoBarukimwanawaNeriyaanachitamongamwa zonseadamuuzaYeremiyamneneri,nawerengam’buku mawuaYehovam’nyumbayaYehova
9M’chakachachisanuchaYehoyakimu+mwanawa Yosiya,mfumuyaYuda,m’mweziwachisanundichinayi, +analengezakutiasalekudya+pamasopaYehovakwa anthuonseakuYerusalemu+ndikwaanthuonseamene anachokeram’mizindayaYudakupitakuYerusalemu.
10PamenepoBarukianawerengam’bukumawua Yeremiyam’nyumbayaYehova,+m’chipindacha Gemariya+mwanawaSafanimlembi,+m’bwalo lapamwamba,+pakhomolachipatachatsopanocha nyumbayaYehova,+m’makutuaanthuonse
11MikayamwanawaGemariya,mwanawaSafani, anamvam’bukumawuonseaYehova
12Kenakoanatsikiram’nyumbayamfumu,+m’chipinda chamlembi,+ndipotaonani,akalongaonseanakhala mmenemo,+Elishama+mlembi,+Delayamwanawa Semaya,+ElinatanimwanawaAkibori,+Gemariya mwanawaSafani,+ZedekiyamwanawaHananiya,+ndi akalongaonse
13PamenepoMikayaanawauzamawuonseamene anamvapameneBarukianaŵerengabukum’makutua anthu
14PamenepoakalongaonseanatumizaYehudimwanawa Netaniya,mwanawaSelemiya,mwanawaKusi,kwa Baruki,kukanenakuti,Tengam’dzanjalakompukutu umeneunauwerengam’makutuaanthu,nubwereNdipo BarukimwanawaNeriyaanatengampukutum'dzanjalace, nadzakwaiwo
15Ndipoanatikwaiye,Khalapansi,nuwerengem’makutu mwathuChonchoBarukianawerengam’makutumwawo 16Ndipokunali,pameneanamvamauonse,anaopawina ndimnzace,natikwaBaruki,Tidzamuuzandithumfumu mauonsewa
17NdipoanafunsaBarukikuti,Utiuze,Unalembabwanji mauawaonsem’kamwamwace?
18NdipoBarukianayankhaiwo,Anachulukirakwaine mauonsewandipakamwapake,ndipondinawalembandi inkim’buku.
19PamenepoakalongaanatikwaBaruki,Muka,kabisale, iwendiYeremiya;ndipomunthuasadziwekumenemuli
20Ndipoanalowakwamfumum’bwalo,naikampukutuwo m’chipindachaElisamamlembi,nafotokozeramawuonse m’makutuamfumu
21PamenepomfumuinatumaYehudikukatenga mpukutuwo,ndipoiyeanauchotsam’chipindachaElisama mlembi.NdipoYehudianauwerengam’makutuamfumu, ndim’makutuaakalongaonseameneanaimirirapafupindi mfumu
22Tsopanomfumuinakhalam’nyumbayachisanu m’mweziwachisanundichinayi,+ndipomotounali kuyakam’ng’anjopamasopake
23Ndipokunali,pameneYehudianaŵerengamasamba atatukapenaanai,anadulandimpeniwakulembera, nauponyam’motoumeneunalipang’anjo,mpakampukutu wonseunathapamotoumeneunalipang’anjo.
24Komaiwosanachitemantha,kapenakung’ambazovala zawo,ngakhalemfumu,kapenaatumikiakeonseamene anamvamawuonsewa.
+25KomaElinatani+ndiDelaya+ndiGemariya+ anachonderera+mfumukutiisatenthempukutuwo,+ komasinawamvere.
26KomamfumuinalamulaYerameelimwanawamfumu, SerayamwanawaAzirieli,ndiSelemiyamwanawa AbidielikutiagwireBarukimlembindiYeremiyamneneri, komaYehovaanawabisa
27PamenepomauaYehovaanadzakwaYeremiya, mfumuitatenthampukutuwo,ndimauameneBaruki adawalembam’kamwamwaYeremiya,kuti:
28Utengensompukutuwina,nulembemomawuonse oyambaameneanalimumpukutuwoyamba,umene YehoyakimumfumuyaYudaanautentha +29UkauzeYehoyakimumfumuyaYudakuti,‘Yehova wanenakuti:Waotchampukutuuwu,ndikuti, Unalemberanjim’menemo,kuti,MfumuyakuBabulo idzadzandithu,nadzawonongadzikolino,nidzaletsamo anthundinyama?
30CifukwacaceateroYehovazaYehoyakimumfumuya Yuda;Sadzakhalandiwinawokhalapampando wachifumuwaDavide;
31Ndipondidzamlangaiye,ndimbeuyake,ndiatumiki ake,chifukwachamphulupuluzao;ndipondidzatengerapa iwo,ndipaokhalam'Yerusalemu,ndipaanthuaYuda, zoipazonsendinawaneneraiwo;komasanamvera 32PamenepoYeremiyaanatengampukutuwina, nauperekakwaBarukimlembi,mwanawaNeriya;amene analembam’menemomocokeram’kamwamwaYeremiya mauonseam’bukulimeneYehoyakimumfumuyaYuda analitenthandimoto;
MUTU37
1NdipomfumuZedekiyamwanawaYosiyaanalowa ufumum'malomwaKoniyamwanawaYehoyakimu, ameneNebukadirezaramfumuyakuBabuloanamlonga ufumum'dzikolaYuda
2Komaiye,kapenaatumikiake,kapenaanthuam’dziko, sanamveremawuaYehovaameneananenakudzeramwa mneneriYeremiya
3NdipomfumuZedekiyaanatumizaYehukalimwanawa SelemiyandiZefaniyamwanawaMaaseyawansembekwa Yeremiyamneneri,kuti,TipemphererekwaYehova Mulunguwathu
4TsopanoYeremiyaankalowandikutulukapakatipa anthuwo,chifukwasanamutsekerem’ndende
5PamenepogululankhondolaFaraolinatulukamuIgupto, ndipoAkasidiameneanazingaYerusalemuatamvazaiwo, anachokakuYerusalemu
6PamenepomauaYehovaanadzakwamneneriYeremiya, kuti,
7AteroYehova,MulunguwaIsrayeli;Muziterokwa mfumuyaYuda,imeneinakutumizanikwaine kudzafunsirakwaine;taonani,ankhondoaFarao,amene anaturukakudzathandizainu,adzabwererakuAiguptoku dzikolao.
8NdipoAkasidiadzabweranso,nadzamenyanandimudzi uwu,naulanda,ndikuutenthandimoto
9AteroYehova;Musadzinyenge,ndikuti,Akasidi adzachokandithukwaife,pakutisadzachoka
+10Ngakhalekutimunakanthagululonselankhondola Akasidi+ameneakumenyanananu,+n’kutsalapakati pawoanthuovulala,komaaliyenseakananyamukam’hema wakendikuwotchamzindawundimoto
11Ndipokunali,pamenegululankhondolaAkasidi linaphwanyidwakuYerusalemuchifukwachamantha ankhondoaFarao
12PamenepoYeremiyaanatulukam’Yerusalemukupita kudzikolaBenjamini,kutiadzipatulakumenekopakatipa anthu
13AtafikapachipatachaBenjamini,+panalimkuluwa alonda,dzinalakeIriya,mwanawaSelemiya,mwanawa HananiyanagwiraYeremiyamneneri,nati,Wathawira kwaAkasidi.
14PamenepoYeremiyaanati,Zabodza;Sindinatherekera kwaAkasidiKomaiyesanamveraiye;moteroIriya anatengaYeremiya,napitanayekwaakalonga.
+15ChonchoakalongaanakwiyiraYeremiya+moti anam’menyan’kumutsekeram’ndende+m’nyumbaya Jonatani+mlembi,+chifukwandiameneanamanga ndendeyo
16PameneYeremiyaanaloŵam’dzenje,ndim’zipinda, Yeremiyaanakhalam’menemomasikuambiri;
17PamenepomfumuZedekiyaanatumizaanthunamtenga, ndipomfumuinamfunsamserim’nyumbamwake,niti, KodipalimauochokerakwaYehova?NdipoYeremiya anati,Ulipo,pakutianati,udzaperekedwam'dzanjala mfumuyakuBabulo
18YeremiyaanafunsansomfumuZedekiyakuti:“Kodi ndakulakwiranichiyani,atumikianukapenaanthuwakuti anditsekerem’ndende?
19Alikutitsopanoanenerianuameneanaloserakwainu, kuti,MfumuyaBabulosidzabwerakudzamenyanandiinu, kapenadzikolino?
20Cifukwacaceimvanitu,mbuyewangamfumu,pempho langalivomerezekepamasopanu;kutiusandibwezereku nyumbayaJonatanimlembi,ndingafekomweko.
+21PamenepomfumuZedekiyainalamulakutiYeremiya aperekedwem’bwalolandende,+kutitsikulililonse
amupatsechidutswachamkatechochokeram’khwalalala ophikamkate,+mpakamkatewonseunathamumzindawo. MomwemoYeremiyaanakhalam'bwalolandende
MUTU38
1PamenepoSefatiyamwanawaMatani,ndiGedaliya mwanawaPasuri,ndiYukalimwanawaSelemiya,ndi PasurimwanawaMalikiya,anamvamauameneYeremiya ananenakwaanthuonse,kuti, 2Yehovawanenakuti,‘Ameneadzatsalemumzindauno adzafandilupanga,njala,ndimliri,+komaameneakupita kwaAkasidiadzakhalandimoyo.pakutimoyowace udzakhalacofunkha,nadzakhalandimoyo
3Yehovawanenakuti:“Mzindauwuudzaperekedwa ndithum’manjamwagululankhondolamfumuyaku Babulo,+limenelidzaulande
+4Chonchoakalongaanauzamfumukuti:“Mulolekuti munthuameneyuaphedwe,+chifukwaafooketsamanjaa amunaankhondootsalamumzindaunondimanjaaanthu onsepowauzamawuotere,+pakutimunthuyusafuna ubwinowaanthuawa,+komachoipa.
5PamenepomfumuZedekiyainati,Taonani,iyeali m’dzanjalanu;
6PamenepoanatengaYeremiyandikumponyam’dzenjela Malikiyamwanawamfumu,limenelinalim’bwalola alonda,+ndipoanatsitsaYeremiyandizingweNdipo m’dzenjemomunalibemadzi,komamatope;ndipo Yeremiyaanamiram’thope
7TsopanoEbedimelekiMkusi,+mmodziwandunaza m’nyumbayamfumu,anamvakutiYeremiyaanaika m’dzenjepamenepomfumuidakhalapachipatacha Benjamini;
8Ebedimelekianaturukam’nyumbayamfumu,nalankhula ndimfumu,kuti,
9Mbuyewangamfumu,anthuawaachitazoipam’zonse zimeneanamchitiraYeremiyamneneri,ameneanamponya m’dzenje;ndipoadzafandinjalam’maloameneali:pakuti mulibemkatem’mudzimo
10PamenepomfumuinauzaEbedimelekiMkusi,kuti, Tengakunoamunamakumiatatu,nutulutseYeremiya mnenerim’dzenje,asanafe
11PamenepoEbedimelekianatengaanthuwo,nalowa m’nyumbayamfumupansipamosungiramochuma, natengamonsanzazakalendinsanzazowola,nazitsitsandi zingwem’dzenjekwaYeremiya.
12NdipoEbedi-MelekiMkusi,anatikwaYeremiya,Ikatu nsanzazakaleizindinsanzazowolam’makhwapamwako pansipazingweNdipoYeremiyaanachitachomwecho
13PamenepoanaturutsaYeremiyandizingwe,namturutsa m’dzenje;
14PamenepomfumuZedekiyaanatumizaanthukukatenga mneneriYeremiyakwaiyepakhomolachitatula m’nyumbayaYehovausandibisirekalikonse
15PamenepoYeremiyaanatikwaZedekiya,Ndikakuuzani, simudzandiphakodi?ndipongatindikupatsauphungu, sundimveraIne?
+16ChoteromfumuZedekiyainalumbiriraYeremiya m’tseri,+kuti:“PaliYehova,+ameneanatipatsiramoyo umenewu,+sindidzakupha,kapenakukuperekam’manja mwaanthuameneakufunamoyowako
17PamenepoYeremiyaanauzaZedekiyakuti:“Yehova, Mulunguwamakamu,MulunguwaIsiraeliwanenakuti: Ukaturukandithukumkakwaakalongaamfumuyaku Babulo,moyowakoudzakhalandimoyo,ndimudziuwu sudzatenthedwandimoto;ndipomudzakhalandimoyo, ndinyumbayanu;
18Komaukapandakupitakwaakalongaamfumuya Babulo,mzindaunoudzaperekedwam’manjamwa Akasidi,+ndipoadzautenthandimoto,+ndipoinu simudzapulumukam’manjamwawo
+19NdiyenomfumuZedekiyaanauzaYeremiyakuti: “NdiopaAyudaameneagweram’manjamwaAkasidi,+ kutiangandiperekem’manjamwawon’kundiseka.
20KomaYeremiyaanati,SadzakuperekaiweMverani mauaYehovaamenendinenakwainu;
21Komaukakanakuturuka,mauameneYehova wandionetsandiawa:
22Ndipotaonani,akazionseotsalam’nyumbayamfumu yaYudaadzatulutsidwakwaakalongaamfumuyaku Babulo;
+23Choteroadzatulutsaakazianuonsendianaanukwa Akasidi,+ndipoinusimudzapulumukam’manjamwawo, +komamudzagwidwandidzanjalamfumuyakuBabulo, +ndipomudzatenthetsamzindaunondimoto
+24PamenepoZedekiyaanauzaYeremiyakuti:“Mawu amenewaasadziwemunthualiyense,+ndiposudzafa
25Komaakalongaakamvakutindinalankhulandiiwe, nadzakwaiwe,nadzatikwaiwe,Utiuzechimenewanena kwamfumu,usatibisire,ndipositikupha;ndiponsozimene mfumuinakuuzani
+26Pamenepouwauzekuti,‘Ndinaperekapembedzero langa+pamasopamfumu,kutiisandibwezerekunyumba yaJonatanikutindikaferekumeneko
27PamenepoakalongaonseanadzakwaYeremiya, namfunsa,ndipoiyeanawauzamongamwamauonseawa adauzamfumuNdipoanalekakulankhulanaye;pakuti sanazindikirikamlanduwo.
28ChoteroYeremiyaanakhalam’BwalolaAlonda+ mpakatsikulimeneYerusalemuanalandidwa,+ndipoiye analikumenekopameneYerusalemuanalandidwa.
MUTU39
1ChakachachisanundichinayichaZedekiyamfumuya Yuda,mweziwakhumi,Nebukadirezaramfumuyaku BabuloanadzandiankhondoakeonsekuYerusalemu, naumangiramisasa
2Ndipom’chakacha11chaZedekiya,mweziwachinayi, tsikulachisanundichinayilamweziwo,mzindawo unapasuka
3AkalongaonseamfumuyaBabuloanalowandikukhala pachipatachapakati,+amenendiNerigali-sarezere, Samugarinebo,Sarisekimu,Rabisarisi,Nerigali-sarezere Rabimagi,+pamodzindiakalongaenaonseamfumuya Babulo
4Ndipokunali,pameneZedekiyamfumuyaYuda anawaona,ndiamunaonseankhondo,anathawa,naturuka m’mudziusiku,njirayakumundawamfumu,pacipata pakatipamakomaaŵiri,naturukanjirayakuchigwa 5KomagululankhondolaAkasidilinawathamangitsa,+ ndipoanam’pezaZedekiya+m’zidikhazaYeriko,+ n’kumugwiran’kupitanayekwaNebukadinezaramfumu
Yeremiya
yaBabulokuRibila+m’dzikolaHamati,+kumene anam’weruza.
6PamenepomfumuyaBabuloinaphaanaaZedekiyaku Ribilapamasopake,ndipomfumuyaBabuloinaphanso audindoonseaYuda.
7NdipoanakolowolamasoaZedekiya,nammangandi maunyolo,kumtengerakuBabulo
8NdipoAkasidianatenthandimotonyumbayamfumu, ndinyumbazaanthu,nagumulampandawaYerusalemu
+9PamenepoNebuzaradani+mkuluwaasilikaliolondera mfumu+anatengaanthuameneanatsalamumzindawo n’kupitanawokuukapolokuBabulo,+ndiothawaamene anathawirakwaiyepamodzindianthuenaonseamene anatsala
10KomaNebuzaradanikapitaowaalondaanasiyam’dziko laYudaenaosaukaaanthu,ameneanalibekanthu, nawapatsamindayamphesandimindanthawiyomweyo
11TsopanoNebukadirezaramfumuyaBabuloanalamula Nebuzaradani+mkuluwaasilikaliolonderamfumu zokhudzaYeremiyakuti:
12Mtengeni,nimuyang’anirebwino,osamchitirachoipa; komauchitekwaiyemongaadzanenandiiwe.
+13ChoteroNebuzaradani+mkuluwaasilikaliolondera mfumu,+Nebusasibani,+Rabisarisi,+Nerigali-sarezere, +Rabimagi+ndiakalongaonseamfumuyaBabulo.
+14IwoanatumizaanthukukatengaYeremiyam’Bwalo laAndende+n’kumuperekakwaGedaliya+mwanawa Ahikamu,mwanawaSafani,+kutiapitenayekwawo,+ motianakhalapakatipaanthuwo
15NdipomauaYehovaanadzakwaYeremiyaali wotsekeredwam’bwalolakaidi,kuti;
16Pita,lankhulandiEbedi-MelekiMkusi,kuti,Atero Yehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli;Taonani, ndidzatengeramudziuwumauangakuucitirazoipa,si zabwino;ndipozidzakwaniritsidwatsikulimenelopamaso panu
17Komandidzakupulumutsatsikulimenelo,atiYehova, ndiposudzaperekedwam’manjamwaanthuameneuwaopa 18Pakutindidzakupulumutsandithu,ndiposudzaphedwa ndilupanga,komamoyowakoudzakhalachofunkhakwa iwe,chifukwawakhulupiriraIne,atiYehova
MUTU40
1MauameneanadzakwaYeremiyaocokerakwaYehova, atammasulaNebuzaradanikazembewaalondaaja kucokerakuRama,m’meneanamtengawomangidwa maunyolomwaonseotengedwandendeakuYerusalemu ndiYuda,ameneanatengedwandendekumkakuBabulo 2NdipokapitaowaalondaanatengaYeremiya,natikwa iye,YehovaMulunguwakowanenachoipaichipamalo ano.
3TsopanoYehovawachibweretsa,ndipowachitamonga ananena,chifukwamwachimwiraYehova,osamveramawu ake,chifukwachakechinthuichichakufikirani
4Ndipotsopano,taona,ndikumasulaleromaunyoloali padzanjalako.KukakukomerakunkananekuBabulo,tiye; ndipondidzakusamalirani,komangaticikuipiranikumuka nanekuBabulo,lekani;taona,dzikolonseliripamaso pako;
5Komaasanabwerere,anati,BweransokwaGedaliya mwanawaAhikamu,mwanawaSafani,amenemfumuya
kuBabuloinamikakukhalawolamuliramidziyaYuda,ndi kukhalanayepakatipaanthu;Choterokapitaowaalonda anampatsachakudyandimphotho,namlolaamuke
6PamenepoYeremiyaanapitakwaGedaliyamwanawa AhikamukuMizipa;nakhalanayepakatipaanthuotsala m’dzikomo
7Tsopanoakapitawoonseamaguluankhondoameneanali kuthengo,+iwondianthuawo,atamvakutimfumuya BabuloyaikaGedaliya+mwanawaAhikamukukhala bwanamkubwam’dzikolo,+n’kumuikiraamuna,akazi, ana,+ndianthuosaukaam’dzikolo,+amene sanatengedwekuukapolokuBabulo
8KenakoanafikakwaGedaliyakuMizipa,amenendi IsimaelimwanawaNetaniya,YohananindiYonatani,ana aKareya,SerayamwanawaTanumeti,anaaEfaiwaku Netofa,ndiYezaniyamwanawaMmaakati,iwondianthu awo
+9Gedaliya+mwanawaAhikamu+mwanawaSafani analumbirira+iwondianthuawokuti:“Musaope kutumikiraAkasidi
10Komaine,taonani,ndidzakhalakuMizipakutumikira Akasidi,ameneadzabwerakwaife;komasonkhanitsani vinyo,ndizipatsozamalimwe,ndimafuta,ndikuziika m’zotengerazanu,ndikukhalam’midziyanuimene mwalanda.
11Momwemonso,AyudaonseokhalakuMowabu,ndiana aAmoni,ndiEdomu,ndiokhalam’maikoonse,anamva kutimfumuyaBabuloyasiyaotsalaaYuda,ndikutiinaika GedaliyamwanawaAhikamu,mwanawaSafani, kuwatsogolera;
+12NgakhaleAyudaonseanabwererakuchokerakumalo onsekumeneanawathamangitsira+n’kupitakudzikola YudakwaGedaliyakuMizipa,+ndipoanasonkhanitsa vinyondizipatsozam’chilimwe+zambirimbiri.
13NdipoYohananimwanawaKareya,ndiakazembeonse amaguluankhondoameneanalikuthengo,anadzakwa GedaliyakuMizipa;
14Ndiyenoanamufunsakuti:“KodiukudziwakutiBaalisi +mfumuyaanaaAmonianatumizaIsimaeli+mwanawa Netaniyakutiadzakupha?KomaGedaliyamwanawa Ahikamusanawakhulupirira
15PamenepoYohananimwanawaKareyaananenandi Gedaliyam’tserikuMizipa,kuti,Ndilolenindipite ndikapheIsimaelimwanawaNetaniya,osadziŵamunthu aliyense;
+16KomaGedaliya+mwanawaAhikamuanauza YohananimwanawaKareyakuti:“Usachitezimenezi chifukwaumanamiziraIsimaeli.
MUTU41
1Ndipokunali,mweziwacisanundiciwiri,Ismayeli mwanawaNetaniya,mwanawaElisama,wambeu yacifumu,ndiakalongaamfumu,ndiwoanthukhumi pamodzinaye,anadzakwaGedaliyamwanawaAhikamu kuMizipa;+Kumenekoanadyachakudyapamodziku Mizipa.
2PamenepoIsimaelimwanawaNetaniya,ndiamuna khumiameneanalinaye,ananyamuka,naphaGedaliya mwanawaAhikamu,mwanawaSafani,ndilupanga, namuphaiyeamenemfumuyakuBabuloinamuika kukhalakazembewadziko
Yeremiya
3IsimaelianaphansoAyudaonseameneanalinaye,+ pamodzindiGedaliyakuMizipa,+Akasidiamene anapezekakumeneko,+ndiamunaankhondo
4NdipopanalitsikulachiwiriataphaGedaliya,ndipo palibeameneanadziwa.
+5AnabweraenaochokerakuSekemu,+kuSilo+ndiku Samariya,+amuna80atametedwandevu,+zovalazawo zong’ambika,+odzichekaokha+alindinsembe+ndi zofukiza+m’manjamwawo,kutiabwerenazokunyumba yaYehova
6NdipoIsimaelimwanawaNetaniyaanaturukakuMizipa kukakomananao,akulirapoyendaiye;ndipokunali, pokomananao,anatikwaiwo,IdzanikwaGedaliyamwana waAhikamu
7Ndipokunali,atafikapakatipamudzi,Ismayelimwana waNetaniyaanawapha,nawaponyam’katimwadzenje, iyendiamunaameneanalinaye
8Komapakatipawopanaliamuna10ameneanauza Isimaelikuti:“Musatiphe,+chifukwatilindichuma m’munda,tirigu,balere,mafutandiuchiChonchoadaleka, ndiposanawaphepamodzindiabaleawo
9TsopanodzenjelimeneIsimaelianaponyamomitembo yonseyaanthuameneanawaphachifukwachaGedaliya,+ ndilolimenemfumuAsainapangachifukwachoopaBaasa mfumuyaIsiraeli,ndipoIsimaelimwanawaNetaniya anadzazamondianthuophedwa
10PamenepoIsimaelianatengandendeanthuonseotsalaa kuMizipa,anaaakaziamfumu,ndianthuonseamene anatsalakuMizipa,ameneNebuzaradanimkuluwaalonda anawaperekakwaGedaliyamwanawaAhikamu; 11KomaYohananimwanawaKareya,ndiakazembeonse amaguluankhondoameneanalinaye,anamvazoipazonse zimeneIsmayelimwanawaNetaniyaanachita
12Kenakoanatengaamunaonsewon’kupitakukamenyana ndiIsimaelimwanawaNetaniya,ndipoanam’peza m’mphepetemwamadziambiriakuGibeoni
13TsopanoanthuonseameneanalindiIsimaeliataona YohananimwanawaKareyandiakuluakuluonseamagulu ankhondoameneanalinaye,anasangalala
14ChonchoanthuonseameneIsimaelianawatengaku Mizipaanatembenukan’kupitakwaYohananimwanawa Kareya
15KomaIsimaelimwanawaNetaniyaanathawapamodzi ndiamuna8kwaYohananindikupitakwaanaaAmoni
16PamenepoanatengaYohananimwanawaKareya,ndi akazembeonseankhondoameneanalinaye,otsalaonsea anthu,ameneanawalanditsakwaIsmayelimwanawa Netaniya,kuMizipa,ataphaGedaliyamwanawaAhikamu, amunaamphamvuankhondo,ndiakazi,ndiana,amene anabwezakwaGibeoni
17Ndipoanachoka,nakhalam’nyumbayaKimhamu,ili pafupindiBetelehemu,kutialowekuAigupto; +18ChifukwachaAkasidi,+chifukwaanalikuwaopa+ chifukwaIsimaelimwanawaNetaniyaanaphaGedaliya mwanawaAhikamu,amenemfumuyaBabuloinamuika kukhalabwanamkubwam’dzikolo
MUTU42
1Pamenepoakazembeonseankhondo,ndiYohanani mwanawaKareya,ndiYezaniyamwanawaHoshaya,ndi
anthuonse,kuyambirawamng'onokufikirawamkulu, anayandikira;
2NdipoanauzamneneriYeremiyakuti:“Pempherolathu livomerezekepamasopanu,+ndipomutipemphererekwa YehovaMulunguwanu+chifukwachaotsalaonsewa. (pakutitatsalaowerengekaokhaaambiri,mongamasoanu atipenya;)
3kutiYehovaMulunguwanuatisonyezenjiraimene tingayendemo,ndichimenetichite
4PamenepomneneriYeremiyaanatikwaiwo,Ndamva inu;taonani,ndidzapempherakwaYehovaMulunguwanu mongamwamauanu;ndipokudzali,kuticiriconse Yehovaadzakuyankhani,ndidzakudziwitsani; sindidzakubisiranikanthu
5NdipoiwoanatikwaYeremiya,Yehovaakhalemboni yowonandiyokhulupirikapakatipathu,tikapandakuchita mongamwazonseYehovaMulunguwanu adzakutumiziranikwaife
6Kayaaliabwinokapenaoipa,tidzamveramawua YehovaMulunguwathuamenetikutumizanikwaiye;+ kutizitikomere,+pomveramawuaYehovaMulungu wathu.
7Ndipopanaliatapitamasikukhumi,mawuaYehova anadzakwaYeremiya
8PamenepoanaitanaYohananimwanawaKareya,ndi akazembeonseamaguluankhondoameneanalinaye,ndi anthuonse,kuyambirawamng’onokufikirawamkulu;
9Ndipoanatikwaiwo,AteroYehova,Mulunguwa Israyeli,amenemunanditumakwainekutindipereke pembedzerolanupamasopake;
10Mukadzakhalabem’dzikolino,ndidzakumangani, osakupasula,ndidzakubzalani,osakuzulani;
11MusaopemfumuyakuBabulo,imenemukuiopa; musamuwope,atiYehova,pakutiInendilindiinukuti ndikupulumutsenindikukulanditsanim'dzanjalake
12Ndipondidzakuchitiranichifundo,kutiakuchitireniinu chifundo,ndikukubwezanikudzikolanu.
13Komamukadzati,Sitikhalam’dzikolino,kapena kumveramauaYehovaMulunguwanu;
14Nanena,Iyayi;komatidzalowam’dzikolaAigupto, kumenesitidzawonankhondo,sitidzamvakulirakwa lipenga,kapenakukhalandinjalayamkate;ndipo tidzakhalakomweko;
15TsopanoimvanimawuaYehova,inuotsalaaYuda; AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Mukalunjikitsakonsenkhopezanukulowam’Aigupto,ndi kupitakukakhalakumeneko;
+16Pamenepokudzachitikakutilupanga+limene munaliopalidzakupezanikumenekom’dzikolaIguputo,+ ndiponjalaimenemunaiopaidzakutsatiranikumenekoku Iguputondipomudzaferakomweko
17Ndipokudzakhalakwaamunaonseamenealozankhope zaokulowam’Aiguptokukakhalakumeneko;adzafandi lupanga,ndinjala,ndimliri;ndipopalibendimmodzi yemweameneadzatsalekapenakupulumukakuzoipa zimenendidzawatengera
18PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; Mongamkwiyowangandiukaliwangazatsanuliridwapa okhalam'Yerusalemu;momwemoukaliwanga udzathiridwapainu,pakulowam’Aigupto;ndipo simudzaonansomaloano
Yeremiya
19Yehovawanenazainu,otsalaaYuda;musapiteku Aigupto;dziwanindithukutindakulangizanilero. 20Pakutimunadzinyengam’mitimayanu,+pamene munanditumakwaYehovaMulunguwanundikuti, ‘TipemphererekwaYehovaMulunguwathu;+ndizonse zimeneYehovaMulunguwathuadzanena,mutiuze momwemo,ndipotidzachichita 21Ndipolerondakudziwitsani;komasimunamveramaua YehovaMulunguwanu,kapenaciriconseananditumakwa inu
22Tsopanodziwanindithukutimudzafandilupanga,+ njala,+mliri,+kumalokumenemukufunakupitakondi kukhalangatialendo.
MUTU43
1Ndipokunali,Yeremiyaatathakunenakwaanthuonse mauonseaYehovaMulunguwao,ameneYehova Mulunguwaoanamtumakwaiwo,ndiwomauawaonse; 2PamenepoAzariyamwanawaHosaya,ndiYohanani mwanawaKareya,ndianthuonseonyada,ananenandi Yeremiya,kuti,Wanenazonama;
3KomaBarukimwanawaNeriyaakukukakamizanikuti atiperekem’manjamwaAkasidi,+kutiatiphe+ndi kutitengerakuukapolokuBabulo.
4PamenepoYohananimwanawaKareya,ndiakazembe onseankhondo,ndianthuonsesanamveramauaYehova, kutiakhalem’dzikolaYuda.
+5KomaYohanani+mwanawaKareya+ndiakuluakulu onseamaguluankhondoanatengaotsalaonseaYuda ameneanabwererakuchokerakumitunduyonseyaanthu kumeneanawathamangitsira+kutiakakhalem’dzikola Yuda
6amuna,akazi,ana,ndianaaakaziamfumu,ndimunthu aliyenseameneNebuzaradanimkuluwaasilikaliolondera mfumuanasiyandiGedaliyamwanawaAhikamumwana waSafani,Yeremiyamneneri,ndiBarukimwanawa Neriya
7ChoteroanafikakudzikolaIguputo,+chifukwa sanamveremawuaYehova,ndipoanafikakuTapanesi.
8PamenepomauaYehovaanadzakwaYeremiyaku Tapanesi,kuti,
9Tengamiyalaikuluikulum’dzanjalako,nuibisem’dothi m’kuwombanjerwa,kumenekulipakhomolanyumbaya FaraokuTapanesi,pamasopaanthuaYuda; 10Ndipouwauzekuti,Yehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli,atero;Taonani,ndidzatumizandikutenga NebukadirezaramfumuyakuBabulo,mtumikiwanga,ndi kuikampandowakewachifumupamiyalaiyindinayibisa; ndipoadzayalachihemachakechachifumupamwamba pawo
11Ndipoakadzafika,adzakanthadzikolaAigupto, nadzaperekawoyeneraimfakuimfa;ndiiwoamene ayenerakutengedwaukapolo;ndiamenealialupangaaphe lupanga
12Ndipondidzasonkhamotom’nyumbazamilunguya Aigupto;ndipoadzawatentha,nadzawatengandende;ndipo adzatulukam’menemondimtendere
13AdzathyolansomafanoakuBetesemesi,ameneali m’dzikolaAigupto;ndinyumbazamilunguyaAigupto adzazitenthandimoto
MUTU44
1MauameneanadzakwaYeremiyaponenazaAyudaonse okhalam’dzikolaAigupto,okhalakuMigidoli,ndi Tapanesi,ndiNofi,ndim’dzikolaPatirosi,kuti:
2AteroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; MwaonazoipazonsendinatengeraYerusalemu,ndimidzi yonseyaYuda;ndipotaonani,leroalibwinja,ndipo mulibemunthuwokhalamo;
+3Chifukwachazoipazimeneanachitakutiandikwiyitse, +popitakukafukiza+ndikutumikiramilunguina,+imene iwosanaidziwe,+inuyokapenamakoloanu
4Komandinatumizakwainuatumikiangaonseaneneri, ndikalawiram’mamawandikuwatuma,ndikuti,Musachite chonyansaichichimenendidananacho
5Komaiwosanamvere,kapenakutcherakhutulawokuti asiyezoipazawo,osafukizansembekwamilunguina
6Cifukwacaceukaliwangandiukaliwanga unatsanulidwa,nuyakam'midziyaYudandim'miseuya Yerusalemu;ndipoalibwinjandibwinja,mongalerolino 7CifukwacacetsopanoateroYehova,Mulunguwa makamu,MulunguwaIsrayeli;Cifukwacacemucitira moyowanucoipacacikuruici,kukucotseranimwainu mwamunandimkazi,ndimwanandiwoyamwam’Yuda, kutiasakusiyirenimmodziwotsala;
8Munandikwiyitsandintchitozamanjaanu,+pofukizira zofukizakwamilunguina+m’dzikolaIguputo,+kumene munapitakokutimukhalemo,+kutimudziwononge+kuti mukhaletemberero+ndichitonzopakatipamitunduyonse yapadzikolapansi?
9Kodimwaiwalazoipazamakoloanu,ndizoipaza mafumuaYuda,ndizoipazaakaziawo,ndizoipazanu, ndizoipazaakazianu,zimeneanachitam’dzikolaYuda, ndim’misewuyaYerusalemu?
10Sanadzichepetsakufikiralerolino,sanaope,kapena kuyendam’cilamulocanga,kapenam’malembaanga, amenendinaikapamasopanundipamasopamakoloanu.
11CifukwacaceateroYehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli;Taonani,ndidzakulozeraniinuchoipa,ndikupha Yudayense.
12NdipondidzatengaotsalaaYuda,ameneanaloza nkhopezaokulowam’dzikolaAiguptokukakhala kumenekomongaalendo;indeadzathedwandilupangandi njala;adzafa,kuyambirawamng’onokufikirawamkulu, ndilupangandinjala;ndipoadzakhalachotembereredwa, ndichodabwitsa,ndichotembereredwa,ndichitonzo. 13Pakutindidzalangaiwookhalam’dzikolaIgupto, mongandinalangiraYerusalemu,ndilupanga,ndinjala, ndimliri;
14koterokutipasakhalemmodziwaotsalaaYuda,amene analowam’dzikolaAiguptokukakhalakumeneko,amene adzapulumukakapenakutsala,kutiabwererekudzikola Yuda,kumeneakufunakubwererakukakhalakumeneko: pakutipalibeameneadzabwerera,komawopulumuka 15Pamenepoamunaonseameneanadziwakutiakaziawo anafukiziramilunguina,ndiakazionseamene anaimirirapo,khamulalikulu,ndianthuonseokhala m’dzikolaAigupto,kuPatirosi,anayankhaYeremiya,kuti: 16Komamawuamenemwatiuzam’dzinalaYehova sitikumverani.
17Komatidzachitadichirichonsechiturukam’kamwa mwathu,kufukizachofukizakwamfumukazi
Yeremiya
yakumwamba,ndikuithiriransembezothira,monga tinachitiraife,ndimakoloathu,mafumuathu,ndiakalonga athu,m’midziyaYuda,ndim’makwalalaaYerusalemu; +18Komakuyambirapamenetinasiyakufukiza+ zofukiza+kwamfumukaziyakumwamba+ndikuithirira nsembezothira,+tasowazinthuzonse,+ndipotathedwa ndilupanga+ndinjala
19Mwomwoikatwatelakufwelelangwetuvatuvavavulu vejikwivwangakuwaha,kahatwatelakutachikiza ngachilihivyumavizenavimulingisatupwenga vakuwahilila?
20PamenepoYeremiyaanauzaanthuonse,amuna,akazi, ndianthuonseameneanamuyankhakuti:
21Zofukizazimenemunafukizam’mizindayaYudandi m’misewuyaYerusalemu,+inundimakoloanu,mafumu anu,+akalongaanundianthuam’dzikolo,kodiYehova sanazikumbukire,ndiposizinalowem’maganizomwake?
+22Yehovasanathensokupirirachifukwachazochita zanuzoipa+ndiponsochifukwachazonyansazimene munazichitachifukwachakedzikolanulasandukabwinja, ndichodabwitsa,nditemberero,lopandawokhalamo, mongalerolino.
+23Popezamwafukizazofukiza,+chifukwa munachimwiraYehova,+osamveramawuaYehova,+ simunayendem’chilamulochake,+malamuloake,+ mbonizake,+24chifukwachazimenemwachitazo chifukwachakechoipaichichakugweranimongalerolino 24Yeremiyaananenansokwaanthuonse,ndikwaakazi onse,ImvanimawuaYehova,inuAyudaonseokhala m’dzikolaAigupto
25Yehovawamakamu,MulunguwaIsiraeliwanenakuti: Inundiakazianumunalankhulandipakamwapanu,ndipo mwakwaniritsandidzanjalanu,kuti,Tidzakwaniritsadi zowindazathuzimenetinalumbirira,kufukizachofukiza kwamfumukaziyakumwamba,ndikuithiriransembe zothira;
26ChifukwachakeimvanimawuaYehova,inuAyuda onseokhalam’dzikolaAigupto;Taonani,ndalumbirapa dzinalangalalikulu,atiYehova,kutidzinalanga silidzatchulidwansom'kamwamwamunthualiyensewa Yudam'dzikolonselaAigupto,kuti,PaliYehovaMulungu 27Taonani,ndidzawayang’anirandikuwachitirachoipa, osatikuwachitirazabwino;
28Komaowerengekaopulumukalupangaadzabwera kuchokeram’dzikolaIguptokunkakudzikolaYuda;
29Ndipoichichidzakhalachizindikirokwainu,ati Yehova,kutindidzakulanganim’malomuno,+kuti mudziwekutimawuangaadzakuikiranindithukuti akuchitirenichoipa
30AteroYehova;Taonani,ndidzaperekaFaraoHofra mfumuyaAiguptom'dzanjalaadaniace,ndim'dzanjala iwoakufunamoyowace;mongandinaperekaZedekiya mfumuyaYudam’dzanjalaNebukadirezaramfumuyaku Babulo,mdaniwake,ameneanafunamoyowake
MUTU45
1MauameneYeremiyamnenerianauzaBarukimwanawa Neriya,pameneiyeanalembamawuawam’bukupakamwa paYeremiya,m’chakachachinayichaYehoyakimu+ mwanawaYosiyamfumuyaYuda,kuti: 2Yehova,MulunguwaIsrayeli,aterokwaiwe,Baruki;
3Iweunati,Tsokainetsopano!pakutiYehova wawonjezerachisonipachisonichanga;Ndinakomoka pobusamoyowanga,ndiposindipezampumulo
4Ukaterokwaiye,AteroYehova;Taonani,chimene ndamangandidzachipasula,ndichimenendabzala, ndidzachizula,ndilodzikoililonse
5Ndipoudzifunirawekhazazikulu?usawafunefune:pakuti, taona,ndidzatengeracoipapaanthuonse,atiYehova;
MUTU46
1MauaYehovaameneanadzakwaYeremiyamneneri motsutsanandiamitundu;
+2PaIguputo+ndigululankhondolaFarao-neko+ mfumuyaIguputo,+limenelinalipafupindimtsinjewa FiratekuKarikemisi,+limeneNebukadirezaramfumuya Babuloanakantham’chakachachinayichaYehoyakimu+ mwanawaYosiyamfumuyaYuda
3Konzanichikopandizikopa,ndipoyandikirani kunkhondo
4Manganiakavalo;ndipokwerani,inuapakavalo, nimuimirirendizisotizanu;konzanimikondo,ndikuvala zingwe
5N’chifukwachiyanindawaonaalindimanthandipo abwereram’mbuyo?ndipoamphamvuaoaphwanyidwa, nathawa,osayang'anam'mbuyo,pakutimanthaanali ponseponse,atiYehova
6Aliwiroasathawe,ngakhalewamphamvuasapulumuke; +Iwoadzapunthwa+n’kugwerakumpotokumtsinjewa Firate
7Ndaniuyuameneakukwerangatimtsinje,amenemadzi akeamayendangatimitsinje?
8Ejipitoaukangatimtsinje,ndipomadziake akugwedezekangatimitsinje;nati,Ndidzakwera, ndidzaphimbadzikolapansi;ndidzawonongamzindawo ndiokhalamo
9Kwerani,inuakavalo;ndikukwiya,magaretainu;ndi amphamvuatuluke;AetiopiandiAlibiya,akunyamula zikopa;ndiAludia,akugwirandikupindauta
10PakutiilinditsikulaYehova,Yehovawamakamu, tsikulakubwezera,kutiabwezerecilangokwaadaniake; ndipolupangalidzadya,lidzakhutandikuledzerandi mwaziwao;pakutiAmbuyeYehovawamakamualindi nsembem’dzikolakumpotopamtsinjewaFirate
11KwerakuGileadi,ukatengemvunguti,namwaliiwe, mwanawamkaziwaAigupto;pakutisimudzachiritsidwa.
12Amitunduamvazamanyaziako,ndipokulirakwako kwadzazadzikolapansi;
13MawuameneYehovaanauzamneneriYeremiya,+kuti NebukadirezaramfumuyaBabuloadzabwerakudzakantha dzikolaIguputo
14NenanimuIgupto,lengezanikuMigidoli,lalikiraniku NofindikuTapanesi;pakutilupangalidzadyapozungulira iwe
15N'chifukwachiyaniolimbamtimaakokolokedwa? sanayime,popezaYehovaanawaingitsa
16Iyeanagwetsaambiri,inde,winaanagwapamnzake; 17Ndipoanapfuulakumeneko,FaraomfumuyaAigupto aliphokoso;wadutsanthawiyoikika
18PaliIne,wateroMfumu,dzinalakeYehovawamakamu, ndithumongaTaborialipakatipamapiri,ndingati Karimelim’mphepetemwanyanja,momwemoadzafika
19Iwemwanawamkaziwokhalam’Aigupto,dzikonzere kunkakundende;
20Aiguptoalingating’ombeyaikaziyokongolandithu; imachokerakumpoto.
21Ndiponsoaganyuakealipakatipakengating’ombe zonenepa;pakutiiwonsoabwereram’mbuyo,nathawa pamodzi;
22Mawuakeadzayendangatinjoka;pakutiadzayendandi khamulankhondo,nadzamdzerandinkhwangwa,monga otemankhuni
23Iwoadzadulankhalangoyake,’+wateroYehova, ngakhalekutisiifufuzidwachifukwaachulukakuposa ziwala,ndipoaliosawerengeka.
24MwanawamkaziwaAiguptoadzakhalandimanyazi; adzaperekedwam’manjamwaanthuakumpoto
25Yehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli,atero; Taonani,ndidzalangaaunyinjiwaNo,ndiFarao,ndi Aigupto,ndimilunguyao,ndimafumuao;ngakhaleFarao, ndionseakukhulupiriraIye;
+26Ndidzawaperekam’manjamwaameneakufunamoyo wawo+ndim’manjamwaNebukadirezaramfumuya Babulo+ndim’manjamwaatumikiake,+pambuyopake anthuwoadzakhalamongatimasikuakale,”+watero Yehova
27Komausaope,iweYakobomtumikiwanga,usachite mantha,iweIsrayeli;ndipoYakoboadzabwera,nadzakhala mumpumulondimwamtendere,ndipopalibewakumopsa 28Usaope,iweYakobomtumikiwanga,atiYehova, pakutiInendilindiiwe;pakutindidzatheraamitunduonse kumenendinakuingitsirakoiwe;komasindidzakusiya wosalangakonse.
MUTU47
1MauaYehovaameneanadzakwaYeremiyamneneri ponenazaAfilisti,FaraoasanakantheGaza
2AteroYehova;Taonani,madziakwerakuchokera kumpoto,adzakhalachigumula,nadzamizadzikondizonse zirim'mwemo;mudzi,ndiiwookhalamo;pamenepoanthu adzalira,ndionseokhalam’dzikoadzalira.
3Paphokosolakupondakwazibodazaakavaloake amphamvu,ndikuthamangakwamagaletaake,ndi mkokomowanjingazake,+atatesadzayang’anam’mbuyo kwaanaawochifukwachakulefukakwamanjaawo; +4Chifukwachatsikulimenelikubwerakudzafunkha+ Afilisiti+onse,+ndikupham’TurondikuSidoni wothandizaaliyensewotsala,+pakutiYehovaadzafunkha +Afilisiti+otsalaam’dzikolaKafitori.
5DazilafikapaGaza;Asikeloniwadulidwapamodzindi otsalaam'chigwachawo;mudzadzichekakufikiraliti?
6OlupangalaYehova,udzakhalampakalitikukhalachete? dziikirewekham’chokwakwachako,puma,nutonthole.
7Kodiungakhalechetebwanji,popezaYehovawaupereka lamulolokhudzaAsikelonindigombelanyanja? pamenepoadauika
MUTU48
1PaMoabuateroYehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli;TsokakwaNebo!pakutiwapasuka;Kiriataimu wachititsidwamanyazi,walandidwa;Misigabuwachita manyazi,wachitamantha
2SipadzakhalansokutamandidwakwaMoabu;tiyeni, tiulikhane,lisakhalensomtundu.Ndipoudzadulidwa,iwe Madimeni;lupangalidzakulondola
+3Mawuakufuula+adzamvekakuchokeraku Horonaimu,+kufunkhandikuwonongakwakukulu.
4Moabuwawonongedwa;ang'onoakeamvekakulira
5Pakutim’chitundachaLuhitimudzakwerakulira kosalekeza;pakutipakutsikirakwaHoronaimuadaniamva kulirakwachiwonongeko
6Thawani,pulumutsanimiyoyoyanu,khalaningati chitsambacham’chipululu
+7Pakutichifukwachakutiwadalirantchitozako+ndi chumachako,+iwensoudzagwidwa,+ndipoKemosi+ adzapitakuukapolopamodzindiansembeakendi akalongaake
8Wofunkhaadzafikapamidziyonse,ndipopalibemudzi udzapulumuka;
+9PerekanimapikokwaMowabu+kutiathaŵendi kuthawa,+pakutimizindayakeidzakhalabwinja,+moti mulibewokhalamo
10WotembereredwaiyeameneachitantchitoyaYehova monyenga,ndiwotembereredwaiyeameneabweza lupangalakekumwazi
11Moabuwakhalawodekhakuyambiraubwanawake, wakhalapamitsengayake,sanatsanulidwechotengeraku chiwiya,sanapitekuukapolo;
12Cifukwacace,taonani,masikuadza,atiYehova,amene ndidzamtumiziraosokera,ameneadzamsokeretsa, nadzakhuthulaziwiyazace,ndikuswamabotoloao
+13MowabuadzachitamanyazichifukwachaKemosi,+ mongammenenyumbayaIsiraeliinachitiramanyazindi Betelichifukwachachikhulupirirochawo
14Mukutibwanji,Ndifeamphamvundiamphamvu kunkhondo?
15Moabuwafunkhidwa,+ndipowatulukam’mizinda yake,+ndipoanyamataakeosankhidwamwapadera atsikirakukaphedwa,”+wateroMfumu,amenedzinalake ndiYehovawamakamu
16TsokalaMowabulayandikira,ndipotsokalake lifulumira.
17Inunonseamenemukumzinga,m’lirenichisoni;ndipo inunonseamenemudziwadzinalace,nenani,Yathyoka bwanjindodoyolimba,ndindodoyokongola!
18IwemwanawamkaziwokhalakuDiboni,tsikapa ulemererowako,nukhalendiludzu;pakutiwofunkha Mowabuadzakugwerani,nadzaonongamalingaanu.
19IwewokhalakuAroeri,imanim’njira,nuwone;funsani wothawayo,ndiwopulumukayo,ndikuti,Chachitika n’chiyani?
20Moabuwachitamanyazi;pakutiwapasuka;lirani mofuula;munenekuArinoni,kutiMoabuwapasuka; 21Ndipochiweruzochafikiradzikolachidikha;paHoloni, ndipaYahaza,ndipaMefaati; 22ndipaDiboni,ndipaNebo,ndipaBeti-dibulataimu; 23ndipaKiriyataimu,ndipaBeti-gamuli,ndipa Betemeoni; 24ndipaKerioti,ndipaBozira,ndipamidziyonseya dzikolaMowabu,yakutalikapenayapafupi
25NyangayaMowabuyadulidwa,+ndipodzanjalake lathyoledwa,”+wateroYehova.
26Muledzeretseni,pakutianadzikuzapamasopaYehova;
27KodiIsrayelisanalichonyozekakwainu?Kodi adapezekamwaachifwamba?pakutikuyambirapamene unayankhulazaiye,unalumphandichisangalalo
+28Inuokhalam’Mowabu,siyanimizinda+ndikukhala m’thanthwe,+ndipomukhalengatinjiwaimeneimamanga chisanjachakem’mbalimwapakamwapadzenje
29TamvakudzikuzakwaMowabu,kudzikuzakwake, kudzikuzakwake,kunyadakwake,ndikudzikuzakwa mtimawake
30Ndidziwamkwiyowake,atiYehova;koma sikudzakhalachomwecho;mabodzaakesadzatero
31CifukwacacendidzaliraMowabu,ndikuliriraMoabu yense;mtimawangauliriraanthuakuKiheresi.
32IwempesawakuSibima,ndidzakuliriraiwendikulira kwaYazeri;nthambizakozinaolokanyanja,mpakaku nyanjayaYazeri;
33Kukondwandikukondwazachotsedwam’mundawa zipatsozambiri,ndim’dzikolaMoabu;ndipondaletsa vinyom’zoponderamomphesa;kufuulakwawo sikudzakhalakufuula
+34KuyambirakufuulakwaHesiboni+mpakakuEleale +ndikuYahazi+analankhulamawuawo,+kuyambiraku Zowari+mpakakuHoronaimu,+ngating’ombeyaikazi yazakazitatu,+pakutimadziakuNimurimu+adzakhala mabwinja.
+35“Ndidzathetsansom’Mowabu,”+wateroYehova, “iyeameneamaperekansembepamalookwezeka,+ndi wofukiziramilunguyake.
36CifukwacacemtimawangaudzaliriraMowabungati zitoliro,ndipomtimawangaudzaliriraanthuakuKiheresi ngatizitoliro;
37Pakutimutuuliwonseukhalewadazi,ndindevuzonse zametedwa;
+38PamadengaonseanyumbazaMowabu+ndi m’misewuyakepadzakhalamaliro+chifukwa ndaphwanyaMowabungatichiwiyachosasangalatsa,”+ wateroYehova.
39Adzakuwa,ndikuti,Wagwetsedwabwanji!Moabu wabwereram'mbuyondimanyazi!moteroMoabu adzakhalachoseketsandichochititsamanthakwaonse omuzungulira
40PakutiateroYehova;Taonani,iyeadzaulukangati mphungu,ndipoadzatambasulamapikoakepaMoabu.
41Keriotiwalandidwa,ndimaloachitetezoadabwa,ndi mitimayaanthuamphamvuakuMowabutsikulimenelo idzakhalangatimtimawamkaziamenealindizowawa zake
42Mowabuadzawonongedwakutiasakhalensomtunduwa anthu,+chifukwawadzikuzapamasopaYehova
43Mantha,dzenje,ndimsamphazidzakugwera,iwe wokhalam’Mowabu,”+wateroYehova
44Wothawamanthaadzagwam’dzenje;ndipoiyeamene atulukam’dzenjeadzakodwamumsampha,+pakuti ndidzabweretsapaMowabu,+chakachakuwalanga,”+ wateroYehova
45OthawaanaimapansipamthunziwaHesibonichifukwa chankhondo;komamotoudzaturukakuHesiboni,ndilawi lamotopakatipaSihoni,nunyeketsangondyayaMoabu, ndinsongayamituyaanthuachiwawa
46TsokaiweMowabu!+anthuaKemosi+atha,+ chifukwaanaakoaamunaatengedwandende,+ndiana akoaakaziatengedwakuukapolo
+47Komam’masikuotsirizandidzabwezansoundendewa Mowabu,”+wateroYehova.Kufikirapanochiweruzocha Moabu
MUTU49
1PonenazaanaaAmoni,ateroYehova;KodiIsrayeli alibeana?alibewolowanyumba?Nangamfumuyao ilowanjiGadi,ndianthuaceakukhalam'midzimwace bwanji?
+2Choterotaonani,masikuakubwera,”+wateroYehova, ‘amenendidzamveketsaphokosolankhondo+muRaba+ waanaaAmoni.ndipolidzakhalamuluwabwinja,ndiana akeaakaziadzatenthedwandimoto;
3Lira,iweHesiboni,pakutiAiwapasuka;lirani,anaakazi aRaba,dzimangiraniziguduli;malirani,thamanganiuku ndiukom’malinga;pakutimfumuyaoidzankakundende, ndiansembeakendiakalongaakepamodzi
4Udzitamabwanjim’zigwa,m’cigwacamadzioyenda, iwemwanawamkaziwobwereram’mbuyo?amene anakhulupirirachumachake,kuti,AdzafikakwaInendani?
5Taona,ndidzakutengeramantha,atiAmbuyeYehovawa makamu,ochokerakwaonseakuzunguliraiwe;ndipo mudzaingitsidwayensepanja;ndipopalibe adzasonkhanitsawosochera.
6Pambuyopakendidzabwezansoundendewaanaa Amoni,”+wateroYehova
7PonenazaEdomu,Yehovawamakamuwanenakuti; KodikuTemanikulibensonzeru?uphunguwathakwa anzeru?nzeruzawozatha?
8Thawani,bwererani,khalanimwakuya,inuokhalaku Dedani;pakutindidzatengeratsokalaEsaupaiye,nthawi imenendidzamlanga
9Akadzakwainuotcheramphesa,sadzasiyakhunkhalina? ngatiakubausiku,adzawonongakufikiraatakwanira
10KomandabvulaEsau,ndavundukulamaloaceobisika, ndiposakhozakubisala;
11Siyaanaakoamasiye,Inendidzawasungaamoyo;ndipo amasiyeakoandikhulupirireIne
12PakutiateroYehova;Taonani,iwoamenechiweruzo chawosichinalichakumwachachikhoadamwandithu; ndipoiwendiweameneudzakhalawosalangidwakonse? sudzakhalawosalangidwa,komaudzamwakondithu.
13Pakutindalumbirapainendekha,atiYehova,kuti Boziraadzakhalabwinja,chitonzo,bwinja,nditemberero; ndimidziyaceyonseidzakhalamabwinjakosatha.
14NdamvamphekeserazochokerakwaYehova,+ndipo mthengawatumidwakwaanthuamitunduina+kuti, ‘Sonkhananipamodzi,mumuukirendikuwukira kunkhondo
15Pakutitaona,ndidzakuyesawamng’onomwaamitundu, ndiwonyozekamwaanthu.
16Kuopsakwakokukunyenga,ndikudzikuzakwamtima wako,iwewokhalam’mapangaathanthwe,amene ukhazikikapamwambapaphiri;
17NdipoEdomuadzakhalabwinja;
18MongammeneanapasulidwaSodomundiGomorandi midziyoyandikananayo,atiYehova,palibemunthu adzakhalammenemo,ngakhalemwanawamunthu adzakhalammenemo.
19Taonani,iyeadzakwerangatimkangowochokera kuphirilaYorodanokunkakumalookhalaamphamvu,
Yeremiya
komamodzidzimutsandidzam’thamangitsa;pakutiafanana ndiinendani?ndipondaniadzandiikirainenthawi?ndipo mbusaameneadzaimapamasopangandani?
20ChonchoimvaniuphunguwaYehovaumene wakonzeraEdomu;ndizolingalirazacezimene anazingiriraokhalakuTemani:Zoonadi,ang'onoazoweta adzakokaiwo;
21Dzikolapansiligwedezekandimkokomowakugwa kwao,ndimkokomowaceunamvekam'NyanjaYofiira
22Taonani,adzakweranadzaulukirangati chiwombankhanga,nadzatambasuliramapikoakepa Bozira;
23ZaDamasiko.+Hamati+ndiAripadi+achitamanyazi +chifukwaamvauthengawoipapalichisonipanyanja; sichingakhalechete
24Damasikowafooka,watembenukakutiathawe,ndipo manthaamgwira;zowawandizowawazamugwirangati mkaziwobala
25Kodimzindawamatamandosunasiyidwebwanji, mzindawachisangalalochanga!
26Choteroanyamataakeadzagwam’makwalalaake,+ ndipoamunaonseankhondoadzaphedwatsikulimenelo,” +wateroYehovawamakamu
27NdidzayatsamotopakhomalaDamasiko,ndipo udzanyeketsanyumbazachifumuzaBeni-hadadi.
+28PonenazaKedara+ndimaufumuakuHazori+ ameneNebukadirezaramfumuyaBabuloanawakantha,+ Yehovawanenakuti:Nyamukani,kweranikuKedara,ndi kufunkhaanthuakum'mawa
29Mahemaaondizowetazaoadzazilanda;adzadzitengera nsaruzotchingazao,ndizotengerazaozonse,ndingamila zao;ndipoadzafuulirakwaiwo,Manthaaliponseponse
30Thawani,thamangiranikutali,khalanimozama,inu okhalam’Hazori,”+wateroYehova.pakuti NebukadirezaramfumuyakuBabulowakupangiraniupo, ndipowakupangiraniciwembu
31Nyamukani,kweranikumtunduwolemereka,umene ukukhalamosasamala,atiYehova,umeneulibezitseko kapenamipiringidzo,wokhalapaokha
32Ngamilazawozidzafunkhidwa,ndizowetazawo zambirizidzafunkha;+Ndidzabweretsatsokalawo kuchokerakumbalizonse,”+wateroYehova
33NdipoHazoriadzakhalamokhalaankhandwe,ndi bwinjakosatha;
34MawuaYehovaameneanadzakwamneneriYeremiya ponenazaElamu+kumayambirirokwaufumuwa ZedekiyamfumuyaYuda,kuti:
35AteroYehovawamakamu;Taonani,ndidzathyolauta waElamu,mutuwamphamvuzao
36NdipopaElamundidzabweretsamphepozinayi kuchokerakumalekezeroanayiakumwamba,+ndipo ndidzabalalitsaiwokumphepozonsezo;ndipo sipadzakhalamtundukumeneopirikitsidwaaElamu sadzafikako
+37NdidzachititsaElamukuchitamanthapamasopa adaniawo+ndipamasopaameneakufunamoyowawo,+ ndipondidzawabweretseratsoka,mkwiyowangawoyaka moto,”+wateroYehovandipondidzatumizalupanga pambuyopao,kufikiranditawatha;
38NdipondidzaikampandowangawachifumukuElamu, +ndipondidzawononga+kumenekomfumundiakalonga,” +wateroYehova
39Komam’masikuotsirizandidzabwezansoundendewa Elamu,”+wateroYehova.
MUTU50
1MauameneYehovaanalankhulamotsutsanandiBabulo ndidzikolaAkasidimwamneneriYeremiya
2Nenanimwaamitundu,lengezani,kwezanimbendera; lengezani,ndipomusabise;nenani,Babulowalandidwa, Beliwachititsidwamanyazi,Merodakiwathyoledwa; mafanoakeachitamanyazi,mafanoakeaphwanyidwa 3Pakutimtunduwaanthuukudzerakumpoto kudzamenyananaye,umeneudzasandutsadzikolake bwinja,lopandawokhalamo;iwoadzasamuka,adzachoka, anthundinyama
4M’masikuamenewondinthawiimeneyo,’+watero Yehova,‘anaaIsiraelindianaaYudaadzabwerapamodzi, akuyendandikulira,+ndipoadzapitakukafunafuna YehovaMulunguwawo.
5AdzafunsanjirayaZiyoni,nkhopezaozikuyang’ana komweko,ndikuti,Tiyeni,tidziphatikekwaYehova m’panganolosatha,limenesilidzaiwalika.
6Anthuangaakhalankhosazosokera,abusaao awasokeretsa,asokeretsaiwopamapiri;
7Onseameneanawapezaanawadya,+ndipoadaniawo anati,‘Ifesitilakwa,+chifukwaanachimwiraYehova, malookhalamochilungamo,+Yehova,chiyembekezocha makoloawo.
8ChokanipakatipaBabulo,tulukanim’dzikolaAkasidi, +mukhalengatimbuzi+patsogolopazoweta
9Pakuti,taonani,ndidzautsandikutengeraBabiloni khamulamitunduikuluikuluyochokeram’dzikola kumpoto;Kumenekoadzatengedwa:miviyaoidzakhala ngatiyangwaziyanzeru;palibeameneadzabwerera pachabe
10NdipodzikolaKasidiadzakhalacofunkha; 11Chifukwamunakondwera,chifukwamudakondwera, inuowonongacholowachanga,chifukwamwanenepa ngating’ombeyaikazipaudzu,ndikulirangating’ombe; 12Mayianuadzakhalandimanyazikwambiri;iyeamene anakubalaniadzachitamanyazi:taonani,womalizirawa amitunduadzakhalachipululu,dzikolowuma,ndi chipululu.
13ChifukwachamkwiyowaYehovasipadzakhalanso anthu,komalidzakhalabwinja;
14DzikonzerenikumenyanandiBabulomomzungulira; inunonseakungautamumponyere,osasiyamivi;pakuti wachimwiraYehova.
15Fuulanimomuzunguliramozungulira,waperekadzanja lake,mazikoakeagwa,makomaakeagwetsedwa;pakuti ndikubwezerachilangokwaYehova;mongaadachita, mumchitireiye.
+16ChotsaniwofesakuBabulo+ndiwogwiritsantchito chikwakwa+panthawiyokolola,+chifukwachakuopa lupangalosautsa+aliyenseadzatembenukirakwaanthu ake,+ndipoaliyenseadzathawirakudzikolakwawo 17Israyelindinkhosayobalalika;mikangoyamuingitsa: choyambamfumuyaAsuriyamudya;ndipopomalizira pakeNebukadirezaramfumuyakuBabulowathyola mafupaake.
Yeremiya
18CifukwacaceateroYehovawamakamu,Mulunguwa Israyeli;Taonani,ndidzalangamfumuyakuBabulondi dzikolace,mongandinalangamfumuyaAsuri
+19NdidzabweretsansoIsiraelikumaloakeokhalamo,+ ndipoadzadyapaKarimelindikuBasana,+ndipomoyo wakeudzakhuta+pamapiriaEfuraimu+ndiGiliyadi
20M’masikuamenewondinthawiimeneyo,’+watero Yehova,+cholakwachaIsiraelichidzafunidwa,koma sichidzapezeka;+ndimachimoaYuda,+koma sadzapezeka,+pakutindidzakhululukiraamene ndawasunga
+21“UkamenyanandidzikolaMerataimu+ndi kukamenyanandianthuokhalakuPekodi.
22M’dzikomuliphokosolankhondo+ndila chiwonongekochachikulu
23Ha!Babulowakhalabwinjamwaamitundu!
24Ndakutcheramsampha,ndipowagwidwa,iweBabulo, ndiposunadziwa;
+25Yehovawatsegulamaloakeosungiramozida+ndipo watulutsazidazaukaliwake,+pakutiiyindintchitoya Yehovawamakamum’dzikolaAkasidi
26Idzanipaiyekuchokerakumalireamalire,tsegulani nkhokwezake;
27Iphaning’ombezakezonse;atsikirekukaphedwa: Tsokakwaiwo!pakutilafikatsikulawo,nthawiyakulanga kwawo
+28Liwulaanthuameneathawa+ndikuthawam’dziko laBabulo+kukalengeza+m’Ziyonikubwezerachilango+ kwaYehovaMulunguwathu,+kubwezerakwakachisi wake
29ItanitsanioponyamivikutiamenyanendiBabulo,+inu nonseakukungauta,+muzizingamozungulira asapulumukemmodziwaiwo;mongamwazonse anazichita,mumchitireiye;pakutiwadzikuzapamasopa Yehova,ndiWoyerawaIsrayeli
30Chifukwachakeanyamataakeadzagwam’makwalala, ndiamunaakeonseankhondoadzalikhidwatsikulimenelo, atiYehova
31Taona,nditsutsananawe,iwewonyada,atiAmbuye Yehovawamakamu,pakutitsikulakolafika,nthawiimene ndidzakulangaiwe
32Ndipowonyadaadzagwa,nadzagwa,ndipopalibe ameneadzamuutsa;
33AteroYehovawamakamu;AnaaIsrayelindianaa Yudaanatsenderezedwapamodzi;anakanakuwalola amuke.
34Mombolowawondiwamphamvu;Yehovawamakamu ndidzinalace:iyeadzawaneneramlanduwaondithu,kuti atsitsimutsedziko,ndikusokonezaokhalam'Babulo +35Lupanga+lilipaAkasidi,+ndipaanthuokhala m’Babulo,+akalongaakendianzeruake,+watero Yehova.
36Lupangaliripaonama;ndipoiwoadzadana:lupangaliri paamphamvuace;ndipoadzathedwanzeru
37Lupangaliripaakavaloao,ndipamagaletaao,ndipa osakanizikaonsealimkatimwake;ndipoiwoadzakhala ngatiakazi:lupangaliripachumachake;ndipoadzabedwa. 38Chilalachilipamadziake;ndipoadzauma;pakutindilo dzikolamafanoosemedwa,ndipoakwiyiramafanoao
39Choterozilombozam’chipululupamodzindizilombo zam’zisumbuzidzakhalammenemo,+ndipoakadzidzi adzakhalammenemo,+ndiposimudzakhalansoanthu
mpakakalekalendiposimudzakhalamoku mibadwomibadwo.
40MongamomweMulunguanapasulaSodomundi Gomorandimidziyoyandikananayo,atiYehova;kotero kutipalibemunthuadzakhalammenemo,ngakhalemwana wamunthuadzakhalammenemo
41Taonani,anthuadzachokerakumpoto,ndimtundu waukulu,ndipomafumuambiriadzaukitsidwakuchokera kumalireadziko
42Adzagwirautandimkondo;aliankhanza,osacita cifundo;mauaoadzabangulangatinyanja,nadzakwerapa akavalo,nadzikonzekeretsa,mongamunthuwakunkhondo, kumenyanandiiwe,mwanawamkaziwaBabulo.
43MfumuyaBabuloyamvambiriyawo,ndipomanjaake analefuka;
44Taonani,adzakwerangatimkangowochokerakuphirila Yorodanokumkakumalookhalaamphamvu;koma ndidzawathamangitsamodzidzimutsa;pakutiafananandi inendani?ndipondaniadzandiikirainenthawi?ndipo mbusaameneadzaimapamasopangandani?
45CifukwacaceimvaniuphunguwaYehova,umene waupangirapaBabulo;ndizolingalirazacezimene alingiriradzikolaAkasidi:Zoonadi,ang'onoazoweta adzakokaiwo;
46PaphokosolakulandidwakwaBabulodzikolapansi lidzagwedezeka,ndipokulirakwamvekamwaamitundu
MUTU51
1AteroYehova;Taonani,ndidzautsiraBabulo,ndiiwo okhalapakatipaiwoakundiukira,mphepoyowononga; 2NdidzatumizaoulutsakuBabulo,ameneadzampeta, nadzakhuthuladzikolake;
3Woponyamivialandeutawakekwaiyewopinda,ndi wodzikwezandichovalachakechamphepo,ndipo musalekerereanyamataake;wononganikonsekhamulake lonse.
4Ophedwawoadzagwam’dzikolaAkasidi,ndi opyozedwam’makwalalaake
5PakutiIsrayeli,kapenaYudasanasiyidwandiMulungu wake,Yehovawamakamu;ngakhaledzikolaolinadzala ndicimopaWoyerawaIsrayeli
6ThawanipakatipaBabulo,ndipoyenseapulumutse moyowake;pakutiiyindiyonyengoyakubwezeraYehova; adzabwezerakwaiyemphothoyo
7Babulowakhalachikhochagolidem’dzanjalaYehova,+ ameneanaledzeretsadzikolonselapansichifukwachake amitundualimisala.
+8Babulowagwamwadzidzidzi+n’kuwonongedwa tenganimankhwalaamankhwalam’kuwawakwake,kuti kapenaangachiritsidwe
9IfetikanafunakuchiritsaBabulo,komaiye sanachiritsidwe;tisiyeniiye,ndipotiyenialiyensetipiteku dzikolakwawo:pakutichiweruzochakechafika kumwamba,ndipochakwezedwampakakumitambo
10Yehovawaonetsachilungamochathu:idzani,tinene m’ZiyonintchitoyaYehovaMulunguwathu.
11Wolanimivi;sonkhanitsanizikopa:Yehovawautsa mzimuwamafumuaAmedi;+chifukwandikubwezera+ kwaYehova,kubwezerakachisiwake.
12KwezanimbenderapamakomaaBabulo,limbitsani ulonda,kwezanialonda,konzaniolalira;pakutiYehova
walingalirandikuchitazimeneananenazaokhala m’Babulo.
13Iwewokhalapamadziambiri,wolemerandichuma, chitsirizirochakochafika,ndimuyesowakusirirakwako.
14Yehovawamakamuwalumbirapaiyeyekha,kuti, Zoonadindidzakudzazandianthu,mongazimbalamba; ndipoadzakuimbiraiwe
15Iyeanalengadzikolapansindimphamvuyake, anakhazikitsadzikolapansindinzeruzake,ndipoanayala kumwambandilunthalake
16Pamenealankhulamauake,palimkokomowamadzi m’mwamba;ndipoakwezeranthunzikumalekezeroa dzikolapansi;
17Munthualiyensealiwopusandiwosadziwa;woumba aliyenseanyazitsidwandifanolosema;pakutifanolake loyengangonyenga,ndipomulibempweyamwaiwo.
18Iwoalichabe,ntchitoyamphulupulu;panthawiya kulangidwakwaoadzatayika
19GawolaYakobosilingafananenazo;pakutiiyendiye analengazonse,ndipoIsrayelindiyendodoyacholowa chake;dzinalakendiYehovawamakamu
20Iwendiwenkhwangwayangandizidazangazankhondo: chifukwandiiwendidzaphwanyaamitundu,ndipondiiwe ndidzawonongamaufumu;
21Ndiiwendidzaphwanyakavalondiwokwerapowake; ndiiwendidzathyolathyolagaretandiwokwerapowake;
22Ndiiwendidzaphwanyamwamunandimkazi;ndiiwe ndidzaphwanyaokalambandiana;ndiiwe ndidzathyolathyolamnyamatandinamwali;
23Ndidzathyolapamodzindiiwembusandinkhosazake; ndiiwendidzatyolatyolamliminding’ombezakegoli;ndi iwendidzathyolathyolaakazembendiolamulira
+24NdidzabwezeraBabulondianthuonseokhala m’KasidizoipazonsezimeneanachitakuZiyonipamaso panu,”+wateroYehova
25Taona,nditsutsananawe,iwephirilakuononga,ati Yehova,ameneuonongadzikolonselapansi; 26Ndiposadzatengakwaiwemwalawapangondya, kapenamwalawamaziko;+komaudzakhalabwinja mpakakalekale,”+wateroYehova.
27Kwezanimbenderam’dziko,lizanilipengamwa amitundu;muikirekazembepaiye;Kwezaniakavalongati zimbalangondo.
28Konzekeranimitunduyaanthukutiamuukire,+ mafumuaAmedi,+akalongaake,olamuliraakeonse,+ ndidzikolonselaulamulirowake.
+29Dzikolidzanjenjemerandikumvachisoni,+chifukwa YehovaadzachitiraBabulo+bwinja,+kutidzikola Babulolikhalebwinjalopandawokhalamo
30AnthuamphamvuakuBabuloasiyakumenyankhondo, +ndipoakhalam’misasayawoAkhalangatiakazi; mipiringidzoyakeyathyoka.
31Mthengawinaadzathamangakukakomanandimnzace, ndimthengawinakukakomanandimnzace,kukauza mfumuyakuBabulokutimudziwakewalandidwa polekezera
32Ndipokutimipatayatsekedwa,ndimabango atenthedwandimoto,ndiankhondoachitamantha
33PakutiateroYehovawamakamu,MulunguwaIsrayeli; MwanawamkaziwaBabuloalingatidwale,ndiyonthawi yomupunthira;
34NebukadirezaramfumuyaBabulowandidyaine, wandiphwanyaine,wandiyesainechiwiyachopanda kanthu,wandimezangatichinjoka,wadzazamimbayake ndizokomazanga,wanditaya.
35Nkhanzazondichitiraine,ndithupilanga,zikhalepa Babulo,adzakhalam’Ziyoni;ndimwaziwangapaokhala m’Kasidi,atiYerusalemu
36CifukwacaceateroYehova;Taonani,ndidzakutsutsani, ndikubwezeracilango;ndipondidzaumitsanyanjayake, ndikuumitsaakasupeake
+37Babuloadzakhalamiunda,+malookhalaankhandwe, +chinthuchodabwitsa+ndicholozetsam’maso,popanda wokhalamo.
38Iwoadzabangulapamodzingatimikango:adzalirangati anaamikango
39M’kutenthakwawondidzawakonzeramadyerero,+ ndipondidzaledzeretsa,+kutiasangalale,+agonetulotofa nato,osadzukanso,”+wateroYehova
40Ndidzawatsitsirakophedwangatianaankhosa,ngati nkhosazamphongopamodzindimbuzizamphongo
41Sesakiwalandidwabwanji!ndipokudabwakwa ulemererowadzikolonselapansi!Babulowasanduka chozizwitsamwaamitundu!
42NyanjayakwerapaBabulo:yakwiririkandimafunde akeaunyinji.
43Mizindayakeyasandukabwinja,dzikoloumandi chipululu,dzikolopandamunthuwokhalamo,ndipopalibe mwanawamunthuwodutsamo.
44NdidzalangaBelim’Babulo,ndipondidzatulutsa m’kamwamwakechimenewameza;
45Anthuanga,tulukanipakatipake,ndipoaliyense apulumutsemoyowakekumkwiyowoyakamotowa Yehova
46ndimtimawanuungalefuke,ndikuopambiri idzamvekam’dziko;Mphekeserazidzafikachakachimodzi, ndipopambuyopakechakachinachidzafikambiri,ndi chiwawapadziko,wolamulirandiwolamulira.
47Cifukwacace,taonani,masikuakudza,pamene ndidzaweruzazifanizirozosemazakuBabulo;
48Pamenepokumwambandidzikolapansi,ndizonsezili mmenemozidzaimbiraBabulo,+pakutiofunkhaadzafika kwaiyekuchokerakumpoto,”+wateroYehova
49MongaBabuloanagwetsaophedwaaIsrayeli, momwemonsoophedwaadzikolonselapansiadzagwapa Babulo
50Inuamenemwapulumukalupanga,chokani, musaimirire:kumbukiraniYehovamulikutali,ndipo Yerusalemuakumbukiremumtimamwanu.
51Tachitamanyazi,chifukwatamvachitonzo;manyazi aphimbankhopezathu;pakutialendoalowam'malo opatulikaanyumbayaYehova
52Cifukwacace,taonani,masikuadza,atiYehova, pamenendidzaweruzamafanoakeosema,ndim’dzikolace lonseovulazidwaadzabuula
+53NgakhaleBabuloatakwerakumwamba,+ngakhale atalimbitsampandawolimbakwambiripamaloake otetezeka,+komaofunkhaadzachokerakwainekudzafika kwaiye,”+wateroYehova
54KukumvekakulirakochokerakuBabulo,+ndi chiwonongekochachikuluchochokeram’dzikolaAkasidi.
Yeremiya
55PakutiYehovawafunkhaBabulo,naonongamomawu akulu;mafundeakeakabangulangatimadziakulu, phokosolamawuawolimveka
56Popezawofunkhawam’fikira,ngakhalepaBabulo, ndipoamunaakeamphamvualandidwa,mautaaoonse athyoledwa;pakutiYehovaMulunguwakubwezera adzabwezerandithu
57Ndipondidzaledzeretsaakalongaake,ndianzeruake, akalongaake,ndiolamuliraake,ndiamunaakeamphamvu; 58AteroYehovawamakamu;MakomaotakataaBabulo adzaphwanyidwandithu,ndizipatazakezazitali zidzatenthedwandimoto;ndipoanthuadzagwirantchito pachabe,ndimitundupamoto,ndipoiwoadzatopa.
59MawuameneYeremiyamnenerianalamulaSeraya mwanawaNeriya,mwanawaMaaseya,pameneanapita ndiZedekiyamfumuyaYudakuBabulom’chaka chachinayichaulamulirowakeNdipoSerayauyuanali kalongawodekha
60ChoteroYeremiyaanalembam’bukuzoipazonse zimenezidzagweraBabulo,mawuonsewaolembedwa okhudzaBabulo
+61PamenepoYeremiyaanauzaSerayakuti:“Ukakafika kuBabulon’kuonandikuwerengamawuonsewa 62Pamenepouziti,Yehova,mwanenamotsutsamaloano, kuliononga,kutipasakhalemunthuwokhalamo,kapena nyama,komakutilikhalebwinjakosatha 63Ndipokudzali,pakuthakuwerengabukhuili, umalingirepomwala,ndikuliponyapakatipaFirate; 64Ndipoudzati,MomwemoBabuloadzamira,ndipo sadzaukansochifukwachachoipachimenendidzamtengera; ndipoadzatopa.MpakapanondimawuaYeremiya.
MUTU52
1Zedekiyaanaliwazakamakumiawirimphambucimodzi polowaufumuwace,nakhalamfumuzakakhumindi cimodzim'Yerusalemu.+Dzinalamayiakelinali Hamutali+mwanawamkaziwaYeremiyawakuLibina
2IyeanapitirizakuchitazoipapamasopaYehova, mogwirizanandizonsezimeneYehoyakimuanachita.
3PakutichifukwachamkwiyowaYehovazinachitikira muYerusalemundiYuda,mpakaanawachotsapamaso pake,+motiZedekiyaanapandukiramfumuyaBabulo.
4Ndipokunali,m’chakachachisanundichinayicha ulamulirowake,mweziwakhumi,tsikulakhumila mweziwo,NebukadirezaramfumuyakuBabuloanadza, iyendigululakelonselankhondo,kumenyanandi Yerusalemu,namangamisasamouzungulira,nauzungulira.
5Choteromzindawounazingidwampakachakacha11cha MfumuZedekiya
6Ndipom’mweziwacinai,tsikulacisanundicinaila mweziwo,njalainakulam’mudzi,ndipomunalibe chakudyakwaanthuam’dziko
7Pamenepomzindawounapasulidwa,+ndipoamunaonse ankhondoanathawa+ndikutulukamumzindawousiku kudzerapachipatachapakatipamakomaawiriakumunda wamfumu.(TsopanoAkasidianalipafupindimudzi pozungulirapo)ndipoanayendanjirayakuchigwa 8KomagululankhondolaAkasidilinathamangitsa mfumuyo,+n’kukapezaZedekiyam’zidikhazaYeriko. ndikhamulacelonselinabalalikakumcokera
9Kenakoanagwiramfumuyon’kupitanayokwamfumu yaBabulokuRibila+m’dzikolaHamati.kumene adamweruza
10MfumuyaBabuloinaphaanaaZedekiyapamasopake, ndipoinaphansoakalongaonseaYudakuRibila.
11NdipoanakolowolamasoaZedekiya;+Kenakomfumu yakuBabuloinam’mangamaunyolo+n’kupitanayeku Babulondikum’tsekeram’ndendempakatsikulaimfa yake
12Tsopanom’mweziwachisanu,patsikulakhumila mweziwo,m’chakacha19chaNebukadirezaramfumuya Babulo,Nebuzaradani+mkuluwaasilikaliolondera mfumu+ameneanalikutumikiramfumuyaBabulo anafikakuYerusalemu
13NdipoanatenthanyumbayaYehova,ndinyumbaya mfumu;ndinyumbazonsezaYerusalemu,ndinyumba zonsezaakulu,anazitenthandimoto;
14NdipogululonselankhondolaAkasidi,limenelinali ndimkuluwaasilikaliolonderamfumu,linagwetsa mpandawonsewaYerusalemumozungulira
15PenepapoNebuzaradanimulongozgiwaŵalinda ŵakatolerakuwuzgaŵanyakemwaŵanthuŵakavu,na ŵanthuŵanyakeawoŵakakhalapomumsumba,naawo ŵakagaluka,awoŵakapokerakwathembalaBabulonina wumbauwowose.
16KomaNebuzaradanikapitaowaalondaanasiyaena mwaosaukaam’dzikokutiakhaleolimamindayamphesa ndiolima.
+17Komansomizatiyamkuwa+imeneinalim’nyumba yaYehova,zotengera,+nyanjayamkuwa+imeneinali m’nyumbayaYehova,Akasidianathyolan’kutenga mkuwawakewonsen’kupitanawokuBabulo
18Anatengansomiphika,ndizoolera,ndizozimitsiranyale, ndimbalezolowa,ndizipande,ndiziwiyazonsezamkuwa zimeneankatumikiranazo
19ndimbalezowazira,ndizopaliramoto,ndimbale zolowa,ndimiphika,ndizoikaponyali,ndizipande,ndi zikho;ndichumachagolidichagolidi,ndichasilivacha siliva,anacotsakapitaowaalonda
20Zipilalaziwirizo,nyanjaimodzi,nding’ombe zamphongo12zamkuwazimenezinalipansipazotengera zimeneMfumuSolomoinapangam’nyumbayaYehova, mkuwawaziwiyazonseziunaliwosalemera.
21Ponenazazipilalazo,nsanamiraimodzikutalikakwake kunalimikono18;ndichingwechamikonokhumindi iwirichinalizungulira;ndikuchindikalakwakekunalizala zinayi;
22Ndipopamwambapakepanalimutuwamkuwa;ndi msinkhuwamutuumodziunalimikonoisanu,ndi maukondendimakangazapamituyozungulira,yonse yamkuwaChipilalachachiwirichinalinsochimodzimodzi ndimakangaza.
23Ndipopanalimakangazamakumiasanundianaikudza asanundilimodzimbaliimodzi;ndimakangazaonseapa ukondeanalizanapozungulirapake
24NdipomkuluwaalondaanatengaSerayawansembe wamkulu,ndiZefaniyawansembewachiŵiri,ndialonda atatuapakhomo;
25Anatengansomdindom’mudzimo,woyang’aniraamuna ankhondo;ndiamunaasanundiawiriaiwoakukhala pafupindinkhopeyamfumu,opezekam'mudzi;ndi mlembiwamkuluwakhamulo,wakuwerengaanthua
m’dziko;ndiamunamakumiasanundilimodziaanthua m’dziko,opezekapakatipamudzi.
+26ChoteroNebuzaradani+mkuluwaasilikaliolondera mfumuanawatengan’kupitanawokwamfumuyaBabulo kuRibila.
27MfumuyaBabuloinawakantha+ndikuwapha+ku Ribila+m’dzikolaHamatiChoteroYudaanatengedwa ukapolokuchokam’dzikolakwawo.
28AwandianthuameneNebukadirezaraanawatenga ndende:m’chakachachisanundichiwiriAyudazikwi zitatumphambumakumiawirikudzaatatu;
29M’chakachakhumindichisanundichitatucha ulamulirowaNebukadirezaraanatengerandendeanthu mazanaasanundiatatukudzamakumiatatundiawiri kuchokerakuYerusalemu
30M’chakacha23chaNebukadirezara,Nebuzaradani+ mkuluwaasilikaliolonderamfumuanatengeraAyuda anthu745Anthuonseanalipo4,600
31Ndipokunali,cakacamakumiatatumphambuzisanu ndiziwiricandendeyaYehoyakinimfumuyaYuda, mweziwakhumindiciwiri,tsikulamakumiawirindi zisanulamwezi,EvilimerodakimfumuyakuBabulo m’cakacoyambacaufumuwaceanakwezamutuwa YehoyakinimfumuyaYuda,namturutsam’ndende
32Nalankhulanayemokomamtima,nakwezampando wakewachifumupamwambapamipandoyamafumu okhalanayem’Babulo;
33Ndipoanasinthazobvalazakezam’ndende,nadya mkatepamasopakemasikuonseamoyowake
34Ndipopazakudyazake,mfumuyakuBabulo inkampatsachakudyachosalekeza,tsikunditsiku,kufikira tsikulaimfayake,masikuonseamoyowake